< Nahum 1 >

1 Pa inge kas ke acn Nineveh, oana ma liyeyuk in sie aruruma lal Nahum, sie mwet Elkosh.
Uthenga wonena za Ninive. Buku la masomphenya a Nahumu wa ku Elikosi.
2 LEUM GOD El sie God loloik, El kalyaelos su lainul. El foloksak nu selos ke kasrkusrak lal.
Yehova ndi Mulungu wansanje ndiponso wobwezera; Yehova amabwezera ndipo ndi waukali. Yehova amabwezera adani ake ndipo ukali wake umakhala nthawi zonse pa adani akewo.
3 LEUM GOD El tia sa in kasrkusrakak, Tusruktu El arulana ku, Ac pacl nukewa El kalyei mwet su oru ma koluk. Yen LEUM GOD El fahsr we, eng upa ac sikyak; Kutkut in ye nial orala pukunyeng uh!
Yehova sakwiya msanga koma ndi wa mphamvu yayikulu; ndipo sadzalola kuti munthu wolakwa asalangidwe. Iye amayenda mʼkamvuluvulu ndi mʼnamondwe, ndipo mitambo ndi fumbi la ku mapazi ake.
4 El sap ku nu sin meoa, ac meoa paola! El akpaoyela pac infacl uh. Ima in acn Bashan uli, Insroan fineol Carmel srusrala, Ac ros in acn Lebanon efla.
Amalamulira nyanja ndipo imawuma; amawumitsa mitsinje yonse. Zomera za ku Basani ndi Karimeli zimawuma ndipo maluwa a ku Lebanoni amafota.
5 Eol uh kusrusr ye mutun LEUM GOD, Eol srisrik uh kofelik ye mutal. Faclu usrusryak ke pacl LEUM GOD El sikla; Faclu ac mwet nukewa fac rarrar.
Mapiri amagwedera pamaso pake ndipo zitunda zimasungunuka. Dziko lapansi limanjenjemera pamaso pake, dziko lonse ndi zonse zokhala mʼmenemo.
6 Ke pacl El kasrkusrak, su ku in moulla? Su ku in moulla liki foloyak lal? El okoala fulen kasrkusrak lal; Eot uh mwesri nu ke kutkut ye mutal.
Ndani angathe kuyima pamaso pake Iye akalusa? Ndani angapirire mkwiyo wake woopsa? Ukali wake ukuyaka ngati moto; matanthwe akunyeka pamaso pake.
7 LEUM GOD El wo; El loango mwet lal in pacl in ongoiya; El karinganulos su nget nu sel.
Yehova ndi wabwino, ndiye kothawirako nthawi ya masautso. Amasamalira amene amamudalira,
8 El arulana kunausla mwet lokoalok lal oana sie sronot lulap su fungla. El supwala mwet su lainul nu infulan misa.
koma ndi madzi achigumula choopsa Iye adzawononga adani ake (Ninive); adzapirikitsira adani ake ku malo a mdima.
9 Mea kowos pwapa sulali sang lain LEUM GOD? El ac kunauskowosla. Wangin mwet ku in alein nu sel pacl luo.
Chiwembu chilichonse chimene akukonzekera kumuchitira Yehova adzachiwononga kotheratu; msautso sudzabweranso kachiwiri.
10 Kowos su lungse sruhi ac fah isisyak Oana kokul su pinpinla ac sroan mah pao.
Iwo adzakodwa mu ziyangoyango za minga ndipo adzaledzera ndi vinyo wawo; adzatenthedwa ngati ziputu zowuma.
11 Oasr sie mwet su tuku liki kom, Nineveh, sesseslana ke pwapa sulal elan oru lain LEUM GOD.
Kwa iwe, Ninive, kunachokera munthu wa cholinga choyipa, wofuna kuchitira Yehova chiwembu, amene amapereka uphungu woyipa.
12 Pa inge ma LEUM GOD El fahk nu sin mwet Israel, mwet lal: “Mwet Assyria finne ku ac pus suna, elos ac fah kunausyukla ac wanginla. Mwet luk, nga tuh akkeokye kowos meet, tusruktu nga fah tia sifilpa oru.
Yehova akuti, “Ngakhale Asiriyawo ali ndi abwenzi, kaya iwowo ndi ambiri, koma adzawonongedwa ndi kutheratu. Ngakhale ndinakuzunza iwe Yuda, sindidzakuzunzanso.
13 Inge nga fah aksafyela ku lun Assyria fowos, ac wotyalik sein ma kaprikowosi.”
Tsopano ndidzathyola goli lake pa khosi lako ndipo ndidzadula maunyolo ako.”
14 Pa inge ma LEUM GOD El wotela ke mwet Assyria: “Ac fah wangin tulik natulos in folokonak inen sou lalos. Nga fah kunausla ma sruloala su oan in tempul lun god lalos. Nga akoo sie kulyuk nu sin mwet Assyria — tia fal elos in moul!”
Yehova walamulira za iwe, Ninive kuti, “Sudzakhala ndi zidzukulu zimene zidzadziwike ndi dzina lako. Ndidzawononga zifanizo zosema ndi mafano owumba amene ali mʼnyumba ya milungu yako. Ine ndidzakukumbira manda chifukwa ndiwe woyipitsitsa.”
15 Liye, mwet roso se pa tuku fineol uh me ingo, ac use pweng wo! El fahsr in sulkakin ke kutangla! Mwet Judah, oru kufwa in akfulat lowos an, ac sang nu sin God ma kowos wulela ku mu kowos ac sang nu sel an. Mwet koluk fah tia sifilpa utyak mweuni acn lowos. Wutiyukla na pwaye elos!
Taonani, pa phiripo, mapazi a munthu amene akubweretsa nkhani yabwino, amene akulengeza za mtendere! Inu anthu a ku Yuda, chitani madyerero anu ndipo kwaniritsani malumbiro anu. Anthu oyipa sadzakuthiraninso nkhondo; iwo adzawonongedwa kotheratu.

< Nahum 1 >