< On Lal Solomon 8 >

1 Nga ke in tamulel se luk pa kom, Ac in nina kiuk ah pa katiti kom ke titi lal uh, Na nga fin sun kom inkanek uh, Nga lukun ngokya motom ac mwet uh ac tia suk lah efu.
Ukanakhala kuti ndiwe mlongo wanga, amene anayamwa mawere a amayi anga! Ndikanakumana nawe pa njira, ndikanakupsompsona, ndipo palibe wina aliyense akanandinyoza.
2 Nga lukun uskomla nu lohm sin nina kiuk, Kom in tuh luti nu sik ouiyen lungse uh. Nga lukun sot pac wain keng ac wo emah uh nu sum, Ac kom ac pula sronin pomegranate sunuk uh.
Ndikanakutenga ndi kukulowetsa mʼnyumba ya amayi anga, amayi amene anandiphunzitsa, ndikanakupatsa vinyo wotsekemera kuti umwe, zotsekemera za makangadza.
3 Nga ilung lac paol lasa, Ac lac paol layot kafisyuyang nu yorol.
Mutu wanga watsamira dzanja lake lamanzere ndipo dzanja lake lamanja landikumbatira.
4 Wulema nu sik, mutan Jerusalem, Lah kowos fah tia oru kutena ma in lusrong pacl in pwar lasr uh.
Inu akazi a ku Yerusalemu, ndithu ndikukupemphani: musachigwedeze chikondi kapena kuchiutsa mpaka pamene chifunire ichocho.
5 Su mutan se fahsru yen mwesis ah me, Fungfungla ke mwet se ma el lungse yohk? Verse Lun Mutan Se Nga okaskomyak ye sak apple soko ah, Yen se ma kom tuh isusla we ah.
Kodi ndani uyo akutuluka ku chipululuyo, atatsamira wokondedwa wakeyo? Mkazi Ndinakudzutsa pa tsinde pa mtengo wa apulosi, pamenepo ndi pamene amayi anachirira, pamenepo ndi pamene wokubereka anamva ululu pokubala iweyo.
6 Kaliya insiom tuh in tia lungse kutena mwet sayuk; Nimet kom kafisya sie pacna mwet nu iniwom sayuk. Lungse uh ku, oana misa; Ac nunkeyen lungse uh fokoko oana kulyuk uh. Lungse ac ngutyak oana sie e firir Ac lalelik oana sie e lulap ma ac liksreni esukak acn uh. (Sheol h7585)
Undiyike pamtima pako ngati chidindo, ngati chidindo cha pa dzanja lako; pakuti chikondi nʼchamphamvu ngati imfa, nsanje ndiyaliwuma ngati manda. Chikondi chimachita kuti lawilawi ngati malawi a moto wamphamvu. (Sheol h7585)
7 Kof uh tia ku in fwela, Ac wangin pac sronot ku in konela. Tusruktu mwet se fin ke molela lungse ke kasrpal, Nunak in sufan mukefanna pa el ac eis kac uh.
Madzi ochuluka sangachizimitse chikondi, mitsinje singachikokolole chikondicho. Ngati wina apereka chuma chonse cha mʼnyumba mwake chifukwa cha chikondi, adzangonyozeka nazo kotheratu.
8 Oasr tamtael fusr se wiasr, Ac srakna srik tetel. Mea kut ac oru nu sel Fin oasr mukul ke payuk sel?
Ife tili naye mlongo wathu wamngʼono, koma alibe mawere, kodi tidzamuchitira chiyani mlongo wathuyu pa tsiku limene adzamufunsire?
9 El fin oana sie pot Na kut ac musaela sie tower silver fac. Ac el fin oana sie srungul Na kut ac fah nawella ke sak cedar.
Ngati iye ndi khoma, tidzamumangira nsanja ya siliva. Ngati iye ndi chitseko, tidzamutchinga ndi matabwa a mkungudza.
10 Pot soko pa nga, Ac titi luk uh pa tower kac. Mukul se nga lungse uh etu lah ke nga welul uh Nga konauk insewowo ac misla.
Ine ndili ngati khoma, ndipo mawere anga ndi nsanja zake. Tsono mʼmaso mwa bwenzi langa ndine wobweretsa mtendere.
11 Oasr ima in grape se lal Solomon In acn se pangpang Baal Hamon. Oasr mwet ima ma orekmakin acn sac, Ac kais sie selos moli nu sel ke sie tausin ipin mani silver.
Solomoni anali ndi munda wampesa ku Baala-Hamoni; iyeyo anabwereketsa munda wamphesawo kwa alimi, aliyense mwa iwo ankayenera kupereka ndalama zasiliva 1,000 mʼmalo mwa zipatso zake.
12 Solomon, eis ipin silver tausin lom an, Ac sang luofoko nu sin mwet ima uh. A funu nga, oasr ima in grape luk sefacna!
Koma munda wanga wampesa ndi wangawanga ndiponso wa ine ndekha. Iwe Solomoni, khala nazo ndalama zasiliva 1,000 ndipo ndalama zasiliva 200 ndi za amene akusamalira mundawo.
13 Mutan saok sik, lela nga in lohng pusrem inima uh me, Mwet kawuk luk elos soano in lohng ke kom ac kaskas.
Iwe amene umakhala mʼminda uli pamodzi ndi anzako, ndilole kuti ndimve liwu lako!
14 Kuiyuk, yume nu yuruk oana soko gazelle, Oana soko deer mukul fusr fineol uh, yen mahsrik keng uh kap we.
Fulumira wokondedwa wanga, ndipo ukhale ngati gwape kapena mwana wa mbawala wothamanga mʼmapiri mʼmene mumamera mbewu zokometsera chakudya.

< On Lal Solomon 8 >