< Soakas 15 >

1 Sie top fisrasr akmisyela kasrkusrak, a sie kas toasr ac purakak kasrkusrak.
Kuyankha kofatsa kumathetsa mkwiyo, koma mawu ozaza amautsa ukali.
2 Ke mwet lalmwetmet elos kaskas, mwet uh mwel etauk. A mwet lalfon elos filakunla kas lusrongten.
Munthu wanzeru amayankhula zinthu za nzeru, koma pakamwa pa zitsiru pamatulutsa za uchitsiru.
3 LEUM GOD El liye ma orek in acn nukewa; El suiya ma nukewa kut oru — finne wo ku koluk.
Maso a Yehova ali ponseponse, amayangʼana pa oyipa ndi abwino omwe.
4 Kas kulang mwe akkeye kom, a kas toasr ac mwe akmunasye kom.
Kuyankhula kodekha kuli ngati mtengo wopatsa moyo, koma kuyankhula kopotoka kumapweteka mtima.
5 Ma lalfon se pa in pilesru kas in luti lun papa tomom; a lalmwetmet pa in porongo kas in kai lal.
Chitsiru chimanyoza mwambo wa abambo ake, koma wochenjera amasamala chidzudzulo.
6 Mwet suwoswos elos karinganang kasrpalos, a mwet koluk elos sununtei kasrpalos, na ke pacl koluk tuku, elos kwacola.
Munthu wolungama amakhala ndi chuma chambiri, zimene woyipa amapindula nazo zimamugwetsa mʼmavuto.
7 Mwet lalmwetmet akyokye etauk, a mwet lalfon elos tia.
Pakamwa pa anthu anzeru pamafalitsa nzeru; koma mitima ya zitsiru sitero.
8 LEUM GOD El insewowo ke pre lun mwet wo, a El srunga mwe kisa lun mwet koluk.
Nsembe za anthu oyipa zimamunyansa Yehova, koma amakondwera ndi pemphero la anthu owona mtima.
9 LEUM GOD El srunga inkanek lun mwet koluk, a El lungse elos su oru ma suwohs.
Ntchito za anthu oyipa zimamunyansa Yehova koma amakonda amene amafunafuna chilungamo.
10 Kom fin oru ma koluk, kom ac sun kaiyuk upa; kom ac misa kom fin tia lela in aksuwosyeyuk kom.
Amene amasiya njira yabwino adzalangidwa koopsa. Odana ndi chidzudzulo adzafa.
11 LEUM GOD El fin ku in etu ma nukewa ma oan in facl lun mwet misa, na kalem lah sie mwet el tia ku in okanla nunak lal liki God. (Sheol h7585)
Manda ndi chiwonongeko ndi zosabisika pamaso pa Yehova, nanji mitima ya anthu! (Sheol h7585)
12 Mwet inse fulat tia lungse in aksuwosyeyuk elos; elos tiana suk kas in kasru sin mwet lalmwetmet.
Wonyoza sakonda kudzudzulidwa; iye sapita kwa anthu anzeru.
13 Ke pacl mwet uh engan, elos israsr srisrik, a ke pacl elos asor, insialos toasrlana.
Mtima wokondwa umachititsa nkhope kukhala yachimwemwe, koma mtima wosweka umawawitsa moyo.
14 Mwet lalkung lungse na lutlut, a mwet sulalkung mansisna in nikin.
Mtima wa munthu wozindikira zinthu umafunafuna nzeru, koma pakamwa pa zitsiru pamadya uchitsiru wawo.
15 Mwet sukasrup elos moul in fosrnga pacl nukewa, a mwet ma insewowo, elos moul in engan pacl nukewa.
Munthu woponderezedwa masiku ake onse amakhala oyipa, koma mtima wachimwemwe umakhala pa chisangalalo nthawi zonse.
16 Wo in sukasrup ac in sangeng sin LEUM GOD, liki na in kasrup ac moul in lokoalok.
Kuli bwino kukhala ndi zinthu pangʼono nʼkumaopa Yehova, kusiyana ndi kukhala ndi chuma chambiri uli pamavuto.
17 Ac wo in mongo mahsrik yen oasr lungse we, liki na in mongo ikwa yuyu yen oasr srunga we.
Kuli bwino kudyera ndiwo zamasamba pamene pali chikondi, kusiyana ndi kudyera nyama yangʼombe yonenepa pamene pali udani.
18 Mwet mongsa elos purakak akukuin, a mwet mongfisrasr elos akmisye.
Munthu wopsa mtima msanga amayambitsa mikangano, koma munthu woleza mtima amathetsa ndewu.
19 Kom fin alsrangesr, kom ac sun ma upa yen nukewa, a kom fin suwohs, wangin mwe lokoalok ac sun kom.
Njira ya munthu waulesi ndi yowirira ndi mtengo waminga, koma njira ya munthu wolungama ili ngati msewu waukulu.
20 Sie tulik lalmwetmet el akenganye papa tumal. Sie tulik lalfon el pilesru nina kial.
Mwana wanzeru amakondweretsa abambo ake, koma mwana wopusa amanyoza amayi ake.
21 Mwet lalfon elos engankin orekma lalfon lalos, a mwet lalmwetmet elos ac oru ma suwohs.
Uchitsiru umakondweretsa munthu wopanda nzeru, koma munthu womvetsa zinthu amayenda mowongoka.
22 Kutena pwapa ma srihk kas in kasru nu kac, ac tia ku in fahla wo; enenu in oasr kas in kasru sin mwet pus, na ac fah wo saflaiya.
Popanda uphungu zolinga zako munthu zimalephereka, koma pakakhala aphungu ambiri zolinga zimatheka.
23 Mwe engan na yohk in konauk kas fal nu ke sripa se lun pacl sac!
Munthu amakondwera ndi kuyankha koyenera, ndipo mawu onena pa nthawi yake ndi okoma.
24 Mwet lalmwetmet elos fahsr ke inkanek ma utyak nu ke moul; tia ke inkanek ma oatula nu ke misa. (Sheol h7585)
Munthu wanzeru amatsata njira yopita ku moyo kuti apewe malo okhala anthu akufa. (Sheol h7585)
25 LEUM GOD El ac fah kunausla lohm sin mwet filang, a El fah loangela acn sin katinmas.
Yehova amapasula nyumba ya munthu wonyada koma amasamalira malo a mkazi wamasiye.
26 LEUM GOD El srunga nunak koluk, a El insewowo ke kas kulang.
Maganizo a anthu oyipa amamunyansa Yehova, koma mawu a anthu oyera mtima amamusangalatsa.
27 Kom fin oru ma laesla ke inkanek kutasrik, kom ac pwanma ongoiya nu fin sou lom. Nimet eis mol in eyeinse, na moul lom fah loes.
Munthu wofuna phindu mwachinyengo amavutitsa banja lake, koma wodana ndi ziphuphu adzakhala ndi moyo.
28 Mwet wo elos nunku meet liki elos topuk. Mwet koluk elos sa in topuk, a kwana orala tukulkul.
Munthu wolungama amaganizira za mmene ayankhire, koma pakamwa pa munthu woyipa pamatulutsa mawu oyipa.
29 Ke pacl mwet wo uh pre, LEUM GOD El porongo, a El ngetla lukelos su oru ma koluk.
Yehova amakhala kutali ndi anthu oyipa, koma amamva pemphero la anthu olungama.
30 Ngetnget kulang ac akenganye kom, ac pweng wo ac fah akkeyekom.
Kuwala kwa maso kumasangalatsa mtima ndipo uthenga wabwino umalimbitsa munthu.
31 Kom fin porongo pacl kaiyuk kom uh, kom lalmwetmet.
Womvera mawu a chidzudzulo amene apatsa moyo adzakhala pakati pa anthu anzeru.
32 Kom fin srunga lutlut, kom sifacna akkolukye kom. Kom fin porongo kas in kai nu sum, ac fah yokelik etauk lom.
Amene amanyoza mwambo amadzinyoza yekha, koma womvera mawu a chidzudzulo amapeza nzeru zomvetsa zinthu.
33 Sangeng sin LEUM GOD pa inkanek nu ke etauk. Kom enenu in pusisel, na fah akfulatyeyuk kom.
Kuopa Yehova kumaphunzitsa munthu nzeru, ndipo kudzichepetsa ndi ulemu chili patsogolo ndi kudzichepetsa.

< Soakas 15 >