< Malachi 1 >

1 Pa inge kas su LEUM GOD El sang nu sel Malachi in fahkak nu sin mwet Israel.
Uthenga: Mawu a Yehova kwa Israeli kudzera mwa Malaki.
2 LEUM GOD El fahk nu sin mwet lal, “Nga nuna lungse kowos pacl nukewa.” Tusruktu elos topuk fahk, “Kom akkalemye lungse lom nu sesr fuka?” LEUM GOD El topuk, “Esau ac Jacob eltal tamulel, tuh nga lungse Jacob ac fwil natul,
Yehova akuti, “Ine ndakukondani. Koma inu mukufunsa kuti, ‘Kodi mwatikonda motani?’” Yehova akuti, “Kodi Esau sanali mʼbale wake wa Yakobo? Komatu Ine ndinakonda Yakobo,
3 ac nga srungal Esau ac fwil natul. Nga sukela acn sel Esau ac sang fulan eol we tuh in nien muta lun kosro lemnak.”
koma ndinamuda Esau, ndipo dziko lake lamapiri ndalisandutsa chipululu ndipo cholowa chake ndasiyira ankhandwe a mʼchipululu.”
4 Mwet Edom, su fwil natul Esau, fin fahk, “Siti sesr kunausyukla, tusruktu kut ac fah sifilpa musaeak,” na LEUM GOD El fah topuk, “Lela elos in sifil musai — nga fah sifil kunausla. Ac fah pangpang elos, ‘Sie facl koluk,’ ac ‘Mutunfacl se su LEUM GOD El kasrkusrak se nwe tok!’”
Mwina Edomu nʼkunena kuti, “Ngakhale taphwanyidwa, tidzamanganso mʼmabwinja.” Koma Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Iwo angathe kumanganso, koma Ine ndidzazigwetsanso. Iwo adzatchedwa dziko loyipa, la anthu amene Yehova wayipidwa nawo mpaka muyaya.
5 Mwet Israel elos fah sifacna liye ma inge ke mutalos, ac elos ac fahk, “LEUM GOD El arulana ku, ac ku lal liyeyuk sayen facl Israel pac!”
Inu mudzaziona zimenezi ndi maso anu ndipo mudzati, ‘Yehova ndi Wamkulu, ukulu wake umafika ngakhale kunja kwa malire a Israeli!’
6 LEUM GOD Kulana El fahk nu sin mwet tol uh, “Sie wen el sunakin papa tumal, ac sie mwet kulansap el sunakin mwet kacto lal. Nga papa tomowos — efu kowos ku tia sunakinyu? Nga Mwet Kacto lowos — efu kowos ku tia akfulatyeyu? Kowos aksruksrukeyu, a kowos siyuk, ‘Kut aksruksruke kom fuka?’
“Mwana amalemekeza abambo ake, ndipo wantchito amaopa abwana ake. Ngati Ine ndine abambo anu, ulemu wanga uli kuti? Ngati ndine mbuye wanu, nanga kundiopa kuli kuti?” Akutero Yehova Wamphamvuzonse. “Ndinu, inu ansembe, amene mumanyoza dzina langa. “Komatu mukufunsa kuti, ‘Kodi timanyoza dzina lanu bwanji?’
7 Ke kowos kisakin mwe mongo kolukla fin loang luk uh. Na kowos sifil siyuk, ‘Kut tia akfulatye kom fuka?’ Nga ac fahk nu suwos: ke kowos aklusrongtenye loang luk.
“Inu mwanyoza dzina langa popereka chakudya chodetsedwa pa guwa langa lansembe. “Komatu mukufunsa kuti, ‘Kodi ife takunyozani bwanji?’ “Mwandinyoza ponena kuti tebulo la Yehova ndi lonyozeka.
8 Ke kowos use soko kosro kun ku mas ku osaksak in kisakin nu sik, ya kowos nunku mu wangin ma koluk kac? Srike sangwin soko kain kosro se ingan nu sel governor — ya el ac insewowo suwos, ku oru kutena ma in kasrekowos?”
Mukamapereka nsembe nyama zosaona, kodi sicholakwa? Mukamapereka nsembe nyama zachilema kapena zodwala, kodi sicholakwa? Kayeseni kuzipereka kwa bwanamkubwa wanu! Kodi akasangalatsidwa nanu? Kodi akazilandira? Akutero Yehova Wamphamvuzonse.
9 Inge, kowos mwet tol, srike siyuk sin God Elan oru wo nu sesr. El ac tia topuk pre lowos uh, na ac fah ma lowos pa koluk uh.
“Tsopano tayesani kupempha Mulungu kuti akuchitireni chifundo. Kodi ndi zopereka zotere mʼmanja mwanu, Iye angakulandireni?” Akutero Yehova Wamphamvuzonse.
10 LEUM GOD Kulana El fahk, “Nga ke sie suwos in kaliya srungul ke Tempul, in kosrala kowos in tia akosak e fin loang luk uh ke wangin sripa. Nga tiana insewowo suwos. Nga fah tia eis mwe sang ma kowos us nu yuruk.
“Ndikulakalaka mmodzi wa inu akanatseka zitseko za Nyumba ya Mulungu, kuti musayatsemo moto pachabe pa guwa langa lansembe! Ine sindikukondwera nanu,” akutero Yehova Wamphamvuzonse, “ndipo Ine sindidzalandira zopereka za mʼmanja mwanu.
11 Ke pacl faht uh takak nwe ke pacl faht uh tili, mwet in mutunfacl nukema faclu elos sunakinyu. Yen nukewa elos esukak mwe keng ac ase mwe kisa wowo nu sik. Elos nukewa akfulatyeyu!
Dzina langa lidzalemekezedwa pakati pa mitundu ya anthu, kuchokera kummawa mpaka kumadzulo. Mʼmalo monse adzapereka nsembe zofukiza ndi zopereka zangwiro mʼdzina langa, chifukwa dzina langa lidzakhala lalikulu pakati pa mitundu ya anthu,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
12 Tusruktu kowos akkolukye loang luk ke kowos fahk mu wangin sripa, ac ke kowos kisakin mwe mongo koluk fac.
“Koma inu mumalinyoza ponena kuti tebulo la Ambuye, ‘ndi lodetsedwa,’ ndipo chakudya chake, ‘nʼchonyozeka!’
13 Kowos fahk mu, ‘Kut totola ke oreyen ma inge uh!’ ac sungalik infwewos nu sik. Kowos use kosro pusrla, ku ma osaksak, ku mas, in kisakin nu sik. Ya kowos nunku mu nga ac eis ma ingan suwos?
Ndipo inu mumati, ‘Ndi zotopetsa zimenezi!’ Ndipo mumandinyogodola Ine,” akutero Yehova Wamphamvuzonse. “Pamene inu mubweretsa nyama zakuba, zolumala kapena zodwala ndi kupereka nsembe, kodi Ine ndizilandire kuchokera mʼmanja mwanu?” Akutero Yehova.
14 In selngawiyuk mwet kutasrik se su kisakin soko kosro koluk lumah nu sik, ke oasr ma na wo ac fas soko inmasrlon un kosro natul, su el tuh wulema in kisakin nu sik! Tuh nga sie tokosra fulat, ac mwet in mutunfacl nukewa sangeng sik.”
“Atembereredwe munthu wachinyengo amene ali ndi nyama yayimuna yabwino mʼgulu la ziweto zake ndipo analumbira kuyipereka, koma mʼmalo mwake nʼkupereka nsembe kwa Ambuye nyama yosayenera. Yehova Wamphamvuzonse akuti, ‘Pakuti ndine mfumu yayikulu, dzina langa liyenera kuopedwa pakati pa anthu a mitundu yonse.’”

< Malachi 1 >