< Psalm 30 >

1 [Psalm lal David, In Onkakinyuk ke Kisaiyuk Tempul] Nga kaksakin kom, LEUM GOD, mweyen kom moliyula Ac tia lela tuh mwet lokoalok luk in aksruksrukyeyu.
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba popereka Nyumba ya Mulungu. Ndidzakukwezani Yehova, chifukwa mwanditulutsa kwakuya, ndipo simunalole kuti adani anga akondwere pa ine.
2 Ke nga tung ac pang nu sum, LEUM GOD luk, Kom akkeyeyula.
Inu Yehova Mulungu wanga ndinapempha kwa Inu thandizo ndipo Inu munandichiritsa.
3 Kom sruokyuwi liki misa. Nga tufokfokla nu in luf loallana, A kom folokinyume nu ke moul. (Sheol h7585)
Inu Yehova, munanditulutsa ku manda, munandisunga kuti ndisatsalire mʼdzenje. (Sheol h7585)
4 On ac kaksakin LEUM GOD, Kowos mwet sulela lal! Esam ma El su Mutallana El oru, Ac sang kulo nu sel.
Imbirani Yehova inu anthu ake okhulupirika; tamandani dzina lake loyera.
5 Mulat lal oan ke kitin pacl na, A wo lal oan ma pahtpat. Sahp ac oasr tung ke fong, Tusruktu, engan fah sikyak ke lotutang.
Pakuti mkwiyo wake umakhala kwa kanthawi koma kukoma mtima kwake ndi kwa moyo wonse; utha kuchezera kulira usiku wonse, koma chimwemwe chimabwera mmawa.
6 Nga pula inse misla, ac fahk nu sik sifacna, “Nga fah tiana kutangyukla.”
Pamene ndinaona kuti ndili otetezedwa ndinati, “Sindidzagwedezekanso.”
7 LEUM GOD, kom arulana wo nu sik, Kom tuh karinginyume oana sie pot ku fineol uh. Na tok kom wikinkomla likiyu, Oru nga sangeng.
Inu Yehova, pamene munandikomera mtima, munachititsa phiri langa kuyima chilili; koma pamene munabisa nkhope yanu, ndinataya mtima.
8 Nga tuh pang nu sum, LEUM GOD; Nga siyuk ke kasru lom, ac fahk:
Kwa Inu Yehova ndinayitana; kwa Ambuye ndinapempha chifundo;
9 “Nga fin misa, ac mea nu sum? Nga fin som nu inkulyuk, mea ac wo nu sum kac? Ya mwet misa elos ku in kaksakin kom? Ya elos ac ku in fahkak ke lupan wo lom?
“Kodi pali phindu lanji powonongeka kwanga ngati nditsikira ku dzenje? Kodi fumbi lidzakutamandani Inu? Kodi lidzalengeza za kukhulupirika kwanu?
10 Lohngyu, LEUM GOD, ac pakomutuk! LEUM GOD, kasreyu!”
Imvani Yehova ndipo mundichitire chifundo; Yehova mukhale thandizo langa.”
11 Kom ekulla asor luk nu ke engan ac onsrosro. Kom usla supwar likiyu Ac rauniyula ke engan.
Inu munasandutsa kulira kwanga kukhala kuvina; munachotsa chiguduli changa ndi kundiveka ndi chimwemwe,
12 Ke ma inge nga fah tiana misla in kaksakin kom; Nga fah yuk on in kaksak nu sum. LEUM GOD, kom God luk; Nga fah sot kulo nu sum ma pahtpat.
kuti mtima wanga uthe kuyimbira Inu usakhale chete. Yehova Mulungu wanga, ndidzapereka kwa Inu mayamiko kwamuyaya.

< Psalm 30 >