< Psalm 6 >

1 [Psalm lal David] O LEUM GOD, nik kom kutongyu in mulat lom, Ku kaiyu in kasrkusrak lom.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Molingana ndi seminiti. Salimo la Davide. Inu Yehova, musandidzudzule mu mkwiyo wanu, kapena kundilanga mu ukali wanu.
2 O LEUM GOD, pakomutuk tuh nga arulana totola. Ase ku nu sik tuh nga munaslana,
Ndichitireni chifundo Inu Yehova, pakuti ndalefuka; Inu Yehova chiritseni, pakuti mafupa anga ali pa ululu waukulu.
3 Ac ngunik arulana foroti. O LEUM GOD, kom ac tupan putaka?
Moyo wanga uli pa mazunzo aakulu. Mpaka liti, Inu Yehova, mpaka liti?
4 LEUM GOD, fahsru ac moliyula; Loangeyula liki misa, ke lungkulang lom.
Tembenukani Inu Yehova, ndipo mundilanditse; pulumutseni chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika.
5 In facl sin mwet misa wangin esamyom. Wangin mwet ac kaksakin kom ingo. (Sheol h7585)
Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira; Amakutamandani ndani ali ku manda? (Sheol h7585)
6 Nga totola ke sripen asor luk; Fong nukewa mwe oan kiuk sroksrok ke sroninmutuk, Ac ilul luk uh sroksroki ke tung luk.
Ine ndatopa ndi kubuwula; usiku wonse pa bedi panga pamadzaza ndi misozi yanga; ndimanyowetsa pogona panga ndi misozi.
7 Nga koflana ngetnget wo; Mutuk fafwak Ke tungiyen orekma lun mwet lokoalok luk.
Maso anga atupa chifukwa cha chisoni; akulephera kuona chifukwa cha adani anga.
8 Fahsr likiyu, kowos mwet orekma koluk! LEUM GOD El lohng pusren tung luk;
Chokani kwa ine inu nonse amene mumachita zoyipa, pakuti Yehova wamva kulira kwanga.
9 El lipsre pusren kwafe luk, Ac El ac fah topuk pre luk.
Yehova wamva kupempha kwanga kofuna chifundo; Yehova walandira pemphero langa.
10 Mwet lokoalok luk elos ac fah pulakin mwekin lulap ke kutangyukla elos; Elos fah sa na in akfohsyeyukyak ac lillilla.
Adani anga onse adzachita manyazi ndipo adzakhala ndi mantha; adzabwerera msangamsanga mwa manyazi.

< Psalm 6 >