< Mwet Nununku 15 >

1 Tok kutu, ke pacl in kosrani lun wheat, Samson el us nani fusr soko ac som in osun nu sin mutan kial ah. El fahk nu sin papa talupal, “Nga lungse utyak nu ke infukil lun mutan kiuk ah.” Tusruktu papa sac tia lela.
Patapita nthawi, mu nyengo yodula tirigu, Samsoni anatenga kamwana kambuzi ndipo anapita kukacheza kwa mkazi wake. Iye anati, “Ndikufuna kukalowa ku chipinda cha mkazi wanga.” Koma abambo a mkaziyo anamuletsa kutero.
2 El fahk nu sel Samson, “Nga pangon kom srungalla na pwaye, oru nga eisalang nu sin kawuk se lom ah. Tusruktu tamtael fusr se wial inge el kato lukel. Kom ku in eisal elan aolulla.”
Abambo a mkaziyo anati, “Ine ndimaganiza kuti umamuda kwambiri nʼchifukwa chake ndinamupereka kwa mnzako. Kodi mngʼono wake uja sindiye wokongola kupambana iye? Ingotengani ameneyo mʼmalo mwake.”
3 Na Samson el fahk, “Inge, nga finne oru kutu ma upa nu sin mwet Philistia, ac fah wangin mwetik kac.”
Samsoni anawawuza kuti, “Pano sindikhala wochimwa ndikawachita choyipa chachikulu Afilistiwa.”
4 Na el som ac sruokya kosro fox tolfoko ac kapriya pulalos kais lukwa, ac sang kahp in e nu kac.
Choncho Samsoni anapita nakagwira nkhandwe 300 nazimangirira michira ziwiriziwiri ndipo pa fundo iliyonse ya michirayo anamangirira nsakali.
5 Na el akosak kahp inge ac fuhlelosla in ima in wheat lun mwet Philistia ah. Ouinge wheat ma elos kosrani tari ac wheat ma srakna kapak in ima ah, firiryak nufon, oayapa sak olive wi pac folla.
Anayatsa nsakalizo kenaka ndi kuzitayira nkhandwe zija mʼminda ya tirigu ya Afilisti, ndipo zinatentha milu ya tirigu, ndi wosadula yemwe pamodzi ndi mitengo ya mpesa ndi ya olivi.
6 Ke mwet Philistia elos siyuk lah su oru ma inge, na fwackyang nu selos lah Samson pa oru uh, mweyen papa talupal el tuh eisalang mutan kial Samson nu sin kawuk se lal Samson ah. Ouinge mwet Philistia elos som ac esukak lohm sin papa sac, na mutan sac ac sou lal nufon misa.
Tsono Afilisti anayamba kufunsana kuti, “Ndani wachita izi?” Ena anati, “Ndi Samsoni mkamwini wa munthu wa ku Timna uja chifukwa Mtimunayo anatenga mkazi wake ndi kumupereka kwa mnzake.” Choncho Afilisti anapita kukatentha mtsikanayo pamodzi ndi abambo ake.
7 Samson el fahk nu selos, “Fin pa inge orekma lowos uh, nga fulahk lah nga fah tiana tui nwe ke na nga aksafyela foloksak luk nu suwos!”
Samsoni anawawuza kuti, “Ngati mumachita zangati zimenezi, ndiye ine sindileka mpaka nditakulipsirani.”
8 El oru sie mweun na upa, ac onela mwet puspis selos. Na el som ac muta in luf se ke eot fulat in Etam.
Choncho Samsoni anamenyana nawo koopsa ndipo anapha ambiri a iwo. Kenaka anakalowa mʼphanga la Etamu, nakhala momwemo.
9 Mwet Philistia elos tuku ac tulokunak lohm nuknuk selos in acn Judah, ac elos mweuni acn Lehi.
Pambuyo pake Afilisti anakamanga misasa ya nkhondo mʼdziko la Yuda, ndi kuthira nkhondo mʼdera la Lehi.
10 Mwet Judah elos siyuk selos, “Efu ku kowos tuku mweuni kut?” Na elos fahk, “Kut tuku in sruokilya Samson in folokin nu sel ma el oru nu sesr.”
Anthu a fuko la Yuda anafunsa kuti, “Nʼchifukwa chiyani mwabwera kudzamenyana nafe?” Iwo anayankha kuti, “Tabwera kudzamanga Samsoni ndi kuti timuchite zofanana ndi zimene anatichita.”
11 Na tausin tolu sin mwet Judah inge som nu ke luf se ke eot fulat in Etam ac fahk nu sel Samson, “Ya kom nikin lah mwet Philistia elos pa leum facsr uh— Mea se kom oru nu sesr inge?” Na el topuk ac fahk nu selos, “Ma na elos oru nu sik ah pa nga oru oapana nu selos.”
Ndipo anthu 3,000 a ku Yuda anapita ku phanga la Etamu, ndi kukamufunsa Samsoni kuti, “Kodi iwe sudziwa kuti ife amatilamulira ndi Afilisti? Tsono ndi chiyani chimene watichitachi?” Iye anayankha kuti, “Ine ndinachita zomwe iwo anandichita.”
12 Na elos fahk nu sel, “Kut tuku in kaprikomi tuh kut in eiskomyang nu inpaolos.” Na Samson el fahk, “Fulahk nu sik lah kowos ac tia sifacna uniyuwi.”
Iwo anati kwa iye, “Ife tabwera kuti tikumange ndi kukupereka kwa Afilisti.” Ndipo Samsoni anati, “Lonjezani mwa lumbiro kuti simundipha ndinu.”
13 Na elos fahk, “Aok, kut ac tia unikomi. Kut ac kaprikomi na, ac eiskomyang nu selos.” Ouinge elos kaprilya ke sucl sasu lukwa ac pwanulak liki eot fulat sac.
Iwo anamuyankha kuti, “Ayi, ife sitikupha. Koma tingokumanga ndi kukupereka mʼmanja mwa Afilisti.” Choncho anamumanga ndi zingwe ziwiri zatsopano namutulutsa mʼphanga muja.
14 Ke el sun acn Lehi, mwet Philistia elos sasa ac kasrusr tuku nu yorol. In kitin pacl ah na, ku lun LEUM GOD putati nu facl, ac el wotyalik sucl ma kapriya paol oana luman turet ma firirla tari, ac mwe kapir putatla liki paol.
Samsoni anafika ku Lehi, ndipo Afilisti anamuchingamira akufuwula. Nthawi yomweyo Mzimu wa Yehova unatsika pa iye mwamphamvu ndipo zingwe zimene anamumanga nazo zinasanduka ngati thonje lopsa mʼmoto, zinachita ngati zasungunuka nʼkuchoka mʼmanja mwake.
15 Na el konauk srin oalin donkey soko ma tufahna misa, ac el srukak ac sang onela sie tausin mwet kac.
Anapeza chibwano cha bulu amene anali atangofa kumene. Anachitola ndi kuphera nacho anthu 1,000.
16 Na Samson el on ac fahk, “Ke srin oalin donkey soko, nga uniya sie tausin mwet; Ke srin oalin donkey soko, nga elosak yolin mwet.”
Ndipo Samsoni anati, “Ndi chibwano cha bulu, milu ndi milu ya anthu. Ndi chibwano cha bulu, ndapha anthu 1,000.”
17 Tukun ma inge, el sisla sri soko ah, na pangpang acn se ma inge sikyak we ah Ramath Lehi.
Atatsiriza kuyankhula, anataya chibwanocho, ndipo malowo anawatcha Ramati-Lehi.
18 Na Samson el arulana malu, ouinge el pang nu sin LEUM GOD ac fahk, “Kom ase kutangla na lulap se inge nu sik. Ya pwaye nga ac misa ke sripen malu, ac putatyang nu inpoun mwet pegan?”
Pambuyo pake anamva ludzu kwambiri ndipo anayitana Yehova mopempha kuti, “Inu mwapatsa mtumiki wanu chipulumutso chachikulu chotere. Kodi tsopano ndife ndi ludzu ndi kugwidwa ndi anthu osachita mdulidwewa?”
19 Na God El ikaselik sie acn oalal infohk uh in acn Lehi, ac kof unonak kac me. Ke Samson el nimkofi ngunal folokyang, na el sifilpa kui. Ouinge unon in kof se inge pangpang En-Hakkore, ac srakna oasr in acn Lehi nwe misenge.
Pamenepo Mulungu anangʼamba nthaka ku Lehi, ndipo madzi anatuluka mʼdzenjemo. Samsoni anamwa madziwo, ndipo mphamvu zake zinabwerera nakhalanso monga analili. Choncho chitsimecho chinatchedwa Eni-Hakore, ndipo chilipobe ku Lehiko mpaka lero.
20 Samson el tuh nununku mwet Israel yac longoul, ke pacl se mwet Israel elos muta ye poun mwet Philistia.
Samsoni anatsogolera Israeli pa nthawi ya Afilisti kwa zaka makumi awiri.

< Mwet Nununku 15 >