< Job 21 >
Pamenepo Yobu anayankha kuti,
2 “Porongo ma nga fahk uh; Pwayena ma nga siyuk komtal in akwoyeyu kac.
“Mvetserani bwino mawu anga; ichi chikhale chitonthozo changa chochokera kwa inu.
3 Fuhlema kitin pacl luk in kaskas, ac nga fin tari, Na komtal ku in isrunyu, komtal fin lungse.
Ndiloleni ndiyankhule ndipo ndikatha kuyankhula munditonzetonze.
4 “Alein luk uh tia ma in lain mwet; Oasr sripen semuteng luk uh.
“Kodi ine ndikudandaulira munthu? Tsono ndilekerenji kupsa mtima?
5 Ngetma liyeyu. Ya lumuk tia fal In oru komtal in lut ac kofla kaskas ke komtal suiyuwi uh?
Ndipenyeni ndipo mudabwe; mugwire dzanja pakamwa.
6 Ke nga nunku ma sikyak nu sik uh, Nga arulana oela, ac rarak ke sangeng.
Ndikamaganiza zimenezi ndimachita mantha kwambiri; thupi langa limanjenjemera.
7 “Efu ku God El lela mwet koluk uh in moul, Nwe ke na elos matuoh, ac wona nu selos?
Chifukwa chiyani anthu oyipa amakhalabe ndi moyo, amakalamba ndi kusanduka amphamvu?
8 Oasr tulik natulos ac nutin natulos, Ac elos moulna muta nwe ke na elos liye ke tulik inge matula uh.
Amaona ana awo akukhazikika pamodzi nawo, zidzukulu zawo zikukula bwino iwo akuona.
9 God El tiana sang ongoiya nu ke lohm selos uh; Ac elos tia wi pula mwe aksangeng uh.
Mabanja awo amakhala pa mtendere ndipo sakhala ndi mantha; mkwapulo wa Mulungu suwakhudza nʼkomwe.
10 Aok, cow mukul natulos orek fahko, wo ouiya pacl nukewa, Ac cow mutan uh oswela ma natulos wanginna ma misa.
Ngʼombe zawo zazimuna sizilephera kubereketsa; ngʼombe zawo zazikazi sizipoloza.
11 Tulik natulos uh kasrusrsrusr na srital oana sheep fusr uh,
Amatulutsa ana awo ngati gulu la nkhosa; makanda awo amavinavina pabwalo.
12 Ac onsrosro nu ke pusren mwe on harp ac flute.
Amayimba nyimbo pogwiritsa ntchito matambolini ndi azeze; amakondwa pakumva kulira kwa chitoliro.
13 Elos moul ke moul na misla Ac pacl in misa lalos uh, elos ac misa na in misla ac tiana keok. (Sheol )
Zaka zawo zimatha ali mu ulemerero ndipo amatsikira ku manda mwamtendere. (Sheol )
14 “Mwet koluk uh fahk nu sin God, ‘Fahsr liki kut! Mansis kut in tia etu ma kom lungse.
Koma anthuwo amawuza Mulungu kuti, ‘Tichokereni!’ Ife tilibe chikhumbokhumbo chofuna kudziwa njira zanu.
15 Su Ku liki Ku inge tuh kut in orekma nu sel? Mea, ac oasr ma wo nu sesr kut fin pre nu sel?’
Kodi Wamphamvuzonseyo ndani kuti timutumikire? Ife tipindula chiyani tikamapemphera kwa Iyeyo?
16 Elos fahk mu wo ouiya lalos uh ma na ke ku lalos sifacna, Tusruktu nga tia ku in insese nu ke luman nunak lalos inge.
Komatu ulemerero wawo suli mʼmanja mwawo, koma ine ndimakhala patali ndi uphungu wa anthu oyipa.
17 “Ku nu oasr pacl ma kuniyukla kalem lun mwet koluk uh? Ku nu oasr sie selos pula mwe ongoiya? Nu oasr pacl God El kai mwet koluk uh ke kasrkusrak
“Koma nʼkangati kamene nyale ya anthu oyipa imazimitsidwa? Nʼkangati kamene tsoka limawagwera? Nʼkangati kamene Mulungu amawakwiyira ndi kuwalanga?
18 Ac okulosla oana mah uh ke eng upa, Ku oana kutkut ma sohkla ke pacl in paka uh?
Nʼkangati kamene iwo amakhala ngati phesi lowuluka ndi mphepo, ngati mungu wowuluzika ndi kamvuluvulu?
19 “Komtal fahk mu God El akkeokye sie tulik ke sripen ma koluk lun papa tumal uh. Mo! Lela God Elan akkeokye na mwet se ma orekma koluk an; Lela in kalem selos lah God El oru ouinge ke sripen koluk ma elos sifacna oru.
Paja amati, ‘Mulungu amalanga ana chifukwa cha machimo abambo awo.’ Koma Mulungu amabwezera chilango munthuyo, kuti adziwe kuti Mulungu amalangadi.
20 Lela mwet koluk uh in sifacna us mwatan ma koluk lalos an; Lela elos in pula kasrkusrak lun God Kulana.
Mulole kuti adzionere yekha chilango chake, kuti alawe ukali wa Wamphamvuzonse.
21 Moul lun sie mwet fin safla, Mea pwaye lah ac oasr nunak lal ke tulik natul, lah elos engan ku tia?
Nanga kodi amalabadira chiyani zabanja lake limene walisiya mʼmbuyo, pamene chiwerengero cha masiku ake chatha?
22 Mea, mwet uh ku in luti God, Su nununku mwet nukewa, finne elos su muta yen fulat?
“Kodi alipo wina amene angaphunzitse Mulungu nzeru, poti Iye amaweruza ngakhale anthu apamwamba?
23 “Sie kain mwet ac misa ke pacl na ma yohk wo ouiya nu sel, Ac el mutana okak ac misla.
Munthu wina amamwalira ali ndi mphamvu zonse, ali pa mtendere ndi pa mpumulo,
24 Manol factfat na wo, ac koanon sri kacl uh srakna ku.
thupi lake lili lonenepa, mafupa ake ali odzaza ndi mafuta.
25 A sie kain mwet uh wangin na pwaye engan lal; El inse toasr na ke el moul nwe ke na el misa.
Munthu wina amamwalira ali wowawidwa mtima, wosalawapo chinthu chabwino chilichonse.
26 Tusruktu elos kewa ac oana sie: elos ac misa, pukpuki, Ac manolos afla ke wet.
Olemera ndi osauka omwe amamwalira ndi kuyikidwa mʼmanda ndipo onse amatuluka mphutsi.
27 “Nga etu nunak koluk lomtal ingan.
“Ndikudziwa bwino zimene mukuganiza, ziwembu zanu zomwe mukuti mundichitire.
28 Komtal fahk, ‘Pia lohm sin leum sac inge; Mwet se ma mutana oru ma koluk?’
Inu mukuti, ‘Kodi nyumba ya mkulu uja ili kuti, matenti amene munkakhala anthu oyipa aja ali kuti?’
29 “Ku komtal soenna wi sramsram nu sin mwet ma muta forfor nu saya uh? Komtal tiana etu kain mwe sramsram ma elos ac som nwe foloko srumun uh?
Kodi munawafunsapo anthu amene ali pa ulendo? Kodi munaganizirapo zimene iwo amanena?
30 Ke len ma God El ac kasrkusrak ac akkeokye mwet uh, Mwet koluk uc wacna tia pula ma upa.
Zakuti munthu woyipa amasungidwa chifukwa cha tsiku la tsoka, kuti amapulumutsidwa chifukwa cha tsiku la ukali wa Mulungu?
31 Wanginna mwet muta tukakin mwet koluk uh, Ku folokin nu sel ke ma koluk nukewa ma el orala.
Kodi ndani amadzudzula munthu wochimwayo? Ndani amamubwezera zoyipa zimene anachita?
32 Ke el ac utukla nu ke kulyuk uh, Nu ke luf kial su arulana taranyuk wo,
Iye amanyamulidwa kupita ku manda ndipo anthu amachezera pa manda ake.
33 Mwet puspis ac fah wi fahsr nu ke pukmas uh, Ac finne fohkon acn uh, ac fah arulana mulala nu facl.
Dothi la ku chigwa limamukomera; anthu onse amatsatira mtembo wake, ndipo anthu osawerengeka amakhala patsogolo pa chitanda chakecho.
34 “A komtal! Komtal srike in akwoyeyu ke kas lusrongten! Top lomtal an kikiap nufon!”
“Nanga inu mudzanditonthoza bwanji ine ndi mawu anu opandapakewo palibe chimene chatsala kuti muyankhe koma mabodza basi!”