< Isaiah 54 >

1 Jerusalem, meet kom tuh oana sie mutan wangin tulik natu. A inge kom ku in on ac sasa ke engan, Mweyen ac fah pus tulik nutum Liki sie mutan su mukul tuma tiana som lukel.
“Sangalala, iwe mayi wosabala, iwe amene sunabalepo mwana; imba nyimbo, ndi kufuwula mwachimwemwe, iwe amene sunamvepo ululu wa pobereka; chifukwa mkazi wosiyidwa adzakhala ndi ana ambiri kuposa mkazi wokwatiwa,” akutero Yehova.
2 Akyokyelik lohm nuknuk sum an; Akloesyalik sucl kac, ac akkeyala kwi ma sruok sucl an!
Kulitsa malo omangapo tenti yako, tambasula kwambiri nsalu zake, usaleke; talikitsa zingwe zako, limbitsa zikhomo zako.
3 Kom fah kulelik masrol lom ke siska nukewa; Mwet lom ac fah sifil eis facl ma Mutunfacl saya muta fac in pacl inge. Siti ma wangin mwet we in pacl inge ac fah tingtingi ke mwet.
Pakuti udzasendeza malire ako kumanja ndi kumanzere; ndipo zidzukulu zako zidzalanda dziko la anthu a mitundu ina ndipo zidzakhala mʼmizinda yawo yosiyidwa.
4 Nimet sangeng — kom ac fah tia sifilpa akmwekinyeyuk; Kom ac fah tia sifilpa akpusiselyeyuk. Ac fah mulkinyukla tafongla lom ke pacl lom payuk fusr, Ac oayapa supwar lom ke kom katinmas.
“Usachite mantha; sadzakunyozanso. Usakhumudwe; sudzapeputsidwanso. Udzayiwala za manyazi zimene zinakuchitikira nthawi ya unyamata wako ndipo za manyazi zimene zinakuchitikira pa nthawi ya umasiye wako sudzazikumbukanso.
5 El su orekomla El ac oana sie mukul tuma nu sum — LEUM GOD Kulana pa Inel. God mutal lun Israel fah molikomla — El pa leumi faclu nufon.
Pakuti Mlengi wako ali ngati mwamuna wako, dzina lake ndi Yehova Wamphamvuzonse. Woyerayo wa Israeli ndiye Mpulumutsi wanu; dzina lake ndi Mulungu wa dziko lonse lapansi.
6 Israel, kom oana sie mutan payuk fusr Su mukul tumal el sisella, ac arulana toasr insia. Tusruktu LEUM GOD El pangonkomme nu yorol ac fahk:
Yehova wakuyitananso, uli ngati mkazi wosiyidwa ndi wodzaza ndi chisoni mu mtima, mkazi amene anakwatiwa pa unyamata wake kenaka nʼkukanidwa,” akutero Mulungu wako.
7 “Nga tuh siskomla ke kitin pacl, A ke pakoten lulap luk, nga fah sifil eiskom.
“Kwa kanthawi kochepa, Ine ndinakusiya, koma ndidzakutenganso chifukwa ndimakukonda kwambiri.
8 Nga tuh kasrkusrak ac ngetla liki kom ke kitin pacl, Tusruktu inge nga fah fahkak lungse kawil luk nu sum.” Pa inge ma LEUM GOD su molikomla El fahk.
Ndinakufulatira kwa kanthawi kochepa ndili wokwiya kwambiri. Koma ndi kukoma mtima kwanga kwa muyaya, ndidzakuchitira chifundo,” akutero Yehova Mpulumutsi wako.
9 “In pacl lal Noah nga tuh wulela mu Fahlu ac tiana sifilpa musalla ke sronot. Inge nga wulela in tiana sifil kasrkusrak sum. Nga fah tia sifilpa mulat nu sum ku kai kom.
“Kwa ine zimenezi zili ngati mmene zinalili mʼnthawi ya Nowa. Monga ndinalumbira nthawi imeneyo kuti sindidzawononganso dziko lapansi ndi madzi. Kotero tsopano ndalumbira kuti sindidzakupseraninso mtima, sindidzakudzudzulaninso.
10 Eol uh ac inging uh ku in mokukla, A lungse luk nu sum fah tiana safla; Nga fah liyaung wuleang in misla luk nwe tok.” LEUM GOD su lungse kom El fahk ouinge.
Ngakhale mapiri atagwedezeka ndi zitunda kusunthidwa, koma chikondi changa chosasinthika pa iwe sichidzatha. Pangano langa lamtendere silidzasintha,” akutero Yehova amene amakuchitira chifundo.
11 LEUM GOD El fahk, “O Jerusalem, sie siti keok su musalla tukun paka se Ac wangin mwet in akwoye kom, Nga fah sifil musaeak pwelung lom ke eot saok.
“Iwe mzinda wozunzika, wokunthidwa ndi namondwe ndiponso wopanda wokutonthoza, Ine ndidzakongoletsa miyala yako. Maziko ako ndidzamanga ndi miyala ya safiro.
12 Nga fah musai tower lom ke eot ruby, Ac mutunpot sum ke eot saromrom oana e, Ac pot ma raunikomyak ke wek saok.
Ndidzamanga nsanja zako zankhondo ndi miyala yokongola ya rubi. Ndidzamanga zipata zako ndi miyala yonyezimira ngati moto, ndipo linga lako lonse lidzakhala la miyala yamtengowapatali.
13 “Nga ac fah sifacna luti mwet lom, Ac oru tuh elos in kapkapak ac moul in misla.
Yehova adzaphunzitsa ana ako onse, ndipo ana ako adzakhala ndi mtendere wochuluka.
14 Suwoswos ac pwaye ac fah oru kom in ku. Kom ac fah tia pulakin mwe keok ac mwe aksangang.
Udzakhazikika mʼchilungamo chenicheni: Sudzakhalanso wopanikizika, chifukwa sudzaopa kanthu kalikonse. Sudzakhalanso ndi mantha chifukwa manthawo sadzafika pafupi ndi iwe.
15 Fin oasr kutena mwet mweuni kom, El oru ke tia ma nga sapkin. Ac fah kutangyukla kutena mwet su mweun lain kom.
Ngati wina adzakuthirani nkhondo, si ndine amene ndachititsa; aliyense amene adzalimbana nanu adzagonja chifukwa cha iwe.
16 “Nga pa orala mwet orekma ke osra, Su tanak sie e ac orala kufwen mwe mweun. Nga pac pa orala mwet mweun, Su orekmakin kufwen mwe mweun in uniya mwet.
“Taona, ndi Ine amene ndinalenga munthu wosula zitsulo amene amakoleza moto wamakala ndi kusula zida zoti azigwiritse ntchito. Ndipo ndine amene ndinalenga munthu wosakaza kuti awononge;
17 Tusruktu wangin kufwen mwe mweun ac fah kunauskomla. Ac fah oasr top lom nu selos nukewa su akkolukye kom. Nga fah loango mwet kulansap luk Ac oru tuh elos in kutangla.” LEUM GOD pa fahk ma inge.
palibe chida chopangidwa ndi mdani chimene chidzakupweteke, ndipo onse okuneneza pa mlandu udzawatsutsa. Umu ndimo adzapezekere atumiki a Yehova. Chipambano chawo chichokera kwa Ine,” akutero Yehova.

< Isaiah 54 >

A Dove is Sent Forth from the Ark
A Dove is Sent Forth from the Ark