< Psalm 63 >

1 [Psalm lal David ke el Muta Yen Mwesis in Judea] O God, kom God luk, Ac nga kena apkuran nu sum. Nga suk kom ke insiuk nufon; Ngunik malukin kom Oana sie acn paola ac pulamlamla ke sripen wangin kof we.
Salimo la Davide. Pamene anali mʼchipululu cha Yuda. Inu Mulungu, ndinu Mulungu wanga, moona mtima ine ndimakufunafunani; moyo wanga uli ndi ludzu lofuna Inu, thupi langa likulakalaka inu, mʼdziko lowuma ndi lotopetsa kumene kulibe madzi.
2 Lela tuh nga in liye kom in lohm mutal; Lela nga in liye lupan ku ac wolana lom.
Inu ndinakuonani ku malo anu opatulika ndipo ndinapenya mphamvu zanu ndi ulemerero wanu.
3 Tuh lungse kawil lom wo liki na moul lun mwet uh, Ke ma inge nga fah kaksakin kom.
Chifukwa chikondi chanu ndi choposa moyo, milomo yanga idzakulemekezani.
4 Nga fah sot kulo nu sum ke lusenna moul luk; Ac nga ac fah sralak pouk in pre nu sum.
Ndidzakutamandani masiku onse a moyo wanga, ndipo mʼdzina lanu ndidzakweza manja anga.
5 Ngunik ac fah kihp, oana sie mwet su mongo ke sie kufwa. Ac nga ac fah onkakin on engan ac kaksak nu sum.
Mudzakhutitsa moyo wanga ndi zonona. Ine ndidzakutamandani ndi mawu anthetemya.
6 Ke nga oan fin mwe oan kiuk, nga esam kom; Nga nunku keim ke fong fon,
Pa bedi panga ndimakumbukira inu; ndimaganiza za Inu nthawi yonse ya usiku.
7 Ke sripen kom mwe kasru luk in pacl nukewa. Ye lulin poum, nga on ke engan.
Chifukwa ndinu thandizo langa, ine ndimayimba mu mthunzi wa mapiko anu.
8 Nga fungwot nu sum, Ac kom karinginyu ke po ku lom.
Moyo wanga umakangamira Inu; dzanja lanu lamanja limandigwiriziza.
9 Elos su suk in uniyuwi Ac fah oatula nu infulan misa.
Iwo amene akufunafuna moyo wanga adzawonongedwa; adzatsikira kunsi kozama kwa dziko lapansi.
10 Elos ac fah misa ke mweun, Ac kosro wolf ac fah kangla manolos.
Iwo adzaperekedwa ku lupanga ndi kukhala chakudya cha ankhandwe.
11 Tokosra el ac fah engan Mweyen God El sang kutangla nu sel. Elos su oru wulela ke Inen God elos fah kaksakunul, A oalin mwet kikiap fah kauli.
Koma mfumu idzakondwera mwa Mulungu; onse amene amalumbira mʼdzina la Mulungu adzalemekeza Mulunguyo, koma pakamwa pa anthu onama padzatsekedwa.

< Psalm 63 >