< Isaiah 23 >

1 Kas in fahkak inge ma ke acn Tyre. Wowoyak ac asor, kowos mwet kalkal fin meoa! Acn suwos, Tyre, kunausyukla; lohm we ac molsron we wanginla. Ke oak okowos ac foloko liki acn Cyprus, kowos ac fah lohng pweng kac.
Uthenga wonena za Turo: Lirani mofuwula, inu oyendetsa sitima za pa madzi za ku Tarisisi: pakuti mzinda wa Turo wawonongedwa ndipo mulibe nyumba kapena dooko. Zimenezi anazimva pochokera ku Kitimu.
2 Kowos in tung mwemelil, kowos mwet kuka lun Sidon! Kowos supu mwet
Khalani chete inu anthu okhala mʼmbali mwa nyanja, inu amalonda a ku Sidoni, iwe amene unalemera ndi anthu oyenda pa nyanja.
3 in tupalla meoa in moli ac kukakin wheat ma kap ke acn Shihor sisken infacl Nile in acn Egypt, ac in oru inkanek in kuka lalos yurin mutunfacl puspis.
Pa nyanja zazikulu panabwera tirigu wa ku Sihori; zokolola za ku Nailo, ndipo munachita malonda ndi anthu a mitundu ina.
4 Siti Sidon, kom akmwekinyeyukla! Meoa ac acn loallana meoa siskomla ac fahk, “Wanginna tulik nga oswela. Nga soenna tufahla wen ku acn.”
Chita manyazi, iwe Sidimu pakuti nyanja yayankhula, linga la ku nyanja (Turo) layankhula kuti, “Sindinamvepo zowawa za kubereka kapena kuberekapo mwana; sindinalerepo ana aamuna kapena kulera ana aakazi.”
5 Finne mwet Egypt elos ac fah lut ac oela pacl se elos lohng lah kunausyukla acn Tyre.
Mawuwa akadzamveka ku Igupto, iwo adzachita mantha akadzamva kuti Turo wawonongeka.
6 Mwet Phoenicia, kowos in wowoyak ac tung! Srike in kaing nu Tarshish!
Wolokerani ku Tarisisi, lirani mofuwula, inu anthu okhala mʼmbali mwa nyanja.
7 Mea pwaye lah pa inge Tyre, siti na pwar se ma musaiyukla ke pacl na loes somla? Ya pa inge siti se ma supwala mwet in tupalla meoa ac eis acn ingo tuh in acn selos?
Kodi uwu si mzinda wachisangalalo uja, mzinda wakalekale, umene anthu ake ankapita kukakhala ku mayiko akutali?
8 Su lumahla tuh mwe ongoiya inge nukewa in sikyak nu fin acn Tyre, siti fulat sac, su mwet kuka we elos fisrak ac akfulatyeyuk emeet fin faclu?
Kodi ndani anakonza zimenezi kuti zigwere Turo, mzinda umene unakhazikitsa mizinda ina, mzinda umene amalonda ake ndi akalonga ndi otchuka pa dziko lapansi?
9 LEUM GOD Kulana pa lumahla. El oru in tulokinya filang lalos ke ma elos orala, ac in aktonongyala mwet fulat lalos.
Yehova Wamphamvuzonse anakonza zimenezi kuti athetse kunyada kwawo ndi kutsitsa anthu otchuka a pa dziko lapansi.
10 Fahla ac orek ima, kowos mwet Tyre su muta in acn Tarshish! Wangin sie ac fah sifil loangekowos.
Mubalalike mʼdziko mwanu ngati mtsinje wa Nailo inu anthu a ku Tarisisi, pakuti mulibenso chokutetezani.
11 LEUM GOD El asroela paol fin meoa ac kutangla tokosrai uh. El sap tuh pot ku lun Phoenicia in kunausyukla.
Yehova watambasula dzanja lake kuloza ku nyanja ndipo wagwedeza maufumu ake. Iye walamula kuti Kanaani agwetse malinga ake.
12 Siti Sidon, insewowo lom safla, ac mwet lom akkeokyeyuk. Elos finne kaing nu Cyprus, elos ac tiana konauk misla we.
Iye anati, “Simudzakondwanso konse, inu anthu opanikizidwa a ku Sidoni, tsopano wamphwanyidwa! “Ngakhale muwolokere ku Kitimu, kumeneko simukapezako mpumulo.”
13 (Tia mwet Assyria pa oru kosro lemnak uh in utyak ac nwakla acn Tyre, a mwet Babylonia. Mwet Babylonia pa tulokunak nien fan sisken pot we, ac fukulya acn ku lun Tyre, ac sisla in oan musalla.)
Onani dziko la Ababuloni, anthu amenewa tsopano atheratu! Asiriya asandutsa Turo kukhala malo a zirombo za ku chipululu; anamanga nsanja zawo za nkhondo, anagumula malinga ake ndipo anawasandutsa bwinja.
14 Wowoyak ac asor, kowos mwet kalkal meoa uh! Kunausyukla siti se ma kowos kukin.
Lirani mofuwula, inu anthu oyendetsa sitima za pa madzi za ku Tarisisi; chifukwa malinga ako agwetsedwa!
15 Pacl se ac tuku ke acn Tyre ac mulkinyukla ke yac itngoul, lusenna moul lun sie tokosra. Ke ac safla yac inge, acn Tyre ac fah oana mutan kosro se ke on soko ma fahk mu:
Pa nthawi imeneyo Turo adzayiwalika pa zaka 70, amene ndi masiku a moyo wa mfumu. Koma potsiriza pa zaka 70 zimenezi, Turo adzakhala ngati mkazi wachiwerewere woyimbidwa mu nyimbo:
16 Kom, mutan kosro se ma mulkinyukla, Eis harp nutum ac forfor in siti uh! Srital ac sifilpa onkakin on lom In sifil esamyukyak kom.
“Tenga zeze wako uzungulire mzinda, iwe mkazi wachiwerewere woyiwalika; imba zeze mokometsera, imba nyimbo zambiri, kuti anthu akukumbukire.”
17 Ke yac itngoul ac safla, LEUM GOD El ac lela Tyre in folokla nu ke inkanek in kuka matu lal, ac el ac fah kukakunulla sifacna nu sin tokosrai nukewa lun faclu.
Pakutha pa zaka 70, Yehova adzachitapo kanthu pa Turo. Iye adzabwerera ku ntchito yake yakale monga mkazi wachiwerewere ndipo adzachita zachiwerewere ndi maufumu onse a dziko lapansi.
18 Mani ma el sruokya ke kuka lal uh ac fah kisaiyukyang nu sin LEUM GOD. Acn Tyre ac fah tia elosak ma inge nu sel sifacna ku filiya in nien filma lal, a ac fah orekmakinyuk in kasrelos su lafwekunulosla nu sin LEUM GOD, in akfalye enenu lalos ke mwe mongo ac nuknuk lalos.
Koma phindu lake ndi malipiro ake adzazipereka kwa Yehova; sadzazikundika kapena kuzisunga. Phindu lake lidzapita kwa mtumiki wa Yehova kuti agule zakudya zambiri ndi zovala zokongola.

< Isaiah 23 >