< Psalm 2 >

1 Efu mutanfahl uh ku suk inkanek in alein? Efu ku mwet uh oru nunak lusrongten lalos?
Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu? Akonzekeranji zopanda pake anthu?
2 Tokosra lalos elos tuyak in alein, Ac mwet kol lalos tukeni pwapa in lain LEUM GOD Ac tokosra se su El sulela.
Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo; ndipo olamulira asonkhana pamodzi kulimbana ndi Ambuye ndi wodzozedwa wakeyo.
3 Elos fahk, “Lela kut in srikutla lukelos. Lela kut in srola liki koko lalos.”
Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo ndipo titaye zingwe zawo.”
4 LEUM GOD El muta inkusrao isrun Ac aksruksruki pwapa munas lalos.
Wokhala mmwamba akuseka; Ambuye akuwanyoza iwowo.
5 Na El akesmakyalos ke mulat lal, Ac aksangengyalos ke kasrkusrak lal.
Ndipo iye awadzudzula mu mkwiyo wake ndi kuwaopseza mu ukali wake, kunena kuti,
6 El fahk, “Fin Zion, eol mutal sik, Nga oakiya tari tokosra luk.”
“Ine ndakhazikitsa mfumu yanga pa Ziyoni, phiri langa loyera.”
7 Ac tokosra el fahk, “Nga fah fahkak ma LEUM GOD El sapkin. El fahk nu sik, ‘Kom wen nutik; Misenge nga papa lac tomom.
Ine ndidzalengeza zimene Yehova walamula: Iye anati kwa Ine, “Iwe ndiwe mwana wanga; lero Ine ndakhala Atate ako.
8 Siyuk, ac nga ac fah asot mutunfacl nukewa nu sum; Faclu nufon ac fah ma lom.
Tandipempha, ndipo ndidzachititsa kuti mitundu ya anthu ikhale cholowa chako; malekezero a dziko lapansi kuti akhale chuma chako.
9 Kom ac fah kunauselosla ke osra soko; Kom ac fah foklolosi nu ke ip srisrik, oana sie ahlu orek ke fohk kle.’”
Iweyo udzawalamulira ndi ndodo yaufumu yachitsulo; udzawaphwanya zidutswazidutswa ngati zowumba zadothi.”
10 Inge, kowos tokosra uh, porongo kas in sensenkakin inge. Kowos mwet kol lun faclu, lutlut ke mwe luti se inge.
Kotero, inu mafumu, chenjerani; chenjezedwani, inu olamulira a dziko lapansi.
11 Kulansupu LEUM GOD ke sangeng; Rarrar
Tumikirani Yehova mwa mantha ndi kukondwerera ulamuliro wake monjenjemera.
12 ac epasr nu sel. Kowos fin tia, na kasrkusrak lal ac fah sa in sikyak, Ac kowos ac fah misa. Insewowo elos nukewa su suk nien wikla yorol.
Mpsopsoneni mwanayo kuti angakwiye; kuti mungawonongedwe mʼnjira zanu, pakuti ukali wake utha kuuka mʼkanthawi kochepa. Odala ndi onse amene amathawira kwa Iye.

< Psalm 2 >