< Psalm 85 >

1 [Psalm Lun Tulik Natul Korah] LEUM GOD, kom pakoten nu sin facl sum; Kom oru tuh Israel in sifilpa kapkapak.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la ana a Kora. Yehova munakomera mtima dziko lanu; munabwezeretsa ulemerero wa Yakobo.
2 Kom nunak munas nu sin mwet lom ke ma koluk lalos Ac kom eela ma sutuu lalos nukewa.
Munakhululukira mphulupulu za anthu anu ndi kuphimba machimo awo onse. (Sela)
3 Kom sisla sulung lom nukewa lukelos Ac forla liki folak lun mulat lom.
Munayika pambali ukali wanu wonse ndi kutembenuka kuchoka ku mkwiyo wanu woopsa.
4 Sifil furokkutwot, O God, Mwet Lango lasr, Ac tulokinya sulung lom nu sesr.
Tibwezeretseninso mwakale Inu Mulungu Mpulumutsi wathu, ndipo mutichotsere mkwiyo wanu.
5 Ya kom ac mulat sesr nwe tok? Ya kasrkusrak lom ac tiana tui?
Kodi mudzatikwiyira mpaka liti? Kodi mudzapitiriza kukwiya pa mibado yathu yonse?
6 Oru tuh kut in sifil kui, Na kut su mwet lom, fah kaksakin kom.
Kodi simudzatitsitsimutsanso, kuti anthu anu asangalale mwa Inu?
7 Akkalemye nu sesr lungse kawil lom, O LEUM GOD, Kasrekut ac molikutla.
Tionetseni chikondi chanu chosatha, Inu Yehova, ndipo tipatseni chipulumutso chanu.
8 Nga porongo na ma LEUM GOD El fahk, Tuh El wulema misla nu sesr, mwet lal, Kut fin tia sifil folokla nu ke inkanek lalfon lasr meet.
Ndidzamvetsera zimene Yehova Mulungu adzanena; Iye amalonjeza mtendere kwa anthu ake, oyera mtima ake, koma musawalole kuti abwerere ku zopusa.
9 Pwayena lah El akola in molelosla nukewa su akfulatyal, Ac wolana lal, su mwe loango nu sesr, fah oanna in facl sesr.
Ndithu chipulumutso chake chili pafupi ndi iwo amene amaopa Iye, kuti ulemerero wake ukhale mʼdziko lathu.
10 Lungkulang ac oaru ac fah osun; Suwoswos ac misla ac fah asruoki.
Chikondi ndi kukhulupirika zimakumana pamodzi; chilungamo ndi mtendere zimapsompsonana.
11 Oaru lun mwet uh fah sowak liki faclu nu lucng, Ac suwoswos lun God fah ngeti inkusrao me.
Kukhulupirika kumatumphuka kuchokera ku dziko lapansi, ndipo chilungamo chimayangʼana pansi kuchokera kumwamba.
12 LEUM GOD El ac fah oru tuh kut in kapkapak, Ac facl sesr fah isus fahko wo.
Ndithu Yehova adzapereka chimene chili chabwino, ndipo dziko lathu lidzapereka zokolola zake.
13 Suwoswos fah fahsr meet liki LEUM GOD Ac akoo inkanek lal.
Wolungama amapita patsogolo pake ndi kukonza njira za mapazi ake.

< Psalm 85 >