< Isaiah 27 >

1 In len sac LEUM GOD El ac orekmakin cutlass kulana natul in kalyael Leviathan, dragon soko ma tipirpir ac worwor, ac El ac uniya kosro sulallal lulap soko in meoa uh.
Tsiku limenelo, Yehova ndi lupanga lake lakuthwa, lalikulu ndi lamphamvu, adzalanga Leviyatani chinjoka chothawa chija, Leviyatani chinjoka chodzikulunga; adzapha chirombo choopsa cha mʼnyanja.
2 In len sac LEUM GOD El fah fahk ke ima in grape kato se lal,
Tsiku limenelo Yehova adzati, “Tidzayimba nyimbo ya munda wamphesa wobereka bwino:
3 “Nga liyaung ac aksroksrokye pacl nukewa. Nga liyaung na ke len ac fong, tuh in wangin mwet akkolukye.
Ine, Yehova, ndimawuyangʼanira; ndimawuthirira nthawi zonse. Ndimawulondera usana ndi usiku kuti wina angawononge.
4 Nga tila kasrkusrak ke ima grape sac. Funu oasr kokul ku mah fakfuk nga in lain, nga lukun seukak nufon.
Ine sindinakwiye. Ngati mkandankhuku ndi minga zikanaoneka ndikanalimbana nazo! Ndikachita nazo nkhondo; ndikanazitentha zonse ndi moto.
5 Tusruktu mwet lokoalok lun mwet luk fin lungse nga in karinganulosyang, lela elos in tuku auliyak nu sik. Aok, lela elos in suk misla yuruk.”
Koma ngati apo ayi, abweretu kwa Ine adani angawo kuti ndidzawateteze; apangane nane za mtendere, ndithu, apangane nane za mtendere.”
6 In kutu pacl fa hsru, mwet Israel — filin tulik natul Jacob — fah okahla oana soko sak, ac elos fah fokla ac farengelik. Faclu ac fah afla ke fahko lalos.
Masiku akubwerawo Yakobo adzazika mizu, Israeli adzaphukira ndi kuchita maluwa, ndipo adzadzaza dziko lonse lapansi ndi zipatso.
7 Mwet Israel tiana kaoyeiyuk sin LEUM GOD in upa oana mwet lokoalok lalos, ac tia pac us mwet lalos tuhlac.
Kodi Yehova anakantha Israeli ngati momwe anakanthira anthu amene anazunza Israeli? Kapena kodi Yehova anapha Israeli ngati mmene anthu ena anaphera Israeli?
8 LEUM GOD El kalyei mwet lal ke El supwalosla nu in ssruoh. El pokolosla ke sie eng na upa kutulap me.
Yehova mwawalanga powapirikitsa ndi kuwatumiza ku ukapolo, mwawachotsa ndi mpweya wanu woopsa, monga zimachitikira pa tsiku la mkuntho wochokera kummawa.
9 Tusruktu ma koluk lun Israel ac fah tuleyukla ke pacl se na eot ke loang lun mwet pegan uh ilili nwe ke mokutkuti, ac ma sruloala ke god mutan Asherah, oayapa loang in esukak mwe keng uh, wanginla.
Yehova adzakhululuka kulakwa kwa Yakobo. Iwo adzaonetsa kuti alapadi pamene adzaphwanya miyala yonse ya guwa lachikunja, ngati mmene anthu amaphwanyira miyala yanjereza mpaka kukhala ngati fumbi lokhalokha. Sipadzapezekanso mafano a Asera kapena maguwa ofukiza lubani.
10 Siti ma tuh oasr pot ku we musallana oan — oana sie scn mwesis ma wangin kutena ma we. Ekla oana sie acn cow uh mongla ac mongo mah ac lesak we.
Mzinda wamalinga uja wasanduka bwinja, wasanduka malo osiyidwa, ndi kutayidwa ngati chipululu; kumeneko amadyetselako ana angʼombe kumeneko zimapumulako ziweto ndi kumwetula nthambi za mitengo kotheratu.
11 Lesak uh paola ac kaptelik, na mutan uh telani mwe etong. Ke sripen wangin etauk lun mwet uh, oru God su oralosla El fah tia pakomutalos ku akkalemye pakoten lal nu selos.
Pamene nthambi za mitengoyo zauma, zimathyoka ndipo amayi amabwera nazitola ndi kuzisandutsa nkhuni. Pakuti awa ndi anthu opanda nzeru; kotero Mulungu amene anawapanga sadzachitira chisoni, ndipo Mlengi wawo sawakomera mtima.
12 Ke len sac, LEUM GOD El ac fah eisani mwet lal kais sie, oana ke srisrielik wheat liki kulun wheat uh, mutawauk Infacl Euphrates lac nwe sisken Egypt.
Tsiku limenelo Yehova adzasonkhanitsa pamodzi anthu ake mmodzimmodzi kumalo opunthira tirigu, kuchokera ku mtsinje wa Yufurate mpaka ku mtsinje wa ku Igupto.
13 In len sac, sie ukuk ac fah ukuki in folokonma mwet Israel nukewa su muta in sruoh in acn Assyria ac Egypt. Elos fah tuku ac alu nu sin LEUM GOD in Jerusalem, fin eol mutal sel.
Ndipo tsiku limenelo lipenga lalikulu lidzalira. Amene akuzunzika ku Asiriya iwo amene ali ku ukapolo ku Igupto adzabwera ndi kudzalambira Yehova pa phiri lopatulika mu Yerusalemu.

< Isaiah 27 >