< Jeremiah 13 >

1 LEUM GOD El fahk nu sik nga in som ac molela sie mwe lohl linen ac sang losya infulwuk; a El fahk mu nga in tia twenya in kof uh.
Yehova anandiwuza kuti, “Pita kagule lamba wansalu yosalala ndipo ukavale mʼchiwuno mwako, koma usakamuviyike mʼmadzi.”
2 Ke ma inge nga molela ac sang losyuwi, oana ma LEUM GOD El fahk.
Choncho ndinakagula lambayo, monga momwe anandiwuzira Yehova, ndipo ndinamanga mʼchiwuno mwanga.
3 Na LEUM GOD El sifilpa kaskas nu sik ac fahk,
Kenaka Yehova anandiyankhulanso kachiwiri kuti,
4 “Fahla nu Infacl Euphrates ac okanla mwe lohl se ingan in sie luf ke eot uh.”
“Tenga lamba amene unagula ndi kuvala mʼchiwuno mwako uja. Tsono pita ku mtsinje wa Yufurate ndipo ukamubise lambayo mʼmingʼalu ya mʼmatanthwe.”
5 Ouinge nga som ac okanla sisken Infacl Euphrates, oana LEUM GOD El fahk.
Ndipo ndinapitadi ndi kukabisa lambayo ku Yufurate, monga anenera Yehova.
6 Tukun len puspis, LEUM GOD El fahk nu sik in folokla nu Infacl Euphrates ac eis mwe lohl sac.
Patapita masiku ambiri Yehova anandiwuzanso kuti, “Pitanso ku Yufurate ndipo ukatenge lamba amene ndinakuwuza kuti ukamubise kumeneko.”
7 Ouinge nga folokla, ac pacl se nga konauk acn se ma nga okanla we ah, nga liye lah kulawi ac wanginla sripa.
Choncho ndinapita ku Yufurate kukafukula lambayo ndi kumuchotsa pamalo pamene ndinamubisa, koma nthawi imeneyi nʼkuti lambayo atawonongeka kotheratu ndipo analibenso ntchito.
8 Na LEUM GOD El sifilpa kaskas nu sik ac fahk,
Pamenepo Yehova anandiwuza kuti,
9 “In ouiya se pacna inge, nga fah kunausla inse fulat lun Judah ac filang lulap lun Jerusalem.
“Izi ndi zimene ine ndikunena: ‘Umu ndi mmene ndidzawonongere zimene akunyadira kwambiri a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu.
10 Mwet koluk inge elos tia lungse akosyu. Elos likkeke ac orekma koluk oana meet ah, ac elos alu ac kulansupu god ngia. Ke ma inge, elos ac fah oana mwe lohl se inge ma wanginla sripa.
Anthuwa ndi oyipa. Iwo akana kumvera mawu anga. Mʼmalo mwake amawumirira kutsata milungu ina, kuyitumikira ndi kuyipembedza. Anthu amenewa adzakhala ngati lamba wopanda ntchitoyu.
11 Oana ke sie mwe lohl ac tingilya infulwen sie mwet, ouinge nga tuh finsrak mu mwet Israel ac mwet Judah nukewa in arulana fulme nu sik. Nga oru ouinge tuh elos fah mwet luk, ac elos in kaksakinyu ac akfulatye Inek. Tusruktu elos tiana akosyu.”
Monga momwe lamba amakanirira mʼchiwuno cha munthu, momwemonso ndinakonza kuti nyumba yonse ya Israeli ndi nyumba yonse ya Yuda indikangamire Ine kuti akhale anthu anga, kuti azitamanda dzina langa ndi kulemekeza Ine. Koma iwo sanamvere,’ akutero Yehova.
12 LEUM GOD El fahk nu sik, “Jeremiah, fahk nu sin mwet Israel lah sufa in wain nukewa in nwanala ke wain. Elos ac fah topuk mu elos etu lah sufa in wain nukewa enenu in nwanala ke wain.
“Awuze anthuwo kuti, ‘Yehova Mulungu wa Israeli akuti: Mtsuko uliwonse adzawudzaza ndi vinyo.’ Ndipo ngati iwo anena kwa iwe kuti, ‘Kodi ngati ife sitikudziwa kuti mtsuko uliwonse udzadzazidwa ndi vinyo?’
13 Na kom in fahk nu selos lah nga, LEUM GOD, ac fah oru tuh mwet uh in sruhila — aok tokosra ke fwilin tulik natul David, mwet tol, mwet palu, ac mwet Jerusalem nukewa.
Tsono iwe uwawuze kuti, Yehova akuti ‘Ine ndidzaledzeretsa anthu onse okhala mʼdziko muno, kuyambira mafumu amene amakhala pa mpando waufumu wa Davide, ansembe, aneneri, pamodzi ndi anthu onse amene akukhala mu Yerusalemu.
14 Toko nga fah fukulya mwet inge oana ke sufa uh afokfoki, mwet matu ac mwet fusr oana sie. Wangin pakomuta, kulang, ku nunak munas fah sruokyuwi liki in onelosla.”
Ndidzawagundanitsa mitu kuti aphwanyane okhaokha ngati mitsuko, makolo ndi ana awo, akutero Yehova. Sindidzawamvera chisoni kapena kuwachitira chifundo kapena kukhudzidwa nawo kuti ndileke kuwawononga.’”
15 Mwet Israel, LEUM GOD El kaskas tari! Kowos in inse pusisel ac porongel.
Imvani inu Aisraeli ndipo tcherani khutu, musadzitukumule, pakuti ndi Yehova amene akuyankhula.
16 Akfulatye LEUM GOD lowos, Meet liki El use lohsr Ac kowos tukulkul fineol uh; Meet liki El ekulla kalem se su kowos finsrak nu kac Nu ke lohsr matoltol.
Lemekezani Yehova Mulungu wanu asanagwetse mdima, mapazi anu asanayambe kupunthwa mʼchisisira chamʼmapiri. Asanasandutse kuwala mukuyembekezerako kukhala mdima wandiweyani.
17 Kowos fin tia porongo, Nga ac tung in lukma ke sripen inse fulat lowos. Nga fah tung mwemelil, ac sroninmutuk fah kahkla, Mweyen mwet lun God elos utukla nu in sruoh.
Koma ngati simumvera, ndidzalira kwambiri chifukwa cha kunyada kwanu. Mʼmaso mwanga mwadzaza ndi misozi yowawa chifukwa nkhosa za Yehova zatengedwa ukapolo.
18 LEUM GOD El fahk nu sik, “Fahk nu sin tokosra ac nina kial in fani liki tron lalos, mweyen tefuro wolana lalos itukla liki sifalos.
Uza mfumu pamodzi ndi amayi ake kuti, “Tsikani pa mipando yaufumuyo, pakuti zipewa zanu zaufumu zokongolazo zagwa pansi.”
19 Siti lun Judah layen eir kuhlusyuki. Wangin mwet ku in utyak nu we. Mwet Judah nukewa utukla nu in sruoh.”
Mizinda ya ku Negevi yatsekedwa ndipo palibe wina woti nʼkuyitsekula. Yuda yense watengedwa kupita ku ukapolo, watengedwa yense ukapolo.
20 Jerusalem, liye! Mwet lokoalok lom pa tuku liki acn epang! Pia mwet itukot tuh kom in karingin uh — mwet lom su kom arulana yukin?
Tukula maso ako kuti uwone amene akubwera kuchokera kumpoto. Kodi nkhosa zimene anakusungitsa zili kuti, nkhosa zanu zokongola zija?
21 Mea kom ac fahk ke mwet su kom pangon mu kawuk lom elos kutangkomla ac leum fom? Kom ac keok oana sie mutan isus.
Kodi udzanena chiyani pamene [Yehova] adzakuyikira anthu amene unkanena kuti ndi abale ako akukugonjetsa ndi kukulamulira? Kodi sudzamva zowawa ngati za mayi pa nthawi yake yochira?
22 Kom fin siyuk lah efu ku ma inge sikyak nu sum — efu ku nuknuk lom sisala liki monum ac sruinkuiyuki kom — mweyen ma koluk lom uh arulana yohk.
Ndipo ngati udzadzifunsa kuti, “Kodi zimenezi zandichitikira chifukwa chiyani?” Ndi chifukwa cha machimo anu ambiri kuti zovala zanu zingʼambike ndiponso kuti akuchitireni nkhanza.
23 Ya sie mwet sroalsroal ku in ekulla tuhnal, ku soko leopard ku in sisla tuhntun kacl? Elos funu ku, na kowos su pahlana in oru ma koluk lukun ku in lotela in oru ma pwaye.
Kodi wa dziko la Kusi nʼkusintha khungu lake, kapena kambuku kusintha mawanga ake? Inunso amene munazolowera kuchita zoyipa simungathe kusintha.
24 LEUM GOD El ac akfahsryekowoselik oana ke eng uh okla kutkut yen mwesis.
“Ine ndidzakumwazani ngati mankhusu amene amawuluka ndi mphepo ya ku chipululu.
25 El fahk mu pa inge ma ac sikyak nu sum tok. Pa inge ma El sulela in oru nu sum, mweyen kom mulkunulla ac lulalfongi ke god ma tia pwaye.
Limeneli ndiye gawo lanu, chilango chimene ndakukonzerani chifukwa chondiyiwala Ine ndi kutumikira milungu yabodza, akutero Yehova.
26 LEUM GOD sifacna El ac fah sarukkomla in akmwekinye kom.
Ine ndidzakwinya zovala zanu mpaka ku maso kuti umaliseche wanu uwonekere.
27 El liyena ke kom oru ma El srunga. El liye ke kom fahsr tukun god lun mwet pegan fin inging ac acn tupasrpasr, oana sie mukul su rapkui mutan kien mwet tulan lal, ku oana soko horse mukul mwel horse mutan. We nu suwos, mwet Jerusalem! Kowos ac nasnasla ngac?
Ndaona zonyansa zanu: zigololo zanu, kutchetcherera kwanu ndi ziwerewere zanu, zochitika pa mapiri ndi mʼminda. Tsoka iwe Yerusalemu! Udzakhala wosayeretsedwa pa zachipembedzo mpaka liti?”

< Jeremiah 13 >