< Psalm 120 >
1 Ke nga muta in ongoiya, nga pang nu sin LEUM GOD A El topukyu.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga, ndipo Iye amandiyankha.
2 LEUM GOD moliyula Liki mwet kikiap a mwet kutasrik.
Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza, ndi kwa anthu achinyengo.
3 Kowos, mwet kikiap, mea God El a oru nu suwos? El a kai kowos fuka?
Kodi adzakuchitani chiyani, ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?
4 Ke sukan pisr kosro nutin sie mwet mweun, A mulut firir!
Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.
5 Ke nga muta inmasrlowos, arulana koluk oana nga in muta in acn Meshech Ku muta inmasrlon mwet Kedar.
Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki, kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!
6 Loesla pacl nga muta Inmasrlon mwet su srunga misla.
Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati pa iwo amene amadana ndi mtendere.
7 Ke pacl nga sramsram ke misla, Elos ac lungse mweun.
Ine ndine munthu wamtendere; koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.