< Jeremiah 45 >

1 In yac se akakosr ma Jehoiakim, wen natul Josiah, el tuh tokosra lun Judah, Baruch el simusla kas nukewa nga fahkang nu sel. Na nga fahk nu sel,
Uwu ndi uthenga umene mneneri Yeremiya anawuza Baruki mwana wa Neriya mʼchaka cha chinayi cha Yehoyakimu mwana wa mwana ya Yosiya kuti alembe mʼbuku.
2 “Pa inge kas lun LEUM GOD lun Israel nu sum: ‘Baruch,
“Yehova Mulungu wa Israeli, akunena kwa iwe Baruki kuti:
3 kom fahk mu “Nga fuhleak finsrak! LEUM GOD El ase mwe asor in laesla mwe lokoalok luk. Nga totola ke sao luk, ac nga tia ku in konauk mongla!’”
Iwe unati, ‘Kalanga ine! Yehova wawonjezera chisoni pa mavuto anga. Ine ndatopa ndi kubuwula ndipo sindikupeza mpumulo.’”
4 “Tusruktu nga, LEUM GOD, nga ikruiya ma nga musaela, ac nga fusak ma nga yukwiya. Nga ac oru ouinge nu ke faclu nufon.
Koma Yehova akukuwuza kuti, “Ndidzagwetsa chimene ndinamanga ndipo ndidzazula chimene ndinadzala. Ndidzachita zimenezi mʼdziko lonse.
5 Ya kom suk in orek nu sum wo liki mwet ngia? Nimet nunku ouingan. Nga ac sang mwe ongoiya nu fin mwet nukewa, tusruktu kom sifacna ac fah moulla in kutena acn kom ac som nu we. Nga, LEUM GOD, pa fahk ma inge.”
Kodi tsono ukudzifunira wekha zinthu zazikulu? Usadzifunire. Pakuti ndidzagwetsa mavuto pa anthu onse, koma ndidzasunga moyo wako kulikonse kumene ungadzapite.”

< Jeremiah 45 >