< Job 12 >

1 Na Job el fahk,
Pamenepo Yobu anayankha kuti,
2 “Aok, komtal aolla pusren mwet uh. Komtal fin misa, na lalmwetmet ac fah wi komtal na misa.
“Ndithudi inuyo ndinu anthu ndipo nzeru zanu zidzafera nanu pamodzi!
3 Tusruktu oasr pacna ma nga etu oana komtal; Wanginna ma nga ten liki komtal kac; Mwet nukewa etu ma komtal fahk an.
Koma inenso ndili nazo nzeru ngati inu; ineyo sindine munthu wamba kwa inu. Ndani amene sadziwa zonse zimene mwanenazi?
4 Finne mwet kawuk luk, elos isrunyu pac in pacl inge; Nga ne suwoswosna ac wangin mwetik, a elos isrun yu pacna; Tusruktu, oasr pacl God El tuh topuk pre luk.
“Ndasanduka chinthu choseketsa kwa abwenzi anga, ngakhale ndinkapemphera kwa Mulungu ndipo Iye ankandiyankha. Ine ndasanduka chinthu chongoseketsa, ngakhale ndili wolungama ndi wosalakwa!
5 Komtal tiana pula ma upa, a komtal isrunyu; Komtal sringilya mwet se ma apkuran in ikori uh.
Anthu amene ali pabwino amanyoza anzawo amene ali pa tsoka. Tsokalo limagwa pa amene wayamba kale kugwa.
6 Mwet pisrapasr ac mwet koluk elos mutana in misla, A pwayena god lalos pa ku lalos sifacna.
Nyumba za anthu achifwamba zimakhala pa mtendere, ndipo anthu amene amaputa Mulungu amakhala pabwino, amene amanyamula milungu yawo mʼmanja.
7 “Finne won ku kosro lemnak uh, oasr pac ma elos ku in luti nu sumtal;
“Koma funsa nyama zakuthengo ndipo zidzakuphunzitsa, kapena mbalame zamumlengalenga ndipo zidzakuwuza;
8 Siyuk lalmwetmet sin ma orakrak fin faclu ac ik in meoa uh.
kapena uyankhule ndi dziko lapansi ndipo lidzakuphunzitsa, kapena ulole nsomba zamʼnyanja kuti zikufotokozere.
9 Elos nukewa etu lah poun God pa oralosla uh.
Kodi mwa zonsezi ndi chiti chimene sichidziwa kuti lachita zimenezi ndi dzanja la Yehova?
10 God pa kol moul lun ma El orala inge; Moul lun mwet nukewa oan ye ku lal.
Mʼmanja mwake ndi mʼmene muli moyo wa cholengedwa chilichonse, ndiponso moyo wa anthu a mitundu yonse.
11 Tusruktu, insremtal engan in lohng kas uh, Oana ke loumtal lungse ema mwe mongo.
Kodi khutu sindiye limene limamva mawu monga mmene lilime limalawira chakudya?
12 “Lalmwetmet oasr sin mwet matu uh, Ke elos matuoh, yohk etauk lalos.
Kodi nzeru sipezeka pakati pa anthu okalamba? Kodi moyo wautali sumabweretsa nzeru zomvetsa zinthu?
13 Tusruktu God El sisani kewa lalmwetmet ac ku; El liyaten ac sessesla ke lalmwetmet.
“Kwa Mulungu ndiye kuli nzeru ndi mphamvu; uphungu ndi kumvetsa zinthu ndi zake.
14 God El fin ikruiya sie ma, su ku in sifilpa tulokunak? God El fin kapriya sie mwet, su ac ku in tulala?
Chimene Iye wapasula palibe angachimangenso. Akatsekera munthu mʼndende palibe angamutulutse.
15 Faclu ac paola God El fin tulokinya af uh; Sronot uh tuku ke El fuhlela af upa uh.
Iyeyo akamanga mvula dziko limawuma; akamasula mvulayo, madzi amasefukira pa dziko.
16 “God El ku ac El kutangla pacl nukewa; Mwet kikiap ac mwet ma kiapweyukla kewa oan ye ku lal.
Kwa Iye kuli mphamvu ndi kupambana; munthu wopusitsidwa ndiponso wopusitsa onse ali mu ulamuliro wake.
17 El eisla nunak lalmwetmet lun mwet leum, Ac oru mwet kol uh in orekma oana mwet lalfon.
Iye amalanda aphungu nzeru zawo ndipo amapusitsa oweruza.
18 El sisla tokosra uh liki nien muta fulat lalos, ac oru tuh elos in mwet kapir;
Iye amachotsa zingwe zimene mafumu anawamanga nazo ndipo amawamanga lamba mʼchiwuno mwawo.
19 El akpusiselye mwet tol ac mwet ma oasr wal la uh.
Iye amasocheretsa ansembe atawalanda nzeru zawo ndipo amagonjetsa anthu amphamvu amene ndi okhazikika.
20 El kaliya oalin mwet lulalfongiyuk uh in tia kaskas, Ac El eisla lalmwetmet lun mwet matu lukelos.
Iye amakhalitsa chete aphungu odalirika ndipo amalanda chidziwitso cha anthu akuluakulu.
21 El akmwekinye mwet leum uh Ac tulokinya ku lun mwet kol uh.
Iye amanyoza anthu otchuka ndipo anthu anyonga amawatha mphamvu.
22 El tolak yen lohsr, aok yen lohsr lun misa.
Iye amatulutsira poyera zinthu zozama za mu mdima ndipo mdima wandiweyaniwo amawusandutsa kuwala.
23 El oru kutu mutunfacl uh in yohk ac pwengpeng, Na El sifilpa kutangulosla ac kunauselosla.
Iye amakuza mitundu ya anthu ndipo amayiwononganso; amachulukitsa mitundu ya anthu ndipo amayimwazanso.
24 El oru mwet leum lalos in lalfonla Ac fuhlela elos forfor oana mwet fohsak ac tuhlac;
Iye amalanda nzeru za atsogoleri a dziko lapansi; amawayendetsa mʼthengo mopanda njira.
25 Elos kahlimin acn lohsr uh, ac tukulkul oana mwet sruhi uh.
Iwo amafufuzafufuza njira mu mdima wopanda chowunikira; Iye amawayendetsa dzandidzandi ngati oledzera.

< Job 12 >