< Zechariah 7 >

1 In yac se akakosr ma Darius el Tokosra Fulat, in len se akakosr ke malem se akeu (malem in Kislev), LEUM GOD El ase nu sik sie kas in sulkakinyuk.
Pa chaka chachinayi cha Mfumu Dariyo, pa tsiku lachinayi la Kisilevi, mwezi wachisanu ndi chinayi, Yehova anayankhula ndi Zekariya.
2 Mwet Bethel elos supwal Sharezer, Regemmelech ac mwet mukul sayalos, in som nu in Tempul lun LEUM GOD Kulana, in pre ke akinsewowo lun LEUM GOD
Anthu a ku Beteli anali atatuma Sarezeri ndi Regemu-Meleki pamodzi ndi anthu awo, kuti akapemphe chifundo kwa Yehova
3 ac in siyuk sin mwet tol ac mwet palu mwe siyuk se inge; “Ya kut enenu in srakna orek asor ke musalla lun Tempul, ac lalo ke malem se aklimekosr, oana kut muta oru ke yac puspis nwe inge uh?”
pokafunsa kwa ansembe a ku Nyumba ya Yehova Wamphamvuzonse ndi aneneri kuti, “Kodi ine ndizilira ndi kusala zakudya pa mwezi wachisanu, monga mmene ndakhala ndikuchitira pa zaka zambiri?”
4 Ac pa inge kas lun LEUM GOD ma tuku nu sik.
Pamenepo Yehova Wamphamvuzonse anayankhula nane kuti,
5 El fahk, “Fahkang nu sin mwet in facl se inge ac mwet tol, lah ke pacl ma elos lalo ac tung ke malem aklimekosr ac akitkosr ke pulan yac itngoul inge, elos tia oru in akfulatyeyu.
“Funsa anthu onse a mʼdziko ndi ansembe kuti, ‘Pamene munkasala zakudya pa mwezi wachisanu ndi wachisanu ndi chiwiri pa zaka 70 zapitazi, kodi munkasala chifukwa cha Ine?
6 Ac ke pacl se ma elos mongo ac nim uh, elos oru na nu ke lungse lalos sifacna.”
Ndipo pamene munkadya ndi kumwa, kodi simunkachita zimenezi podzisangalatsa nokha?
7 Pa inge ma LEUM GOD El tuh fahk nu sin mwet palu meet ah, ke pacl se Jerusalem tuh yohk kasrup la ac sessesla ke mwet, ac ke pacl se ma pukanten mwet tuh muta, tia in acn ma rauneak siti ah mukena, a oayapa ke tafunyen eir ac pe eol layen nu roto ah.
Kodi awa si mawu amene Yehova ankanena kudzera mwa aneneri oyamba aja pamene Yerusalemu ndi mizinda yake yozungulira anali pa mtendere ndi pa ulemerero, ndi pamene Negevi ndi ku madera akumadzulo a mʼmbali mwa phiri munali anthu?’”
8 LEUM GOD El sang kas inge nu sel Zechariah:
Ndipo Yehova anayankhulanso ndi Zekariya kuti,
9 “Pacl loes somla nga tuh sang sap soko inge nu sin mwet luk: ‘Kowos in liyaung tuh nununku suwohs in orek, ac tuh kowos in kulang ac pakoten nu sin sie sin sie.
“Yehova Wamphamvuzonse akuti, ‘Muziweruza molungama; muzichitirana chifundo ndi kumverana chisoni.
10 Nimet kowos akkemkatuye katinmas, tulik mukaimtal, mwetsac su muta inmasrlowos, ku kutena mwet su enenu. Ac nimet suk inkanek in akkeokye sie sin sie.’
Musamazunze akazi amasiye kapena ana amasiye, alendo kapena osauka. Musamaganizirane zoyipa mʼmitima mwanu.’
11 “Tusruktu mwet luk elos likkekelana ac tia lungse porongo. Elos kaliya nunak lalos
“Koma makolo anu anakana kumvera uthenga umenewu; anawumitsa mtima nandifulatira, natseka makutu awo kuti asamve.
12 ac akupaye insialos in keke oana eot uh. Mweyen elos tia lohng kas in luti su nga supu sin mwet palu su tuh muta in pacl meet ah, ma inge arulana akkasrkusrakyeyu.
Anawumitsa mitima yawo ngati mwala wa sangalabwi ndipo sanamvere lamulo kapena mawu amene Yehova Wamphamvuzonse anawatumiza mwa Mzimu wake kudzera mwa aneneri oyamba aja. Kotero Yehova Wamphamvuzonse anakwiya kwambiri.
13 Ke sripen elos tuh tia lipsre ke pacl nga kaskas uh, oru nga tia pacna topkolos ke pacl elos pre uh.
“‘Pamene ndinawayitana, iwo sanamvere; choncho pamene iwo anandiyitana, Ine sindinamverenso,’ akutero Yehova Wamphamvuzonse.
14 Nga pokolosla oana sie paka, tuh elos in muta fin acn lun mwet saya. Acn na wowo se inge tuh filfillana oan, wanginna mwet muta fac.”
‘Ndinawamwaza ndi kamvuluvulu pakati pa mitundu yonse ya anthu, kumene anali alendo. Dziko lawo linatsala litasakazidwa kwambiri kotero kuti palibe amene amabwera kapena kupitamo. Umu ndi mmene anasandutsira dziko labwino kukhala chipululu.’”

< Zechariah 7 >