< Psalm 100 >
1 [Soko On in Sang Kulo] Fahkak pusren engan nu sin LEUM GOD, kowos facl nukewa.
Salimo. Nyimbo yothokoza. Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
2 Kulansupu LEUM GOD ke engan, Kowos in tuku nu ye mutal ke on.
Mulambireni Yehova mosangalala; bwerani pamaso pake ndi nyimbo zachikondwerero.
3 Kowos in etu lah LEUM GOD El God. El pa orekutla, ac kut ma lal, Kut mwet srahl, ac sheep lun ima lal.
Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu. Iye ndiye amene anatipanga ndipo ife ndife ake; ndife anthu ake, nkhosa za pabusa pake.
4 Utyak nu in mutunoa sel ke kulo, Ac nu in kalkal lal ke kaksak. Sang kulo nu sel ac kaksakin Inel.
Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko ndi ku mabwalo ake ndi matamando; muyamikeni ndi kutamanda dzina lake.
5 Tuh LEUM GOD El wo, Lungkulang lal oan ma pahtpat, Ac oaru lal nu sin fwil nukewa.
Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya; kukhulupirika kwake nʼkokhazikika pa mibado ndi mibado.