< Soakas 23 >

1 Kom fin wi sie mwet fulat muta mongo, esam akwoya lah su el uh.
Ngati ukhala pansi kuti udye pamodzi ndi wolamulira, uyangʼane bwino zimene zili pamaso pako,
2 Kom finne ke mongo yohk, kom eis na lupa fal.
ngati ndiwe munthu wadyera udziletse kuti usaonetse dyera lakolo.
3 Nimet oasroasr nu ke mwe mongo yuyu el kite kom kac. Sahp el oru in mwe srike kom.
Usasirire zakudya zake, pakuti zimenezo ndi zakudya zachinyengo.
4 Kom in lalmwetmet, ac tia kemkatula in suk mwe kasrup.
Usadzitopetse wekha ndi kufuna chuma, ukhale ndi nzeru ya kudziretsa.
5 Mani lom uh ku in wanginla ke kitin pacl na — oana in oasr posohksok kac, na sohkla oana sie eagle.
Ukangoti wachipeza chumacho uwona posachedwa kuti palibepo. Chumacho chimachita ngati chamera mapiko mwadzidzidzi ndi kuwuluka kunka kumwamba ngati chiwombankhanga.
6 Nimet mongo yurin sie mwet srowohsr, ku mwel mwe mongo yuyu el oru.
Usadye chakudya cha munthu waumbombo, usalakalake zakudya zake zokoma;
7 El ac fahk mu, “Fahsru eis pac kutu mongo uh,” tusruktu el tia fahk ke inse pwaye. Nunak lal siena.
paja iye ndi munthu amene nthawi zonse amaganizira za mtengo wake ngakhale amati kwa iwe, “Idya ndi kumwa,” koma sakondweretsedwa nawe.
8 Kom ac wihtacla ma kom kangla, ac kusen eyeinse lom uh wanginla sripa.
Udzasanza zimene wadyazo ndipo mawu ako woyamikira adzapita pachabe.
9 Nimet srike in sramsram in lalmwetmet nu sin sie mwet lalfon; el tia ku in eis in nunku kac.
Usayankhule munthu wopusa akumva, pakuti adzanyoza mawu ako anzeru.
10 Nimet mokle sie masrol matu, ku eisla acn lun mwet mukaimtal.
Usasunthe mwala wa mʼmalire akalekale kapena kulowerera mʼminda ya ana amasiye,
11 LEUM GOD El ac loangelos ke ku lal, ac aolulos in sramsram lain kom.
paja Mpulumutsi wawo ndi wamphamvu; iye adzawateteza pa milandu yawo kutsutsana nawe.
12 Porongo mwet luti lom, ac sang kuiyom in lutlut.
Mtima wako uzikhala pa malangizo ndipo makutu ako azimvetsera mawu a chidziwitso.
13 Nimet alolo in kai sie tulik. Sie sringsring fal ac tia unilya,
Usaleke kumulangiza mwana; ngati umulanga ndi chikwapu sadzafa.
14 a ma ac molela moul lal. (Sheol h7585)
Ukamukwapula ndi tsatsa udzapulumutsa moyo wake. (Sheol h7585)
15 Tulik nutik, kom fin sun lalmwetmet, nga ac arulana insewowo.
Mwana wanga, ngati mtima wako ukhala wanzeru, inenso mtima wanga udzakondwera.
16 Nga ac arulana engan ke nga lohng kom fahk kas lalmwetmet.
Mtima wanga udzakondwera pamene ndidzakumva ukuyankhula zolungama.
17 Nimet sok sin mwet koluk, a kom in akfulatye LEUM GOD pacl nukewa.
Mtima wako usachite nsanje ndi anthu ochimwa, koma uziopa Yehova tsiku ndi tsiku.
18 Fin ouinge, kom ac fah sun finsrak nukewa lom.
Ndithu za mʼtsogolo zilipo ndipo chiyembekezo chakocho sichidzalephereka.
19 Tulik nutik, porongeyu. Kom in lalmwetmet ac nunak akloalya ke ouiyen moul lom.
Tamvera mwana wanga, ndipo ukhale wanzeru, mtima wako uwuyendetse mʼnjira yabwino.
20 Nimet kupasr nu sin mwet nim wain yokla ac kainmongo.
Usakhale pakati pa anthu amene amaledzera kapena pakati pa anthu amene amadya nyama mwadyera.
21 Mwet lungse nimnim ac mwet kainmongo elos ac sukasrup. Fin pwayena ma kom oru pa mongo ac motul, ac tia paht na kom nukum nuknuk mihsasa.
Paja anthu oledzera ndi adyera amadzakhala amphawi ndipo aulesi adzavala sanza.
22 Porongo papa tomom — funu tia el, kom lukun wangin. Ke pacl se nina kiom el matuoh, akkalemye srui lom nu sel.
Mvera abambo ako amene anakubala, usanyoze amayi ako pamene akalamba.
23 Pwaye, lalmwetmet, lutlut, ac etauk — ma inge kewa fal kom in moli, tusruktu kom in tia kukakunla, mweyen ma inge arulana saok.
Gula choonadi ndipo usachigulitse; ugulenso nzeru, mwambo ndiponso kumvetsa zinthu bwino.
24 Mwe insewowo nu sin sie papa tulik natul fin lalmwetmet ac moul suwohs.
Abambo a munthu wolungama ali ndi chimwemwe chachikulu; Wobala mwana wanzeru adzakondwera naye.
25 Oru ma ac akinsewowoye papa tomom ac nina kiom. Kom fin oru ouinge, nina kiom el ac arulana engan.
Abambo ndi amayi ako asangalale; amene anakubereka akondwere!
26 Wen nutik, lohang akwoya, ac lela moul luk in mwe srikasrak nu sum.
Mwana wanga, undikhulupirire ndipo maso ako apenyetsetse njira zanga.
27 Mutan kosro su eis molin kosro lalos, ac mutan koluk uh, elos sie kwasrip nu ke misa.
Paja mkazi wachiwerewere ali ngati dzenje lozama; ndipo mkazi woyendayenda ali ngati chitsime chopapatiza.
28 Elos soanekom oana mwet pisrapasr, ac oru mukul puspis in tia pwaye nu sin mutan kialos.
Amabisala ngati mbala yachifwamba, ndipo amuna amakhala osakhulupirika chifukwa cha iyeyu.
29 Su oasr ongoiya yoro? Su oasr asor yoro? Su amei ac lungse anwuk finne wangin sripa? Su srusrala atronmuta?
Ndani ali ndi tsoka? Ndani ali ndi chisoni? Ndani ali pa mkangano? Ndani ali ndi madandawulo? Ndani ali ndi zipsera zosadziwika uko zachokera? Ndani ali ndi maso ofiira?
30 Elos su muta paht ke wain uh, ac elos su kar mwe nim ku.
Ndi amene amakhalitsa pa mowa, amene amapita nalawa vinyo osakanizidwa.
31 Nimet lela wain uh in srifekomla, finne srusra ac saromrom in cup uh, ac arulana wo emah ke kom ac ukumya uh.
Usatengeke mtima ndi kufiira kwa vinyo, pamene akuwira mʼchikho pamene akumweka bwino!
32 Ke lotutang tok ah, kom ac pula mu oana soko wet pwasin el ngaliskomi.
Potsiriza pake amaluma ngati njoka, ndipo amajompha ngati mphiri.
33 Motom ac liye ma sakirik, ac nunak lom ac kaskas lom ac fah tia kalem.
Maso ako adzaona zinthu zachilendo ndipo maganizo ndi mawu ako adzakhala osokonekera.
34 Kom ac pula mu kom kalkal meoa — ikwot ikme oana ke kom muta elucng ke kwesu in oak uh.
Udzakhala ngati munthu amene ali gone pakati pa nyanja, kapena ngati munthu wogona pa msonga ya mlongoti ya ngalawa.
35 Na kom ac fahk, “Oasr mwet puokyu, nga tia pula. Oasr mwet uniyu tuh nga tiana esam. Efu ku nga kofla in tukakek? Nga enenu sie pac mwe nim ah.”
Iwe udzanena kuti, “Anandimenya, koma sindinapwetekedwe! Andimenya koma sindinamve kanthu! Kodi ndidzuka nthawi yanji? Ndiye ndifunefunenso vinyo wina.”

< Soakas 23 >