< Jeremiah 49 >

1 Pa inge ma LEUM GOD El fahk ke mwet Ammon: “Pia mukul Israel uh? Ya wangin mwet in tuyak loango facl selos? Fuka tuh mwet ma alu nu sel Molech elos tuku eisla acn sin sruf lal Gad ac oakwuki we?
Yehova ananena izi: Amoni, “Kodi Israeli alibe ana aamuna? Kapena alibe mlowamʼmalo? Tsono nʼchifukwa chiyani anthu opembedza Moleki alanda dziko la Gadi? Nʼchifukwa chiyani anthu ake akukhala mʼmizinda ya Gadi?
2 Tusruktu pacl se ac fah tuku ke nga fah oru mwet in siti fulat Rabbah in lohng kusen mweun, na acn we ac fah sikiyukla, ac inkul we ac fah firirla nwe ke apatla. Na mwet Israel fah sifil eisla acn selos ma mwet Ammon tuh eisla.
Koma nthawi ikubwera,” akutero Yehova, “pamene ndidzamveketse mfuwu wankhondo ku Raba, likulu la Amoni; ndipo malo awo opembedzera milungu yawo adzatenthedwa ndi moto. Choncho Aisraeli adzalandanso dziko lawo kuchokera kwa amene anawalanda poyamba dzikolo,” akutero Yehova.
3 Mwet Heshbon, kowos in wowoyak tung! Acn Ai kunausyukla! Mutan Rabbah, kowos in eoksra! Nokomang nuknuk yohk eoa ac muta in asor, ac sifacna sringil monuwos. Molech, god lowos, fah utukla nu in sruoh, wi mwet tol ac mwet fulat lal.
“Lirani, inu anthu a ku Hesiboni chifukwa wowononga uja wafika! Fuwulani, inu anthu okhala ku Raba! Valani ziguduli ndi kulira mwamphamvu; thamangani uku ndi uku mʼkati mwa malinga, chifukwa mulungu wanu Moleki adzapita ku ukapolo, pamodzi ndi ansembe ake ndiponso akuluakulu ake.
4 Kowos mwet sesuwos, efu kowos ku konkin? Ku lowos uh sriksrikeni. Efu ku kowos lulalfongi ku lowos sifacna, ac fahk mu wangin mwet ac pulaik in mweuni kowos?
Chifukwa chiyani mukunyadira chigwa chanu, inu anthu osakhulupirika amene munadalira chuma chanu nʼkumati: ‘Ndani angandithire nkhondo?’
5 Nga fah use mwe aksangeng nu fowos liki acn nukewa. Kowos nukewa fah kaingelik. Kais sie fah kaing in suk moul lal, ac wangin sie fah ku in orani mwet mweun lowos uh.
Ndidzabweretsa zoopsa pa iwe zochokera kwa onse amene akuzungulira,” akutero Ambuye, Mulungu Wamphamvuzonse. “Mudzathawa, ndipo aliyense adzathawitsa moyo wake. Sipadzapezeka munthu wosonkhanitsanso othawawo.
6 Tusruktu tok, nga fah oru mwet Ammon in sifil kapkapak. Nga, LEUM GOD, pa fahk ma inge.”
“Komabe pambuyo pake, ndidzabwezera kwawo Aamoni,” akutero Yehova.
7 Pa inge ma LEUM GOD Kulana El fahk ke acn Edom: “Ya wanginla pwapa ac oakwuk wo yurin mwet Edom? Ya mwet kasru lalos tila lotelos ke ma fal elos in oru? Ya lalmwetmet nukewa lalos wanginla?
Yehova Wamphamvuzonse ananena izi za Edomu: “Kodi nzeru sizikupezekanso ku Temani? Kodi anzeru analeka kupereka uphungu? Kodi nzeru zawo zinatheratu?
8 Mwet Dedan, kowos in forla, kaing, ac wikla! Nga ac kunausla fwilin tulik natul Esau mweyen sun pacl ngan kaelos.
Inu anthu a ku Dedani, thawani, bwererani ndi kukabisala ku makwalala chifukwa ndidzagwetsa mavuto pa zidzukulu za Esau popeza nthawi yawo ya chiweruzo yafika.
9 Ke mwet uh sifani grape, elos ac likiya kutu in oanna ke oa in grape ah. Ac finne mwet pusrapasr uh ac tuku ke fong, elos ac eis na lupa elos enenu.
Kodi anthu othyola mphesa akanafika kwa inu akanakusiyiraniko mphesa pangʼono pokha? Anthu akuba akanafika usiku akanangotengako zimene akuzifuna zokha?
10 Tusruktu nga arulana kunausla ma nukewa lun fwilin tulik natul Esau, ac nga konauk ac kunausla acn in wikwik lalos, na elos tia ku in sifil wikla we. Mwet Edom nukewa sikiyukla. Wangin siefanna selos lula.
Koma ine ndazivula zidzukulu za Esau. Ndaonetsa poyera malo awo obisalamo, kotero kuti sadzathanso kubisala. Ana ake, abale ake pamodzi ndi anansi ake awonongeka. Palibe wonena kuti,
11 Filiya tulik mukaimtal nutuwos an yuruk, ac nga fah liyalosyang. Katinmas lowos an ku in lulalfongiyu in kasrelos.
‘Siyani ana anu amasiye; Ine ndidzawateteza. Amayi anu amasiye akhoza kudalira Ine.’”
12 “Fin pa mwet su wangin mwata enenu in nim ke cup in kaiyuk, ya kowos nunku mu kowos ac tia wi sun kaiyuk? Mo, kowos enenu na in nim ke cup sac!
Yehova akuti, “Ngati iwo amene sanali oyenera kulangidwa adzamwa chikho cha chiweruzo, ndiye muyesa kuti inuyo simudzalangidwa? Ayi ndithu simudzakhala osalangidwa. Mudzamwa ndithu chikhocho.
13 Nga sifacna fulahk lah siti Bozrah ac fah ekla sie acn sikiyukla ac mwet uh ac tuninfong ke liyeya. Elos ac fah sufan, ac orekmakin inen acn we oana kas in selnga. Inkul atulani nukewa ac fah oan srualana nwe tok. Nga, LEUM GOD, pa fahk ma inge.”
Ine ndikulumbira, akutero Yehova, kuti mzinda wa Bozira udzasanduka bwinja, chinthu chochititsa mantha, chomachiseka ndiponso chotembereredwa. Mizinda yake yonse idzakhala mabwinja mpaka muyaya.”
14 Na nga fahk, “Edom, nga eis sie kas sin LEUM GOD me. El supwama sie mwet in sulkakin nu sin mutunfacl uh tuh elos in orani un mwet mweun lalos ac akola in mweuni kom.
Ndamva uthenga wochokera kwa Yehova: Nthumwi yatumidwa kupita kwa anthu a mitundu ina kukanena kuti, “Sonkhanani pamodzi kuti muthire nkhondo Edomu! Konzekerani nkhondo!”
15 LEUM GOD El ac oru kom in munas inmasrlon mutunfacl uh, ac elos fah pilesrekom.
“Ndidzakuchepetsani pakati pa anthu a mitundu ina. Mudzakhala anthu onyozeka pakati pa anthu.
16 Inse fulat lom uh kiapwekomla, ac kom nunku mu mutunfacl saya elos sangeng sum. Kom muta fin fulu uh, yen fulat fin mangon eol uh; tusruktu kom nwe muta yen fulat oana eagle uh, LEUM GOD El ac srukkomi nwe ten. LEUM GOD, pa fahk ma inge.”
Kuopseza kwako kwakunyenga; kudzikuza kwa mtima wako kwakusocheretsa, iwe amene umakhala mʼmapanga a mʼmatanthwe ndi mʼmapiri. Ngakhale utamanga chisa chako pamwamba kwambiri ngati chiwombankhanga, ndidzakutsitsa pansi kuchokera kumeneko,” akutero Yehova.
17 LEUM GOD El fahk, “Lupan musalla ma ac sikyak in acn Edom ac fah arulana upa, oru elos nukewa su fahsryak we ac fah lut ac tuninfongla.
“Dziko la Edomu lidzasanduka chinthu chochititsa mantha. Onse odutsamo adzadabwa ndi kupukusa mitu yawo chifukwa cha kuwonongeka kwake.
18 Ma ac sikyak nu ke acn Edom inge, pa pacna tuh sikyak nu ke acn Sodom ac Gomorrah ke tuh kunausyukla acn we, wi inkul nukewa ma oan raunela. Wangin mwet ac sifilpa muta we. Nga, LEUM GOD, pa fahk ma inge.
Monga momwe anawonongekera Sodomu ndi Gomora, pamodzi ndi mizinda yake yozungulira,” akutero Yehova, “motero palibe munthu amene adzakhala mu Edomu.
19 Oana ke soko lion ac sasma liki insak matol sisken Infahl Jordan yak nu ke inima folfol insroa, nga fah tuku ac oru mwet Edom in sa kaing liki facl selos. Na mwet kol se nga sulela uh ac fah leumi facl sac. Su ku in lumweyuk nu sik? Su pulaik in kisrungyu? Ma ya mwet leum se ac lainyu?
“Monga mkango wotuluka ku nkhalango za ku Yorodani kupita ku malo a msipu wobiriwira, Ine ndidzapirikitsa anthu a ku Edomu mwadzidzidzi kuchoka mʼdziko lawo. Pambuyo pake ndidzawayikira owalamulira amene ndamufuna Ine. Kodi ndani wofanana nane, ndipo angatsutsane nane ndani? Ndipo ndi mʼbusa uti amene angalimbane nane?”
20 Ouinge, porongo oakwuk ma nga oru in lain mwet Edom, ac ma nga akoo in oru nu sin mwet in siti Teman. Finne tulik natulos, ac amala som, ac mwet nukewa ac fah tuninfongla.
Nʼchifukwa chake imvani. Izi ndi zimene Ine Yehova ndakonza zolangira anthu a ku Edomu ndi a ku Temani. Ngakhale ana omwe adzatengedwa ukapolo ndipo aliyense adzachita mantha chifukwa cha iwo.
21 Pacl se Edom ac putatla uh, kusa uh ac arulana yohk, pwanang faclu nufon kusrusryak, ac pusren tuninfong lun mwet uh ac fah lohngyuk oe yen loessula, sun Meoa Srusra.
Akadzagwa Edomu padzakhala mfuwu waukulu ndipo dziko lapansi lidzanjenjemera; kulira kwawo kudzamveka mpaka ku Nyanja Yofiira.
22 Mwet lokoalok ac fah mweuni Bozrah oana sie eagle asroelik paol ac pwesroulme. Ke len sac, mwet mweun lun Edom ac fah sangeng oana sie mutan ac isus.”
Taonani, mtundu wina udzachita kuwuluka nʼkudzatera pa Bozira ngati chiwombankhanga chimene chatambalitsa mapiko ake. Pa tsiku limenelo mitima ya ankhondo a ku Edomu idzagunda ngati mtima wa mayi pa nthawi yake yochira.
23 Pa inge ma LEUM GOD El fahk ke acn Damascus: “Mwet in siti Hamath ac Arpad elos fosrnga ac sensen mweyen elos lohng pweng koluk. Mwe sensen afnulosi oana pulkulak lun noa meoa, ac elos tia ku in mongla.
Mawu a Yehova onena za Damasiko ndi awa: “Anthu a ku Hamati ndi a ku Aripadi akuchita mantha chifukwa amva nkhani yoyipa. Mitima yawo yagwidwa ndi mantha ndipo ali ngati muja ichitira nyanja yosakhazikika.
24 Mwet Damascus elos munaslana, ac elos nukewa kaing. Elos fosrnga ac sensen ac keok, oana sie mutan in pacl in isus.
Anthu a ku Damasiko alefuka. Abwerera mʼmbuyo kufuna kuthawa chifukwa agwidwa ndi mantha aakulu. Ali ndi nkhawa komanso mantha ngati za mayi pa nthawi yake yochira.
25 Siti se ma tuh pwengpeng ac engan meet, inge wanginla mwet muta we.
Mzinda wotchuka ndi wachikondwerero uja wasiyidwa!
26 Ke len sac, mwet fusr lal ac fah anwuki inkanek lun siti uh, ac mwet mweun lal nukewa sikiyukla.
Nʼchifukwa chake anyamata ake adzagwa mʼmisewu ndi kufa; ankhondo ake onse adzawonongedwa tsiku limenelo,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
27 Nga fah esukak pot lun Damascus, ac nga fah furreak inkul fulat sel Tokosra Benadad. Nga, LEUM GOD Kulana, pa fahk ma inge.”
“Ndidzatentha malinga a Damasiko; moto udzanyeketsa nyumba zaufumu za Beni-Hadadi.”
28 Pa inge ma LEUM GOD El fahk ke sruf Kedar ac facl ma karinginyuk sin acn Hazor, su tuh kutangyukla sel Tokosra Nebuchadnezzar lun Babylonia: “Mweuni mwet Kedar, ac sukela sruf se ingan su muta in acn kutulap!
Mawu a Yehova onena za Kedara ndi maufumu a ku Hazori, amene Nebukadinezara mfumu ya Babuloni anawagonjetsa ndi awa: “Nyamukani mukathire nkhondo ku Kedara. Kawonongeni anthu a kummawako.
29 Sruokya lohm nuknuk selos ac un kosro natulos, mwe lisrlisr ke lohm nuknuk selos ac ma nukewa in lohm selos. Eisla camel natulos ac fahk nu sin mwet uh, ‘Kowos rauniyukla ke mwe aksangeng!’
Landani matenti awo ndi nkhosa zawo, ndiye kuti, mutenge nsalu zawo ndi katundu wawo. Mutengenso ngamira zawo. Anthu adzafuwula kwa iwo kuti, ‘Kuli zoopsa mbali zonse!’
30 “Mwet Hazor, nga LEUM GOD, sensenkakin kowos tuh kowos in kaingla nu yen loessula ac wikla. Tokosra Nebuchadnezzar lun Babylonia el orek pwapa in lain kowos, ac pa inge ma el fahk,
“Thawani mofulumira! Kabisaleni mʼmakhwawa, inu anthu ku Hazori,” akutero Yehova. “Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni wakukonzerani chiwembu; wakonzekera zoti alimbane nanu.
31 ‘Tuyak, som mweuni mwet ingo su muta in misla ac wangin fosrnga lalos! Acn selos wangin mutunpot, wangin pac polosak in sang kaliya, ac wangin facl apkuran nu yorolos.
“Nyamukani kathireni nkhondo mtundu wa anthu umene uli pamtendere, umene ukukhala mosatekeseka,” akutero Yehova, “mzindawo ulibe zipata ngakhalenso mipiringidzo; anthu ake amakhala pa okha.
32 “Eisla camel ac cow nukewa natulos! Mwet ingan su kalla insifalos fototo, nga fah luselosla nu yen nukewa. Nga fah oru tuh ongoiya in tuku nu faclos yen nukewa me.
Ngamira zawo zidzafunkhidwa, ndipo makola a ngʼombe zawo adzalandidwa. Ndidzabalalitsira ku mphepo zinayi onse amene amameta tsitsi lawo chamʼmbali. Ndidzawagwetsera mavuto kuchokera ku mbali zonse,” akutero Yehova.
33 Acn Hazor ac fah sie acn mwesis nwe tok, sie acn ma kosro inima mukena muta we. Wangin mwet ac sifilpa muta we. Nga, LEUM GOD, pa fahk ma inge.”
“Hazori adzasanduka bwinja, malo okhalamo nkhandwe mpaka muyaya. Palibe munthu amene adzayendemo.”
34 Tia paht tukun Zedekiah el tokosrala lun Judah, LEUM GOD Kulana El kaskas nu sik ke acn Elam.
Uthenga umene Yehova anapatsa mneneri Yeremiya wonena za Elamu, Zedekiya mfumu ya Yuda atangoyamba kulamulira ndi uwu:
35 El fahk, “Nga fah uniya mwet pisr nukewa su oru Elam arulana ku.
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Taonani, ndidzathyola uta wa Elamu, umene uli chida chawo champhamvu.
36 Nga fah oru eng uh in tuhyak lain Elam liki acn nukewa, ac nga fah akfahsryelik mwet lal nu yen nukewa, nwe ke wangin sie mutunfacl ma elos tia kaingelik nu we.
Ndidzabweretsa mphepo zinayi pa Elamu kuchokera ku zigawo zinayi zamlengalenga; ndidzawabalalitsira ku mphepo zinayi, ndipo sipadzakhala dziko limene anthu a ku Elamu sadzafikako.
37 Nga fah oru mwet Elam elos in sangeng sin mwet lokoalok lalos, su lungse onelosi. In kasrkusrak lulap luk, nga fah kunausla mwet Elam ac supwala un mwet mweun lainulos nwe ke nga sukelosla nufon.
A ku Elamuwo ndidzachititsa mantha pamaso pa adani awo komanso pamaso pa iwo amene akufuna kuwononga moyo wawo. Ndidzawagwetsera mkwiyo wanga ndipo adzakhala pa mavuto,” akutero Yehova. “Ndidzawapirikitsa ndi lupanga mpaka nditawatheratu.
38 Nga fah kunausla tokosra ac mwet kol lalos, ac nga fah tulokunak tron luk we.
Ndidzakhazika mpando wanga waufumu ku Elamu ndipo ndidzawononga mfumu yake pamodzi ndi akuluakulu ake,” akutero Yehova.
39 Tusruktu tok nga fah oru mwet Elam in sifilpa kapkapak. Nga, LEUM GOD, pa fahk ma inge.”
“Komabe mʼtsogolomo ndidzabwezera anthu a ku Elamu dziko lawo,” akutero Yehova.

< Jeremiah 49 >