< Job 35 >

1 Na Elihu el sifilpa fahk:
Ndipo Elihu anawonjeza kunena kuti,
2 “Ku kom nunku mu ma se inge suwohs Ke kom fahk mu, ‘Nga suwohs ye mutun God.’
“Kodi mukuganiza kuti mukukhoza? Mukunena kuti, ‘Ndine wolungama pamaso pa Mulungu.’
3 Ku ke kom siyuk sin God, ‘Nga fin tia oru ma koluk, mea ac wo nu sik?’
Komanso inu mukufunsa kuti, ‘Kodi phindu langa nʼchiyani, ndipo ndimapeza chiyani ndikapanda kuchimwa?’
4 Nga ac topuk kom, ac mwet kawuk lom ingan pac.
“Ine ndikufuna ndikuyankheni inu pamodzi ndi abwenzi anu omwe.
5 “Ngetak liye acn lucng! Liye fulatiyen pukunyeng uh!
Yangʼanani kumwamba ndipo muone mitambo imene ili kutali ndi inuyo.
6 Kom fin orekma koluk, God El tiana akkolukyeyuk kac. Kom fin oru ma koluk pacl pus, ya ma inge ac aklokoalokyal?
Inuyo mukachimwa, Iye zimamukhudza motani? Ngati machimo anu ndi ochuluka, zimenezo zimachita chiyani kwa Iye?
7 Ya kom kasru God kom fin arulana orek suwohs? Wangin ma God El enenu sum.
Ngati inu ndinu wolungama, mumamupatsa Iyeyo chiyani? Kapena Iye amalandira chiyani chochokera mʼdzanja lanu?
8 Mwet uh pa ac keok ke ma koluk kom oru uh, Ac ma wo kom oru uh ac kasru pac mwet.
Kuyipa kwanu kumangokhudza anthu ngati inuyo, ndipo chilungamo chanu chimakhudza anthu anzanu.
9 “Ke akkeokyeyuk mwet uh, elos ac sasao; Ac elos pang tuh in oasr mwet kasrelos.
“Anthu akufuwula chifukwa cha kuzunzidwa; akufuna chithandizo kuti achoke pansi pa ulamuliro wa anthu amphamvu.
10 Tuh elos tia ngetang nu sin God su oralosla, Su sang soko on in finsrak nu selos ke pacl upa nu selos.
Koma palibe amene akunena kuti, ‘Kodi ali kuti Mulungu, Mlengi wanga, amene amatisangalatsa nthawi ya usiku,
11 Elos tia nget nu sin God su ase etauk nu sesr, Etauk liki kutena kosro, ku won.
amene amatiphunzitsa kupambana nyama za dziko lapansi ndipo amatipatsa nzeru kupambana mbalame zowuluka?’
12 Elos pang in suk kasru, tuh God El tiana topkolos, Mweyen elos mwet koluk ac inse fulat.
Iye sayankha pamene anthu akufuwulira kwa Iye chifukwa cha kudzikuza kwa anthu oyipa.
13 Wangin sripen pang lalos uh; God Kulana El tiana liyalos, ku lohng pusralos.
Ndithu, Mulungu samva kupempha kwawo kopanda pake; Wamphamvuzonse sasamalira zimenezi.
14 “Job, kom fahk mu kom tia ku in liye God; Tusruktu, kom in mongfisrasr ac tupan. Top lal nu sum uh oasr yorol.
Ndipo ndi bodza lalikulu kunena kuti Iye saona zimene zikuchitika. Iye adzaweruza molungama ngati inu mutamudikira
15 In nunak lom kom mu God El ac tiana kalyei mwet, Ac kom mu El tia arulana lohang nu ke ma koluk uh.
ndiye tsono popeza kuti ukali wake sukupereka chilango, zoyipa zambiri zimene anthu amachita,
16 Wangin sripa kom in nuna kaskas na; Kalem tari lah kom tia etu ma kom fahk an.”
abambo Yobu mumangoyankhula zopandapake, mukungochulukitsa mawu opanda nzeru.”

< Job 35 >