< Psalm 144 >

1 [Psalm lal David] Kaksakin LEUM GOD, eot ku luk! El lutiyu in anwuk, Ac akoeyu nu ke mweun.
Salimo la Davide. Atamandike Yehova Thanthwe langa, amene amaphunzitsa manja anga kuchita nkhondo; zala zanga kumenya nkhondo.
2 El eot ku luk ac mwe loeyuk luk, Nien molela luk su langoeyula, Su nga filiya lulalfongi luk se. El akpusiselye mutanfahl nu ye niuk.
Iye ndiye Mulungu wanga wachikondi ndi malo anga otetezedwa, linga langa ndi mpulumutsi wanga, chishango changa mmene ine ndimathawiramo, amene amagonjetsa mitundu ya anthu pansi panga.
3 LEUM GOD, mea mwet uh, tuh kom in akilenulos? Mwet uh ma pilasr, na kom ku lohang nu selos?
Inu Yehova, munthu nʼchiyani kuti mumamusamalira, mwana wa munthu kuti muzimuganizira?
4 Mwet uh oana polo eng se ma tuhwot tuhme; Lusen len lalos oana ohk, su sa na wanginla.
Munthu ali ngati mpweya; masiku ake ali ngati mthunzi wosakhalitsa.
5 O LEUM GOD, ikaselik kusrao ac oatume; Kahlye eol uh, ac elos fah fosryak.
Ngʼambani mayiko akumwamba, Inu Yehova, ndipo tsikani pansi; khudzani mapiri kuti atulutse utsi.
6 Supweya sarom in akfahsryelik mwet lokoalok lom; Pusrkama pisr nutum, ac oru elos in kaing.
Tumizani zingʼaningʼani ndi kubalalitsa adani; ponyani mivi yanu ndi kuwathamangitsa.
7 Asroema poum lucng me. Srukyuyak liki kof loal, ac moliyula. Moliyula liki inpoun mwetsac,
Tambasulani dzanja lanu kuchokera kumwamba; landitseni ndi kundipulumutsa, ku madzi amphamvu, mʼmanja mwa anthu achilendo,
8 Su tia fahk kas pwaye, Ac elos kaskas kikiap elos finne fulahk.
amene pakamwa pawo ndi podzala ndi mabodza, amene dzanja lawo lamanja ndi lachinyengo.
9 Nga fah onkin soko on sasu nu sum, O God, Nga fah srital ke harp ac on nu sum.
Ndidzakuyimbirani nyimbo yatsopano Inu Mulungu; ndidzakuyimbirani nyimbo pa zeze wa nsambo khumi,
10 Kom pa oru tuh tokosra in eis kutangla, Ac kom molella David, mwet kulansap lom.
kwa Iye amene amapambanitsa mafumu, amene amapulumutsa Davide mtumiki wake ku lupanga loopsa.
11 Moliyula liki mwet lokoalok sulallal luk; Moliyula liki ku lun mwetsac, Su tia fahk kas pwaye, Ac elos kaskas kikiap elos finne fulahk.
Landitseni ndi kundipulumutsa, mʼmanja mwa anthu achilendo, amene pakamwa pawo ndi podzaza ndi mabodza, amene dzanja lawo lamanja ndi lachinyengo.
12 Lela tuh wen natusr, su srakna mwet fusr, In oana sak sunasr ma kapak arulana ku. Lela tuh acn natusr in oana sru loeloes Ma tu ke sruwasrik in lohm sin tokosra.
Ndipo ana aamuna pa chinyamata chawo adzakhala ngati mbewu yosamalidwa bwino, ana athu aakazi adzakhala ngati zipilala zosemedwa bwino, zokongoletsera nyumba yaufumu.
13 Lela tuh nien fil fokin ima lasr in nwanala Ke kain in fahko nukewa. Lela tuh sheep in ima lasr In oswe tausin ac ngoul tausin.
Nkhokwe zathu zidzakhala zodzaza ndi zokolola za mtundu uliwonse. Nkhosa zathu zidzaswana miyandamiyanda pa mabusa athu.
14 Lela tuh cow natusr in isus pus Ac in wangin ma isus tuh misa. Lela tuh in wangin pusren asor ke inkanek lasr uh.
Ngʼombe zathu zidzanyamula katundu wolemera. Sipadzakhala mingʼalu pa makoma, sipadzakhalanso kupita ku ukapolo, mʼmisewu mwathu simudzakhala kulira chifukwa cha mavuto.
15 Insewowo mutunfacl se su sikyak ouinge nu selos; Aok, insewowo mutunfacl se su LEUM GOD El God lalos!
Odala anthu amene adzalandira madalitso awa; odala anthu amene Mulungu wawo ndi Yehova.

< Psalm 144 >