< Zechariah 8 >
1 LEUM GOD Kulana El tuh sang kas in sulkakinyuk se inge nu sel Zechariah:
Awa ndi mawu amene Yehova Wamphamvuzonse ananena.
2 “Nga arulana ke kasru acn Jerusalem ke sripen lungse yohk luk nu sin mwet we, sie lungse su pwanang nga kasrkusrak sin mwet lokoalok lal.
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ine ndikuchitira nsanje yayikulu Ziyoni. Mtima wanga ukupweteka chifukwa cha nsanje pa iyeyo.”
3 Nga ac foloko nu Jerusalem, siti mutal sik, ac muta we. Ac fah eteyuk acn we mu sie siti su inse pwayena nu sik, ac eol sin LEUM GOD Kulana ac fah pangpang eol mutal.
Yehova akuti, “Ndidzabwerera ku Ziyoni ndi kukakhala ku Yerusalemu. Pamenepo Yerusalemu adzatchedwa Mzinda wa Choonadi ndipo phiri la Yehova Wamphamvuzonse lidzatchedwa Phiri Lopatulika.”
4 Mukul matu ac mutan matu, su arulana matu pwanang elos orekmakin sikal, elos ac fah sifil tukeni muta ke acn in tukeni in siti uh.
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Abambo ndi amayi okalamba adzakhalanso mʼmisewu ya mu Yerusalemu, aliyense ali ndi ndodo mʼmanja mwake chifukwa cha kuchuluka kwa masiku ake.
5 Ac inkanek uh fah sifilpa sessesla ke tulik mukul ac tulik mutan ma srisrital.
Ndipo misewu ya mu mzindamo idzadzaza ndi anyamata ndi atsikana akusewera.”
6 “Ma se inge ac nunkeyuk mu upa sin mwet lula in mutunfacl se inge, tusruktu ac tia upa sik.
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ngati zikuoneka kuti nʼzosatheka kwa anthu otsala pa nthawi ino, kodi zidzakhala zosathekanso kwa Ine?” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
7 Nga fah molela mwet luk liki facl ma elos utukla sruoh we,
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Taonani ndidzapulumutsa anthu anga kuchokera ku mayiko a kummawa ndi kumadzulo.
8 ac folokunulosme liki acn kutulap ac roto elos in tuh muta in Jerusalem. Elos fah mwet luk, ac nga fah God lalos, ac nga fah leum faclos ke suwohs ac pwaye.
Ndidzawabweretsa kuti adzakhale mu Yerusalemu; adzakhala anthu anga, ndipo Ine ndidzakhala Mulungu wawo, wokhulupirika ndi wolungama pakati pawo.”
9 “Kowos in pulaik na, tuh inge kowos sifil pacna lohng kas su mwet palu elos tuh kaskaskin ke pacl se ma tuh oakwuk pwelung nu ke sifil musaiyuk Tempul luk.
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Inu amene tsopano mukumva mawu awa amene akuyankhula aneneri amene analipo pamene ankayika maziko a nyumba ya Yehova Wamphamvuzonse, ‘limbani mtima kuti mumange Nyumba ya Yehova.’
10 Meet liki pacl sac, wangin sunun mani in sang moli mwet orekma ku kosro in orekma, ac wangin mwet moul in misla ke sripen mwet sulallal. Nga tuh furokla mwet uh in alein nu sin sie sin sie.
Mpaka nthawi imeneyi panalibe munthu wolandira malipiro pa ntchito kapena ndalama zolipirira nyama zogwira ntchito. Panalibe munthu amene ankadzigwirira ntchito mwamtendere chifukwa choopa adani ake, pakuti Ine ndinkawayambanitsa.
11 Tusruktu ingela nga ac oru in sie na liki meet ah nu sin mwet in mutunfacl se inge su painmoulla.
Koma tsopano sindidzachitira otsala mwa anthu awa zomwe ndinachita kale,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
12 Elos ac fah yukwiya sacn sunalos in misla. Ima grape lalos ac fah isus fahko, fohkon acn uh ac fah sranom, na ac fah yohk af. Nga fah sang mwe insewowo inge nukewa nu sin mwet in mutunfacl sik su ac painmoulla.
“Pakuti mbewu zidzamera bwino, mpesa udzabala zipatso zake, nthaka idzatulutsa zomera zake, ndi thambo lidzagwetsa mame. Ndidzapereka zonse kukhala cholowa cha otsala mwa anthu awa.
13 Mwet Judah ac mwet Israel! In pacl meet ah mwet in mutunfacl saya uh ac selngai sie sin sie ac fahk, ‘Lela kain ongoiya ma tuh putati nu fin mwet Judah ac mwet Israel in putati nu fowos!’ Tusruktu nga fah molikowosla, na mwet in mutunfacl saya uh ac fah fahk nu sin sie sin sie, ‘Lela kowos in insewowo oana mwet Judah ac mwet Israel!” Ouinge kowos in pulaik ac tiana sangeng.”
Monga mwakhala muli chinthu chotembereredwa pakati pa mitundu ina ya anthu, inu Yuda ndi Israeli, choncho ndidzakupulumutsani, ndipo mudzakhala dalitso. Musachite mantha, koma limbani mtima.”
14 LEUM GOD Kulana El fahk, “Ke mwet matu lowos meet ah tuh oru nga kasrkusrakak ah, nga lumahla mwe ongoiya nu selos, ac tiana ekulla nunak luk, a nga orala na ma nga akoo nu selos uh.
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Monga ndinatsimikiza mtima kubweretsa choyipa pa inu, komanso osakuchitirani chisoni pamene makolo anu anandikwiyitsa,” akutero Yehova,
15 Tusruktu inge, nga lumahla tari nga in akinsewowoye mwet Jerusalem ac mwet Judah. Ke ma inge, nimet kowos sangeng.
“Choncho tsopano ndatsimikiza mtima kuchitiranso zabwino Yerusalemu ndi Yuda. Musachite mantha.
16 Pa inge ma kowos enenu in oru: Kaskas in pwaye nu sin sie sin sie. In pacl in nununku, kowos oru nununku lowos an in suwohs ac pwaye, tuh in oasr misla.
Zinthu zoti muchite ndi izi: Muziwuzana zoona zokhazokha, muziweruza moona ndi mwachilungamo mʼmabwalo anu;
17 Nimet oru kutena kain oakwuk ma ac kunausla sie sin sie. Ac nimet orek loh kikiap ye fulahk. Nga srunga kikiap, sesuwos, ac kutena ma ac kunausla moul lun mwet.”
musamachitire mnzanu chiwembu, musamakonde kulumbira zonama. Zonsezi Ine ndimadana nazo,” akutero Yehova.
18 LEUM GOD Kulana El sang kas in sulkakinyuk inge nu sel Zechariah:
Yehova Wamphamvuzonse anayankhulanso nane.
19 “Lalo ma orek ke malem akakosr, aklimekosr, akitkosr, ac aksingoul uh, ingela ac fah pangpang kufwa in engan ac insewowo nu sin mwet Judah. Kowos fah lungse ma pwaye ac ma misla.”
Ndipo ananena kuti, “Kusala zakudya kwa pa mwezi wachinayi, chisanu, chisanu ndi chiwiri ndi wakhumi, kudzakhala nthawi yachimwemwe, ya chisangalalo ndi nthawi ya madyerero chikondwerero kwa Yuda. Nʼchifukwa chake muzikonda choonadi ndi mtendere.”
20 LEUM GOD Kulana El fahk, “Pacl se ac fah tuku ke mwet in siti puspis ac fah tuku nu Jerusalem.
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Anthu a mitundu yambiri ndi anthu okhala mʼmizinda yambiri adzabwerabe,
21 Elos su tuku liki sie siti ac fah fahk nu selos su tuku liki sie pacna siti, ‘Kut ac som alu nu sin LEUM GOD Kulana, ac pre Elan akinsewowoye kut. Fahsru wi kut!”
ndipo nzika za mzinda wina zidzapita ku mzinda wina, kukanena kuti, ‘Tiyeni mwamsanga tikapemphe madalitso kwa Yehova ndi kukapembedza Yehova Wamphamvuzonse. Inenso ndikupita kumeneko.’
22 Mwet puspis, oayapa mutunfacl ku puspis, ac fah tuku nu Jerusalem in alu nu sin LEUM GOD Kulana, ac pre ac siyuk ke mwe akinsewowo lal.
Anthu ambiri ndiponso a ku mayiko amphamvu adzabwera ku Yerusalemu kudzapembedza Yehova Wamphamvuzonse ndi kudzapempha madalitso.”
23 In len ingo, mwet saya singoul ac fah tuku nu yurin sie mwet Jew ac fahk, ‘Kut ke wi kom, mweyen kut lohng lah God El wi kowos, mwet Jew.’”
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Masiku amenewo anthu khumi ochokera ku mitundu ya anthu a ziyankhulo zosiyana adzagwira mkanjo wa Myuda ndi kunena kuti, ‘Tipite nawo, chifukwa tamva kuti Mulungu ali nanu.’”