< Isaiah 56 >

1 LEUM GOD El fahk nu sin mwet lal, “Oru ma suwohs ac pwaye, mweyen ac tia paht nga ac molikowosla.
Yehova akuti, “Chitani chilungamo ndi zinthu zabwino, chifukwa chipulumutso changa chili pafupi ndipo ndidzakuwombolani posachedwapa.
2 Nga fah akinsewowoyalos su karinganang len Sabbath ac tia aklusrongtenye. Nga fah akinsewowoyalos su tia oru kutena ma koluk.”
Ndi wodala munthu amene amachita zimenezi, munthu amene amalimbika kuzichita, amene amasunga Sabata osaliyipitsa, ndipo amadziletsa kuchita zoyipa.”
3 Sie mwetsac su weang mwet lun God elan tia fahk mu, “LEUM GOD El tia lela ngan wi mwet lal uh alu.” Sie eunuch elan tia nunku mu el tia ku in wi oaoala nu ke mwet lun God ke sripen el tia ku in orek tulik.
Mlendo amene waphatikana ndi Yehova asanene kuti, “Ndithu Yehova wandichotsa pakati pa anthu ake.” Ndipo munthu wofulidwa asanene kuti, “Ine ndine mtengo wowuma basi.”
4 LEUM GOD El fahk nu sin kain mukul se ingan, “Kom fin akfulatyeyu ke kom karinganang len Sabbath, ac kom fin oru ma nga lungse ac oaru in liyaung wuleang luk,
Popeza Yehova akuti, “Wofulidwa amene amasunga masabata anga, nachita zokomera Ine ndi kusunga pangano langa,
5 na inem ac fah esamyuk in Tempul luk oayapa inmasrlon mwet luk, paht liki na funu oasr wen ac acn nutum. Kom ac fah tiana mulkinyukla.”
ndidzawapatsa dzina ndi mbiri yabwino mʼkati mwa Nyumba yanga ndi makoma ake, kuposa kukhala ndi ana aamuna ndi aakazi. Ndidzawapatsa dzina labwino, losatha ndi losayiwalika.”
6 Na LEUM GOD El fahk nu sin mwetsac su wela mwet lal, su lungse El ac kulansupwal, su akfulatye len Sabbath ac oaru in liyaung wuleang lal:
Yehova akuti, “Alendo amene amadziphatika kwa Yehova, motero kuti amamutumikira Iye, amakonda dzina la Yehova, amamugwirira ntchito, komanso kusunga Sabata osaliyipitsa ndi kusunga bwino pangano langa,
7 “Nga fah uskowosme nu Zion, fineol mutal luk, ac akenganye kowos in iwen pre sik, ac nga fah insewowo in eis mwe kisa ma kowos kisakin fin loang luk. Tempul sik fah pangpang iwen pre nu sin mwet in mutunfacl nukewa.”
amenewa Ine ndidzawafikitsa ku phiri langa lopatulika, ndidzawapatsa chimwemwe mʼnyumba yanga ya mapemphero. Zopereka zawo zopsereza ndi nsembe zawo ndidzazilandira pa guwa langa la nsembe. Paja nyumba yanga idzatchedwa nyumba ya mapemphero ya anthu a mitundu yonse.”
8 LEUM GOD Fulatlana, su folokonma mwet Israel lal nu yen selos liki sruoh, El wulela mu El ac use kutu pac mwet sayalos in welulosyang.
Ambuye Yehova, amene amasonkhanitsa Aisraeli onse ali ku ukapolo akunena kuti, “Ndidzasonkhanitsano anthu ena kuwonjezera amene anasonkhana kale.”
9 LEUM GOD El fahk nu sin mutunfacl saya uh in tuku oana kosro lemnak ac kangla mwet lal.
Bwerani, inu zirombo zonse zakuthengo, inu nonse zirombo zamʼnkhalango bwerani mudzadye!
10 El fahk, “Mwet kol nukewa, su ma kunalos in sensenkakin mwet luk, elos kun! Wangin ma elos etu. Elos oana kosro ngalngul in soan ma tiana wowo — elos oanna ac mweme. Elos lungse na pwaye motul!
Atsogoleri onse a Israeli ndi akhungu, onse ndi opanda nzeru; onse ndi agalu opanda mawu, samatha kuwuwa: amagona pansi nʼkumalota amakonda kugona tulo.
11 Elos oana kosro oasroasr in mongo ma tia etu kihpi. Mwet kol inge wangin etauk lalos. Kais sie selos oru na ma elos lungse, ac suk na ma ac wo nu selos sifacna.
Ali ngati agalu amene ali ndi njala yayikulu; sakhuta konse. Abusa nawonso samvetsa zinthu; onse amachita monga akufunira, aliyense amafunafuna zomupindulitsa iye mwini.
12 Mwet sruhi inge elos fahk, ‘Use kutu wain an kut in nim na ke kuiyasr! Len lutu uh ac fah wo liki na misenge!’”
Aliyense amafuwulira mnzake kuti, “Bwera, tiye timwe vinyo! Tiyeni timwe mowa mpaka kukhuta! Mawa lidzakhala ngati leroli, kapena kuposa lero lino.”

< Isaiah 56 >