< Psalm 125 >

1 Elos su lulalfongi in LEUM GOD, elos oana Fineol Zion, Su koflana mukuikui, ac tia ku in mokleyuk.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni, limene silingagwedezeke koma ndi lokhala mpaka muyaya.
2 Oana ke eol uh rauneak acn Jerusalem, Ouinge LEUM GOD El rauneak mwet lal Ingela ac nwe tok.
Monga mapiri azungulira Yerusalemu, momwemonso Yehova azungulira anthu ake kuyambira tsopano mpaka muyaya.
3 Mwet koluk fah tia leumi acn sin mwet suwoswos pacl nukewa; Fin ouinge, sahp mwet suwoswos ac ku pac in oru ma koluk.
Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala pa dziko limene lapatsidwa kwa anthu olungama, kuti anthu olungamawo angachite nawonso zoyipa.
4 LEUM GOD, oru wo nu selos su oru wo, Nu selos su akos sap lom.
Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino, amene ndi olungama mtima
5 A ke kom kai mwet koluk, Kom in oayapa kaelos su fahsr liki inkanek lom. Lela tuh Israel in muta in misla!
Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota, Yehova adzawachotsa pamodzi ndi anthu ochita zoyipa. Mtendere ukhale pa Israeli.

< Psalm 125 >