< Nehemiæ 7 >

1 Postquam autem ædificatus est murus, et posui valvas, et recensui janitores, et cantores, et Levitas,
Khoma linamangidwa ndipo zitseko zinayikidwa. Pambuyo pake alonda a Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo ndiponso Alevi anasankhidwa.
2 præcepi Hanani fratri meo, et Hananiæ principi domus de Jerusalem (ipse enim quasi vir verax et timens Deum plus ceteris videbatur),
Kenaka ine ndinasankha mʼbale wanga Hanani pamodzi ndi Hananiya woyangʼanira nsanja yankhondo kukhala olamulira Yerusalemu chifukwa iyeyu anali munthu odalirika ndi woopa Mulungu kuposa anthu ena.
3 et dixi eis: Non aperiantur portæ Jerusalem usque ad calorem solis. Cumque adhuc assisterent, clausæ portæ sunt, et oppilatæ: et posui custodes de habitatoribus Jerusalem, singulos per vices suas, et unumquemque contra domum suam.
Ine ndinawawuza kuti, “Musalole kuti zipata za Yerusalemu zitsekulidwe mpaka dzuwa litatentha, ndipo alonda asanaweruke aonetsetse kuti atseka zitseko ndi kuzipiringidza. Musankhe alonda pakati pa anthu okhala mu Yerusalemu, ena akhale pa malo pawo ndi ena akhale moyangʼanana ndi nyumba zawo.”
4 Civitas autem erat lata nimis et grandis, et populus parvus in medio ejus, et non erant domus ædificatæ.
Tsono mzinda wa Yerusalemu unali wotambasuka ndiponso waukulu koma munali anthu ochepa ndipo nyumba zinali zisanamangidwe.
5 Deus autem dedit in corde meo, et congregavi optimates, et magistratus, et vulgus, ut recenserem eos: et inveni librum census eorum qui ascenderant primum, et inventum est scriptum in eo.
Ndipo Mulungu wanga anayika mu mtima mwanga maganizo oti ndisonkhanitse anthu olemekezeka, akuluakulu ndi anthu onse kuti alembetse mayina mwa mabanja awo. Ndinapeza buku limene munalembedwa mayina a mabanja a iwo amene anayamba kubwera kuchokera ku ukapolo. Izi ndi zimene ndinazipeza zitalembedwa mʼmenemo:
6 Isti filii provinciæ, qui ascenderunt de captivitate migrantium, quos transtulerat Nabuchodonosor rex Babylonis, et reversi sunt in Jerusalem et in Judæam, unusquisque in civitatem suam.
Awa ndi anthu a mʼchigawo cha Yuda amene anabwerera kuchokera ku ukapolo amene Nebukadinezara mfumu ya Babuloni anawatenga ukapolo. Iwo anabwerera ku Yerusalemu ndi ku Yuda, aliyense ku mzinda wa makolo ake.
7 Qui venerunt cum Zorobabel, Josue, Nehemias, Azarias, Raamias, Nahamani, Mardochæus, Belsam, Mespharath, Begoai, Nahum, Baana. Numerus virorum populi Israël:
Anabwera pamodzi ndi atsogoleri awa: Zerubabeli, Yesuwa, Nehemiya, Azariya, Raamiya, Nahamani, Mordekai, Bilisani, Misipereti, Bigivai, Nehumu ndi Baana. Tsono chiwerengero cha anthu a ku Israeli chinali chotere:
8 filii Pharos, duo millia centum septuaginta duo:
Zidzukulu za Parosi 2,172
9 filii Saphatia, trecenti septuaginta duo:
Zidzukulu za Sefatiya 372
10 filii Area, sexcenti quinquaginta duo:
Zidzukulu za Ara 652
11 filii Phahathmoab filiorum Josue et Joab, duo millia octingenti decem et octo:
Zidzukulu za Pahati-Mowabu (kudzera mu mʼbado wa Yesuwa ndi Yowabu) 2,818
12 filii Ælam, mille ducenti quinquaginta quatuor:
Zidzukulu za Elamu 1,254
13 filii Zethua, octingenti quadraginta quinque:
Zidzukulu za Zatu 845
14 filii Zachai, septingenti sexaginta:
Zidzukulu za Zakai 760
15 filii Bannui, sexcenti quadraginta octo:
Zidzukulu za Binuyi 648
16 filii Bebai, sexcenti viginti octo:
Zidzukulu za Bebai 628
17 filii Azgad, duo millia trecenti viginti duo:
Zidzukulu za Azigadi 2,322
18 filii Adonicam, sexcenti sexaginta septem:
Zidzukulu za Adonikamu 667
19 filii Beguai, duo millia sexaginta septem:
Zidzukulu za Abigivai 2,067
20 filii Adin, sexcenti quinquaginta quinque:
Zidzukulu za Adini 655
21 filii Ater, filii Hezeciæ, nonaginta octo:
Zidzukulu za Ateri (kudzera mwa Hezekiya) 98
22 filii Hasem, trecenti viginti octo:
Zidzukulu za Hasumu 328
23 filii Besai, trecenti viginti quatuor:
Zidzukulu za Bezayi 324
24 filii Hareph, centum duodecim:
Zidzukulu za Harifu 112
25 filii Gabaon, nonaginta quinque:
Zidzukulu za Gibiyoni 95.
26 filii Bethlehem et Netupha, centum octoginta octo.
Anthu a ku Betelehemu ndi Netofa 188
27 Viri Anathoth, centum viginti octo.
Anthu a ku Anatoti 128
28 Viri Bethazmoth, quadraginta duo.
Anthu a ku Beti-Azimaveti 42
29 Viri Cariathiarim, Cephira, et Beroth, septingenti quadraginta tres.
Anthu a ku Kiriati Yeyarimu Kefira ndi Beeroti 743
30 Viri Rama et Geba, sexcenti viginti unus.
Anthu a ku Rama ndi Geba 621
31 Viri Machmas, centum viginti duo.
Anthu a ku Mikimasi 122
32 Viri Bethel et Hai, centum viginti tres.
Anthu a ku Beteli ndi Ai 123
33 Viri Nebo alterius, quinquaginta duo.
Anthu a ku Nebo winayo 52
34 Viri Ælam alterius, mille ducenti quinquaginta quatuor.
Ana a Elamu wina 1,254
35 Filii Harem, trecenti viginti.
Zidzukulu za Harimu 320
36 Filii Jericho, trecenti quadraginta quinque.
Zidzukulu za Yeriko 345
37 Filii Lod Hadid et Ono, septingenti viginti unus.
Zidzukulu za Lodi, Hadidi ndi Ono 721
38 Filii Senaa, tria millia nongenti triginta.
Zidzukulu za Senaya 3,930.
39 Sacerdotes: filii Idaia in domo Josue, nongenti septuaginta tres.
Ansembe anali awa: A banja la Yedaya (ndiye kuti zidzukulu za Yesuwa) 973
40 Filii Emmer, mille quinquaginta duo.
Zidzukulu za Imeri 1,052
41 Filii Phashur, mille ducenti quadraginta septem.
Zidzukulu za Pasi-Huri 1,247
42 Filii Arem, mille decem et septem. Levitæ:
Zidzukulu za Harimu 1,017.
43 filii Josue et Cedmihel filiorum
Alevi anali awa: A banja la Yesuwa ndi Kadimieli, ndiye kuti zidzukulu za Hodaviya 74.
44 Oduiæ, septuaginta quatuor. Cantores:
Anthu oyimba: Zidzukulu za Asafu 148.
45 filii Asaph, centum quadraginta octo.
Alonda a ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Salumu, Ateri, Talimoni, Hatita ndi Sobai 138.
46 Janitores: filii Sellum, filii Ater, filii Telmon, filii Accub, filii Hatita, filii Sobai: centum triginta octo.
Anthu ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Ziha, zidzukulu za Hasufa, zidzukulu za Tabaoti,
47 Nathinæi: filii Soha, filii Hasupha, filii Tebbaoth,
Zidzukulu Kerosi, zidzukulu za Siya, zidzukulu za Padoni
48 filii Ceros, filii Siaa, filii Phadon, filii Lebana, filii Hagaba, filii Selmai,
Zidzukulu za Lebana za Hagaba, ndi za Salimayi,
49 filii Hanan, filii Geddel, filii Gaher,
Zidzukulu za Hanani, zidzukulu za Gideli, zidzukulu za Gahari,
50 filii Raaia, filii Rasin, filii Necoda,
Zidzukulu za Reyaya, zidzukulu za Rezini, zidzukulu za Nehoda,
51 filii Gezem, filii Aza, filii Phasea,
Zidzukulu za Gazamu, zidzukulu za Uza, zidzukulu za Paseya,
52 filii Besai, filii Munim, filii Nephussim,
Zidzukulu za Besai, zidzukulu za Meunimu, zidzukulu za Nefusimu,
53 filii Bacbuc, filii Hacupha, filii Harhur,
Zidzukulu za Bakibuku, zidzukulu za Hakufa, zidzukulu za Harihuri,
54 filii Besloth, filii Mahida, filii Harsa,
Zidzukulu za Baziliti, zidzukulu za Mehida, zidzukulu za Harisa,
55 filii Bercos, filii Sisara, filii Thema,
Zidzukulu za Barikosi, zidzukulu za Sisera, zidzukulu za Tema
56 filii Nasia, filii Hatipha,
Zidzukulu za Neziya, ndi zidzukulu za Hatifa.
57 filii servorum Salomonis, filii Sothai, filii Sophereth, filii Pharida,
Zidzukulu za antchito a Solomoni: Zidzukulu za Sotai, zidzukulu za Sofereti, zidzukulu za Perida
58 filii Jahala, filii Darcon, filii Jeddel,
zidzukulu za Yaala, zidzukulu za Darikoni, zidzukulu za Gideli,
59 filii Saphatia, filii Hatil, filii Phochereth, qui erat ortus ex Sabaim filio Amon.
zidzukulu za Sefatiya, zidzukulu za Hatilu zidzukulu za Pokereti-Hazebaimu ndi zidzukulu Amoni.
60 Omnes Nathinæi, et filii servorum Salomonis, trecenti nonaginta duo.
Anthu onse ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi zidzukulu za antchito a Solomoni analipo 392.
61 Hi sunt autem qui ascenderunt de Thelmela, Thelharsa, Cherub, Addon, et Emmer: et non potuerunt indicare domum patrum suorum, et semen suum, utrum ex Israël essent,
Ali munsiwa anachokera ku Teli-Mela, Teri-Harisa, Kerubi, Adoni, ndi Imeri, koma sanathe kunena mwa tchutchutchu kuti makolo awo kapena mafuko awo analidi Aisraeli kapena ayi.
62 filii Dalaia, filii Tobia, filii Necoda, sexcenti quadraginta duo.
Zidzukulu za Delaya, zidzukulu za Tobiya ndi zidzukulu za Nekoda 642.
63 Et de sacerdotibus, filii Habia, filii Accos, filii Berzellai, qui accepit de filiabus Berzellai Galaaditis uxorem, et vocatus est nomine eorum.
Ndiponso ena pakati pa ansembe anali awa: zidzukulu za Hobiya, zidzukulu za Hakozi ndi zidzukulu za Barizilai (munthu amene anakwatira mwana wamkazi wa Barizilai wa ku Giliyadi ndipo amatchedwa dzina limenelo).
64 Hi quæsierunt scripturam suam in censu, et non invenerunt: et ejecti sunt de sacerdotio.
Iwowa anafufuzafufuza mayina awo mʼbuku la mibado ya mabanja awo ndipo sanapeze mayina awo kotero anachotsedwa pa unsembe nawerengedwa ngati odetsedwa pa chipembedzo.
65 Dixitque Athersatha eis ut non manducarent de Sanctis sanctorum, donec staret sacerdos doctus et eruditus.
Choncho bwanamkubwa anawawuza anthuwo kuti asamadye nawo chakudya china chilichonse choperekedwa kwa Mulungu mpaka patapezeka wansembe wodziwa kugwiritsa bwino ntchito ya Urimu ndi Tumimu.
66 Omnis multitudo quasi vir unus quadraginta duo millia trecenti sexaginta,
Chiwerengero chonse cha anthuwa chinali 42,360.
67 absque servis et ancillis eorum, qui erant septem millia trecenti triginta septem, et inter eos cantores et cantatrices, ducenti quadraginta quinque.
Kuwonjezera pamenepa panali antchito awo aamuna ndi aakazi 7,337 ndiponso anthu aamuna ndi aakazi oyimba nyimbo okwanira 245.
68 Equi eorum, septingenti triginta sex: muli eorum, ducenti quadraginta quinque:
Panali akavalo 736, abulu angʼonoangʼono 245.
69 cameli eorum, quadringenti triginta quinque: asini, sex millia septingenti viginti.
Ngamira zawo zinalipo 435 ndipo abulu analipo 6,720.
70 Nonnulli autem de principibus familiarum dederunt in opus. Athersatha dedit in thesaurum auri drachmas mille, phialas quinquaginta, tunicas sacerdotales quingentas triginta.
Atsogoleri ena a mabanja anapereka mphatso zothandizira ntchito. Bwanamkubwa anapereka ku thumba losungira chuma, ndalama zagolide za makilogalamu asanu ndi atatu, mabeseni makumi asanu ndi zovala za ansembe 530.
71 Et de principibus familiarum dederunt in thesaurum operis, auri drachmas viginti millia, et argenti mnas duo millia ducentas.
Atsogoleri ena amabanja anapereka ku thumba losungira chuma ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndiponso ndalama za siliva zokwana makilogalamu 1,250.
72 Et quod dedit reliquus populus, auri drachmas viginti millia, et argenti mnas duo millia, et tunicas sacerdotales sexaginta septem.
Anthu ena onse otsala anapereka ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndalama za siliva zokwana makilogalamu 140, ndiponso zovala za ansembe 67.
73 Habitaverunt autem sacerdotes, et Levitæ, et janitores, et cantores, et reliquum vulgus, et Nathinæi, et omnis Israël, in civitatibus suis.
Choncho ansembe, Alevi, alonda a Nyumba ya Mulungu, anthu oyimba nyimbo, ena mwa anthu wamba, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi Aisraeli ena onse ankakhala mʼmizinda yawo. Pofika mwezi wachisanu ndi chiwiri Aisraeli onse anali atakhazikika mʼmizinda yawo.

< Nehemiæ 7 >