< Psalmorum 124 >

1 Canticum graduum. Nisi quia Dominus erat in nobis, dicat nunc Israel:
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Akanapanda kukhala mbali yathu Yehova, anene tsono Israeli,
2 nisi quia Dominus erat in nobis, Cum exurgerent homines in nos,
akanapanda kukhala mbali yathu Yehova, potiwukira anthuwo,
3 forte vivos deglutissent nos: Cum irasceretur furor eorum in nos,
iwo atatipsera mtima, akanatimeza amoyo;
4 forsitan aqua absorbuisset nos.
chigumula chikanatimiza, mtsinje ukanatikokolola,
5 Torrentem pertransivit anima nostra: forsitan pertransisset anima nostra aquam intolerabilem.
madzi a mkokomo akanatikokolola.
6 Benedictus Dominus qui non dedit nos, in captionem dentibus eorum.
Atamandike Yehova, amene sanalole kuti tikhale chakudya cha mano awo.
7 Anima nostra sicut passer erepta est de laqueo venantium: Laqueus contritus est, et nos liberati sumus.
Moyo wathu wawonjoka ngati mbalame yokodwa mu msampha wa mlenje; msampha wathyoka, ndipo ife tapulumuka.
8 Adiutorium nostrum in nomine Domini, qui fecit caelum et terram.
Thandizo lathu lili mʼdzina la Yehova wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.

< Psalmorum 124 >