< Oekyuk 2 >

1 LEUM GOD El fahkang oakwuk inge nu sel Moses ac Aaron.
Yehova anati kwa Mose ndi Aaroni:
2 Ke pacl mwet Israel uh aktuktuk uh, kais sie mwet fah muta ye flag lun sruf lal, ac ke mwe akul lun sou lal. Lohm nuknuk nukewa ac fah tulokyak rauneak Lohm Nuknuk Mutal.
“Aisraeli azimanga misasa yawo mozungulira tenti ya msonkhano motalikira pangʼono. Munthu aliyense amange pamene pali mbendera ya fuko lake.”
3 Elos su tulokinya nien aktuktuk selos layen kutulap, yen faht uh takak we, ac fah mwet ye flag lun u lulap lal Judah, ke kais sie u lalos. Mwet kol lun u tolu uh pa takla ten inge: Sruf Mwet Kol Pisalos Judah Nahshon wen natul Amminadab 74,600 Issachar Nethanel wen natul Zuar 54,400 Zebulun Eliab wen natul Helon 57,400 Pisa lulap: mukul siofok oalngoul onkosr tausin ac angfoko. U lulap lal Judah inge pa ac fahsr meet uh.
Kummawa, kotulukira dzuwa, magulu a msasa wa Yuda amange pamene pali mbendera yawo. Mtsogoleri wa Ayudawo ndi Naasoni mwana wa Aminadabu.
4
Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 74,600.
5
Fuko la Isakara lidzamanga pafupi ndi Yuda. Mtsogoleri wa gulu la Isakara ndi Netanieli mwana wa Zuwara.
6
Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 54,400.
7
Lotsatira lidzakhala fuko la Zebuloni. Mtsogoleri wa gulu la Zebuloni ndi Eliabu mwana wa Heloni.
8
Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 57,400.
9
Anthu onse aamuna mʼmisasa ya Yuda, chiwerengero chawo ndi 186,400 monga mwa magulu awo. Iwowo ndiwo aziyamba kusamuka.
10 Nu layen nu eir, elos su wi muta ye flag lun u lulap lal Reuben fah mutangan aktuktuk in u tolu lalos, ye koko lun mwet kol lalos inge: Sruf Mwet Kol Pisalos Reuben Elizur wen natul Shedur 46,500 Simeon Shelumiel wen natul Zurishaddai 59,300 Gad Eliasaph wen natul Deuel 45,650 Pisa lulap: mukul tausin siofok lumngaul sie ac angfoko lumngaul. U lulap lal Reuben pa ac fahsr akluo uh.
Kummwera kudzakhala magulu a msasa wa Rubeni pamene pali mbendera yawo. Mtsogoleri wa gulu la Rubeni ndi Elizuri mwana wa Sedeuri.
Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 46,500.
Fuko la Simeoni lidzamanga pafupi ndi Rubeni. Mtsogoleri wa gulu la Simeoni ndi Selumieli mwana wa Zurisadai.
Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 59,300.
Lotsatira lidzakhala fuko la Gadi. Mtsogoleri wa gulu la Gadi ndi Eliyasafu mwana wa Deuweli.
Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 45,650.
Anthu onse aamuna mu msasa wa Rubeni, chiwerengero chawo monga mwa magulu awo, ndi 151,450. Iwowo azikhala achiwiri posamuka.
17 Na, inmasrlon u lulap luo meet ac u lulap luo tok ah, mwet Levi in fahsr us Lohm Nuknuk Mutal uh. Kais sie u ac fah fahsr fal nu ke takinyen mutangalos. Elos nukewa fah fahsr in u lalos ye flag lalos.
Tsono tenti ya msonkhano ndi msasa wa Alevi zidzakhala pakati pa misasayo. Iwo adzasamuka monga momwe anamangira misasa yawo, aliyense pa malo ake pamene pali mbendera yake.
18 Nu layen nu roto, elos su wi muta ye flag lun u lulap lal Ephraim fah mutangan aktuktuk in u tolu lalos, ye koko lun mwet kol lalos inge: Sruf Mwet Kol Pisalos Ephraim Elishama wen natul Ammihud 40,500 Manasseh Gamaliel wen natul Pedahzur 32,200 Benjamin Abidan wen natul Gideoni 35,400 Pisa lulap: mukul siofok oalkosr tausin ac siofok. U lulap lal Ephraim pa ac fahsr aktolu uh.
Kumadzulo kudzakhala magulu a msasa wa Efereimu pamene pali mbendera yawo. Mtsogoleri wa Aefereimuwo ndi Elisama mwana wa Amihudi.
Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 40,500.
Fuko la Manase lidzakhala pafupi ndi Efereimu. Mtsogoleri wa Amanase ndi Gamalieli mwana wa Pedazuri.
Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 32,200.
Lotsatira lidzakhala fuko la Benjamini. Mtsogoleri wa Abenjamini ndi Abidani mwana wa Gideoni.
Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 35,400.
Anthu onse aamuna mu msasa wa Efereimu, chiwerengero chawo ndi 108,100 monga mwa magulu awo. Iwowo azikhala achitatu posamuka.
25 Nu layen nu epang, elos su wi muta ye flag lun u lulap lal Dan fah mutangan aktuktuk in u tolu lalos, ye koko lun mwet kol lalos inge: Sruf Mwet Kol Pisalos Dan Ahiezer wen natul Ammishaddai 62,700 Asher Pagiel wen natul Ochran 41,500 Naphtali Ahira wen natul Enan 53,400 Pisa lulap: mukul siofok lumngaul itkosr tausin ac onfoko. U lulap lal Dan pa ac fahsr oetok uh.
Kumpoto kudzakhala msasa wa magulu a Dani pamene pali mbendera yawo. Mtsogoleri wa Adani ndi Ahiyezeri mwana wa Amisadai.
Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 62,700.
Fuko la Aseri lidzamanga pafupi ndi iwowo. Mtsogoleri wa Aaseri ndi Pagieli mwana wa Okirani.
Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 41,500.
Lotsatira lidzakhala fuko la Nafutali. Mtsogoleri wa Anafutali ndi Ahira mwana wa Enani.
Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 53,400.
Anthu onse aamuna mu msasa wa Dani chiwerengero chawo ndi 157,600. Iwo azidzanyamuka pomaliza, ndi mbendera zawo.
32 Pa inge pisen mwet Israel nukewa ke oaoala tari kais sie u: oasr mwet onfoko tolu tausin lumfoko lumngaul.
Amenewa ndi Aisraeli monga mwa mabanja a makolo awo. Chiwerengero cha Aisraeli onse mʼmisasa chinali 603,550, mwa magulu awo.
33 Oana ke LEUM GOD El tuh sapkin nu sel Moses, mwet Levi uh tia wi oaoala lun mwet Israel uh.
Koma Alevi sanawawerenge pamodzi ndi Aisraeli enawo monga momwe Yehova analamulira Mose.
34 Mwet Israel elos oru ma nukewa oana LEUM GOD El tuh sapkin nu sel Moses. Elos mutangan aktuktuk ye flag lalos, ac ke elos mukuiyak elos fahsr fal nu ke takinyen sou lun papa tumalos.
Choncho Aisraeli anachita zonse zomwe Yehova analamulira Mose. Umo ndi momwe amamangira misasa yawo pamene panali mbendera zawo, ndipo ankasamuka monga mwa mafuko a makolo awo.

< Oekyuk 2 >