< On Lal Solomon 6 >

1 Kom su kato oemeet inmasrlon mutan uh, Mukul se kom lungse ingan som nu oya? Fahkma nu sesr lah el fahsr nu ya, Kut in mau ku in kasrekom sokolak.
Iwe wokongola kuposa akazi onsewa, kodi wokondedwa wakoyo wapita kuti? Kodi wokondedwa wakoyo wakhotera njira iti kuti timufunefune pamodzi ndi iwe?
2 Kuiyuk el som nu ke ima lal, Yen sak keng uh kapak we. El som kite un sheep natul in ima sac, Ac kinkin ros kiuf.
Wachikondi wanga watsikira ku munda kwake, ku timinda ta zokometsera zakudya, akukadyetsa ziweto zake ku minda, ndiponso akuthyola maluwa okongola.
3 Mukul se nga lungse inge ma na luk, ac nga ma na lal. El mukena kite un kosro natul inmasrlon ros kiuf uh.
Wokondedwa wangayo ndine wake ndipo iyeyo ndi wangawanga; amadyetsa ziweto zake pakati pa maluwa okongola.
4 Mutan saok sik, kom arulana oasku oana acn Jerusalem, Kom kato oana siti fulat Tirzah, Oaskuiyom mwe kaksak ac arulana insewowo in liyeyuk.
Ndiwe wokongola, bwenzi langa, ngati Tiriza, wokongola kwambiri ngati Yerusalemu, ndiwe woopsa ngati gulu lankhondo lonyamula mbendera.
5 Furokla motom likiyu; Ngetma lom an oru nga kofla in oru kutena ma. Aunsifom sroalsroal ac srosro oana un nani uh Ke ac putati fineol Gilead me.
Usandipenyetsetse; pakuti maso ako amanditenga mtima. Tsitsi lako lili ngati gulu la mbuzi zikutsetsereka kuchokera ku Giliyadi.
6 Wihsum fasrfasr oana sheep Ma tufahna kalkulla ac owola. Tia soko selos fulukla; Nufonna arulana fas, ac kais soko oasr lainya.
Mano ako ali ngati gulu la nkhosa zimene zikubwera kuchokera kokazisambitsa, iliyonse ili ndi ana amapasa, palibe imene ili yokha.
7 Likintupom srusrsrusrame ye nuknuk minini lisringyen motom an.
Kukhalira kumbuyo kwa nsalu yako yophimba kumutu, masaya ako ali ngati mabandu a makangadza.
8 Mansis finne oasr kasra onngoul ac mutan kulansap oalngoul kial tokosra, Wi mutan fusr puspis saya su tia ku in oekyukla.
Ngakhale patakhala akazi a mfumu 60, ndi azikazi 80, ndi anamwali osawerengeka;
9 Tusruktu mutan sefanna pa nga lungse uh, El arulana wo ac kato, oana sie wuleoa. El mutan sefanna nutin nina kial uh, Ac nina kial el kuloel. Mutan nukewa liyal ac kaksakunul; Kasra ac mutan kulansap kien tokosra elos yuk on in kaksak kacl.
koma nkhunda yanga, wangwiro wanga ndi wosiyana ndi wina aliyense; mwana wamkazi yekhayo wa amayi ake, mwana wapamtima wa amene anamubereka. Anamwali anamuona ndipo anamutcha wodala; akazi a mfumu ndi azikazi anamutamanda.
10 Su mutan se inge, ku ngetngeta uh oana kalmen lotu uh? El arulana oasku ac saromrom, Ac srekuti oana faht uh ku malem uh.
Ndani uyu akuoneka ngati mʼbandakucha, wokongola ngati mwezi, wowala ngati dzuwa, wochititsa mantha ngati gulu la ankhondo mbendera zili mʼmanja?
11 Nga oatula inmasrlon sak almond uh In tuh liye sak fusr ma kap infahlfal uh, Ac liye sra sasu ke mah orak uh, Ac ros ma farengelik ke sak pomegranate.
Ndinatsikira ku munda wa mitengo ya alimondi kukayangʼana zomera zatsopano ku chigwa, kukaona ngati mpesa waphukira kapena ngati makangadza ali ndi maluwa.
12 Nga rrarakkom oru nga tufalak ke lungse luk uh, Oana sie mwet utuk chariot ke el ac rarala nu ke mweun uh.
Ndisanazindikire kanthu, ndinakhala ngati ndikulota kuti ndili mʼgaleta pambali pa mfumu yanga.
13 Mutan fusr Shulam se ingan, foloko, foloko, Tuh nga in ku in tuni kom. Verse Lun Mutan Se Efu ku kom lungse tuniyu Ke nga tacn inmasrlon mwet su takla tacn inge?
Bwerera, bwerera iwe namwali wa ku Sulami; bwerera, bwerera kuti ife tidzakupenyetsetse iwe! Mwamuna Chifukwa chiyani mukufuna kudzapenyetsetsa ine mwana wamkazi wa ku Sulami, pamene ndikuvina pakati pa magulu awiri?

< On Lal Solomon 6 >