< Psalm 121 >

1 [Soko On in Utyak] Nga fah ngetak nu fineol uh, Kasru luk ac fah tuku ya me?
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndikweza maso anga ku mapiri; kodi thandizo langa limachokera kuti?
2 Kasru luk tuku sin LEUM GOD me, Su orala kusrao ac faclu.
Thandizo langa limachokera kwa Yehova, wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.
3 El ac fah tia lela niom in mukuikui; El su liyekomyang fah tia motulla.
Sadzalola kuti phazi lako literereke; Iye amene amakusunga sadzawodzera.
4 Liye, El su liyaung Israel Fah tiana motul ku folosuwosla.
Taonani, Iye amene amasunga Israeli sadzawodzera kapena kugona.
5 LEUM GOD El mwet liyaung lom; LEUM GOD El mwe lul lom lac poum layot.
Yehova ndiye amene amakusunga; Yehova ndiye mthunzi wako ku dzanja lako lamanja.
6 Faht uh ac fah tia unikom ke len, Ku malem ke fong.
Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana, kapena mwezi nthawi ya usiku.
7 LEUM GOD El ac fah liyekomyang liki ma koluk nukewa, El ac fah liyaung moul lom.
Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse; adzasunga moyo wako.
8 LEUM GOD El ac fah liyaung illa lom ac ilyak lom, Ingela ac nu tok ma pahtpat.
Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako; kuyambira tsopano mpaka muyaya.

< Psalm 121 >