< Psalm 43 >

1 O God, fahkak lah wangin mwetik, Ac kasreyu ke sripa su mwet ma tia etu God elos lainyu kac; Moliyula liki mwet kikiap ac mwet koluk.
Onetsani kusalakwa kwanga Inu Mulungu; ndipo mundinenere mlandu wanga kutsutsana ndi mtundu wosapembedza; mundilanditse mʼmanja mwa achinyengo ndi anthu oyipa.
2 Kom pa God su langoeyula; Efu kom ku sisyula? Efu ku nga in keok na Ke sulallal lun mwet lokoalok luk?
Pajatu Inu Mulungu ndinu mphamvu zanga. Nʼchifukwa chiyani mwandikana ine? Nʼchifukwa chiyani ndiyenera kuyenda ndikulira, woponderezedwa ndi mdani?
3 Supwama kalem lom ac pwaye lom; Lela tuh in mwe kolyu Ac folokinyume nu Zion, fineol mutal sum, Ac nu in Tempul lom yen kom muta we.
Tumizani kuwunika kwanu ndi choonadi chanu kuti zinditsogolere; mulole kuti zindifikitse ku phiri lanu loyera, kumalo kumene inu mumakhala.
4 Na nga ac fah som nu ke loang lom, O God; Tuh engan luk tuku sum me. Nga ac fah srital ke harp nutik ac on in kaksakin kom, O God, God luk.
Ndipo ndidzapita ku guwa lansembe la Mulungu, kwa Mulungu, chimwemwe changa ndi chikondwerero changa. Ndidzakutamandani ndi zeze, Inu Mulungu wanga.
5 Efu ku nga arulana supwar? Efu ku nga arulana fohs? Nga ac filiya finsrak luk in God, Ac nga fah sifilpa kaksakunul, Mwet Lango luk ac God luk.
Nʼchifukwa chiyani uli ndi chisoni iwe moyo wanga? Nʼchifukwa chiyani wakhumudwa iwe mʼkati mwanga? Khulupirira Mulungu, pakuti ndidzamutamandabe Iye, Mpulumutsi wanga ndi Mulungu wanga.

< Psalm 43 >