< Joshua 17 >

1 Sie ipin acn roto in Infacl Jordan tuh itukyang nu sin kutu sou in sruf lal Manasseh, su tulik se oemeet natul Joseph. Na Machir, papa tumal Gilead, el wen se oemeet natul Manasseh ac el mwet pwengpeng ke mweun se, pa sis acn Gilead ac Bashan su oan kutulap in Infacl Jordan itukyang lal.
Gawo lina la dzikolo linapatsidwa kwa mabanja ena a fuko la Manase, mwana woyamba kubadwa wa Yosefe. Makiri anali mwana woyamba kubadwa wa Manase ndiponso kholo la anthu okhala ku Giliyadi. Popeza kuti iye anali munthu wankhondo, analandira Giliyadi ndi Basani.
2 Acn roto in Infacl Jordan itukyang nu sin sou lula lal Manasseh: Abiezer, Helek, Asriel, Shechem, Hepher, ac Shemida. Pa inge mukul lula natul Manasseh wen natul Joseph, ac elos sifen kais sie sou.
Mabanja ena otsala a fuko la Manase amene analandira dziko ndi awa: Abiezeri, Heleki, Asirieli, Sekemu, Heferi ndi Semida. Izi ndi zidzukulu zina zazimuna za Manase mwana wa Yosefe ndiponso eni mbumba.
3 Na Zelophehad, su ma natul Hepher, natul Gilead, natul Machir, natul Manasseh, wangin mukul natul — mutan mukena, ac inelos pa Mahlah, Noah, Hoglah, Milcah, ac Tirzah.
Panali Zelofehadi mwana wa Heferi, mwana wa Giliyadi, mwana wa Makiri mwana wa Manase. Iyeyu analibe ana aamuna koma aakazi okhaokha ndipo mayina awo ndi awa: Mahila, Nowa, Hogila, Milika ndi Tiriza.
4 Elos som nu yorol Eleazar mwet tol, ac nu yorol Joshua wen natul Nun, ac nu yurin mwet kol ac fahk, “LEUM GOD El tuh sapkin nu sel Moses elan ase ipin acn lasr in oapana ke mukul wiasr inge eis acn lalos.” Na elos sang acn sin mutan inge, in oana ma LEUM GOD El sapkin.
Iwo anapita kwa Eliezara wansembe, Yoswa mwana wa Nuni, ndi atsogoleri ndipo anati: “Yehova analamula Mose kuti ife ndi alongo athu atipatse cholowa chathu.” Choncho iwowo pamodzi ndi abale a abambo awo anawapatsa dera lina la dzikolo kuti likhale monga mwa lamulo la Yehova.
5 Pa inge sripa se sis tuh oasr pac ip singoul itukyang nu sin Manasseh in weang acn Gilead ac Bashan su oan kutulap in Infacl Jordan,
Choncho kuwonjezera pa mayiko a Giliyadi ndi Basani kummawa kwa Yorodani, anthu a fuko la Manase analandiranso magawo khumi
6 mweyen itukyang acn sin mukul oayapa mutan natul Manasseh. Acn Gilead itukyang nu sin mwet lula nukewa in sruf lal Manasseh.
chifukwa ana aakazi a fuko la Manase analandira cholowa chawo pakati pa ana aamuna. Dziko la Giliyadi linali dziko la zidzukulu zonse za Manase.
7 Facl sel Manasseh pa som Asher lac nwe sun acn Michmethath, kutulap in acn Shechem. Na masrol sac fahla eir lac nu ke acn lun mwet Entappuah.
Malire a dziko la Manase anayambira ku Aseri, ndipo anakafika ku Mikimetati kummawa kwa Sekemu. Tsono malire anapita kummwera kuloza kwa anthu a ku Eni-Tapuwa.
8 Acn ma raunela siti Tappuah ma lal Manasseh, tusruktu siti se inge Tappuah ma oan fin masrol an, ma lun tulik natul Ephraim.
(Manase anatenga dziko la Tapuwa, koma mzinda wa Tapuwawo, umene unali mʼmalire mwa Manase unali wa fuko la Efereimu).
9 Na masrol an putati som nwe ke infacl srisrik Kanah. Siti nukewa ma oan eir in infacl srisrik soko ah ma lun tulik natul Ephraim, finne siti inge oan in facl lal Manasseh. Masrol lal Manasseh uh fahla epang sisken infacl srisrik soko ah nwe safla Meoa Mediterranean.
Ndipo malire ake anapitirira kummwera mpaka ku mtsinje wa ku Kana. Mizinda ya kummwera kwa mtsinjewo inali ya fuko la Efereimu ngakhale kuti inali mʼdziko la Manase. Malire a fuko la Manase anapita kumpoto kwa mtsinje wa Kana ndi kukathera ku Nyanja.
10 Acn eir ma lal Ephraim, ac acn epang ma lal Manasseh, ac masrol lalos nu roto pa Meoa Mediterranean. Ac masrol nu roto epang ke acn lal Manasseh sun acn lal Asher, ac masrol nu kuta epang ke acn lal Manasseh sun acn lal Issachar.
Dziko la kummwera linali la Efereimu ndipo la kumpoto linali la Manase. Dziko la Manase linafika ku nyanja ndipo linachita malire ndi Aseri, kumpoto ndiponso Isakara, kummawa.
11 Luin acn sel Issachar ac Asher, acn ekasr inge oan loac, tuh ma lal Manasseh: Beth Shan ac Ibleam ac inkul nukewa ma raunela, oayapa acn Dor (su oan sisken Meoa Mediterranean), Endor, Taanach, Megiddo, ac inkul nukewa ma raunela.
Mʼdziko la Isakara ndi Aseri, Manase analinso ndi mizinda ya Beti-Seani ndi Ibuleamu pamodzi ndi midzi yawo yozungulira. Panalinso Akanaani amene ankakhala ku Dori, Endori, Taanaki ndi Megido pamodzi ndi mizinda yozungulira (wachitatu pa mʼndandandawu ndi Nafati Dori).
12 Tusruktu, mwet Manasseh elos koflana lusak mwet in siti ingo, oru mwet Canaan elos mutana we.
Komabe anthu a fuko la Manase sanathe kuwapirikitsa anthu okhala mʼmizinda imeneyi. Choncho Akanaani anakhalabe mʼmizindayi.
13 Finne pacl se ma mwet Israel elos arulana kui, elos tiana luselosla, tusruktu elos sang orekma upa nu faclos.
Ngakhale Aisraeli anali a mphamvu mʼdzikomo, sanapirikitse Akanaani onse koma anangowasandutsa kukhala akapolo.
14 Na tulik natul Joseph fahk nu sel Joshua, “Efu kom ku ase ipin acn sefanna tuh in ma lasr? Kut arulana pus, mweyen LEUM GOD El akinsewowoye kut.”
Anthu a fuko la Yosefe anati kwa Yoswa, “Chifukwa chiyani mwatipatsa gawo limodzi lokha la dziko kuti likhale cholowa chathu? Ife tilipo anthu ambiri popeza Yehova watidalitsa kwambiri.”
15 Ac Joshua el fahk nu selos, “Kowos fin arulana pus, ac fineol Ephraim fin srikla nu suwos, na kowos utyak nu insak uh ac sifacna sakunla nu suwos kutu acn sin mwet Periz ac mwet Rephaim.”
Yoswa anayankha kuti, “Ngati muli ambiri ndipo dziko la ku mapiri la Efereimu lakucheperani kwambiri, lowani ku nkhalango mudule mitengo, mudzikonzere malo akuti mukhalemo, mʼdziko la Aperezi ndi Arefai.”
16 Ac elos topuk, “Facl sesr fineol uh tia fal nu sesr, tuh mwet Canaan su muta acn tupasrpasr uh oasr chariot osra natulos, kewana elos su muta Beth Shan ac elos su muta Infahlfal Jezreel ac acn nukewa ma raunela acn ingan.”
Tsono zidzukulu za Yosefe zinati, “Dziko la ku mapiri ndi losatikwaniradi, komanso Akanaani onse amene akukhala ku chigwa pamodzi ndi amene akukhala ku Beti-Seani ndi madera awo ndiponso amene ali ku chigwa cha Yezireeli ali ndi magaleta azitsulo.”
17 Joshua el fahk nu sin sruf lal Ephraim ac Manasseh Roto, “Pwaye kowos arulana pus ac ku. Fal in pus liki ipin acn se na lowos.
Koma Yoswa anawuza zidzukulu za Yosefe, za fuko la Efereimu ndi za fuko la Manase kuti, “Inu mulipodi ambiri ndiponso amphamvu. Simulandira gawo limodzi lokha,
18 Fineol uh ma lowos. Finne acn ingan insak, kowos ac fah sakunla ac fah ma lowos nufon. Ac nu ke mwet Canaan an, kowos ac fah luselosla, elos finne mwet ku ac oasr chariot osra natulos.”
dziko la ku mapiri lidzakhalanso lanu. Ngakhale kuti ndi nkhalango yokhayokha koma inu mudzadula mitengo yake ndipo lidzakhala lanu mpaka kumapeto. Ngakhale kuti Akanaani ali ndi magaleta azitsulo ndiponso kuti iwo ndi amphamvu, koma inu mudzawapirikitsa.”

< Joshua 17 >