< Isaiah 18 >

1 Layen nu roto ke infacl in acn Ethiopia, oasr sie facl lohngyuk pusren posohksok we.
Tsoka kwa anthu a ku Kusi. Kumeneko kumamveka mkokomo wa mapiko a dzombe.
2 Mwet roso fulat elos kal tuku liki facl sac ke Infacl Nile fin oak okoalos orekla ke loa. Folokla nu yen suwos, kowos mwet utuk kas mulah! Us sap soko nu in facl suwos ma masrloeyukelik ke infacl puspis. Facl suwos yohk ac ku. Mwet we elos loeska ac fwel manolos, ac mutunfacl uh nufon sangeng selos.
Dziko limenelo limatumiza akazembe pa mtsinje wa Nailo, mʼmabwato amabango amene amayandama pa madzi, ndikunena kuti, “Pitani, inu amithenga aliwiro, kwa mtundu wa anthu ataliatali a khungu losalala, ndi woopedwa ndi anthu. Akazembe anatumidwa ku dziko la anthu amphamvu ndi logonjetsa anthu ena. Dziko lawo ndi logawikanagawikana ndi mitsinje.”
3 Kowos nukewa su muta faclu, kowos in lohng akwoya! Kowos in tawi flag in mweun se ma ac amacyak fin mangon eol uh! Porongo pusren mwe ukuk fin kasla!
Inu nonse anthu a pa dziko lonse, inu amene mumakhala pa dziko lapansi, pamene mbendera yakwezedwa pa mapiri yangʼanani, ndipo pamene lipenga lilira mumvere.
4 LEUM GOD El fahk nu sik, “Nga ac fah ngeti inkusrao me, ac misla oana usren fol ke faht uh, fol ke faht uh, ku oana sikyak lun aunfong ke pacl in kosrani.
Pakuti Yehova akunena kwa ine kuti, “Ndili chikhalire ku malo anga kuno, ndidzakhala chete, ndi kumangoyangʼana, monga momwe dzuwa limawalira nthawi yotentha, monganso momwe mame amagwera usiku pa nthawi yotentha yokolola.”
5 Meet liki orekeni grape uh, ke ros farengla nukewa putatla ac grape uh mwesrla, mwet lokoalok fah kunausla mwet Ethiopia — fisrasr oana ke sie mitmit ac pakela lah ke oa in grape uh.
Pakuti, anthu asanayambe kukolola, maluwa atayoyoka ndiponso mphesa zitayamba kupsa, Iye adzadula mphukira ndi mipeni yosadzira, ndipo adzadula ndi kuchotsa nthambi zotambalala.
6 Monin mwet mweun lalos ac fah sisila nun won ac kosro lemnak uh. In pacl fol won uh ac fah kang manolos, ac in pacl mihsrisr kosro lemnak uh ac kang manolos.”
Mitembo ya anthu ankhondo adzasiyira mbalame zamʼmapiri zodya nyama ndiponso zirombo zakuthengo; mbalame zidzadya mitemboyo nthawi yonse ya chilimwe, ndipo zirombo zidzayidya pa nthawi yonse yachisanu.
7 Pacl se ac tuku ke mwet loeska ac fwel mano inge, su mutunfacl uh nufon sangeng se, elos ac us mwe sang lalos nu sin LEUM GOD Kulana liki facl yohk ac ku se inge ma masrloeyukelik ke infacl puspis. Elos ac fah tuku nu ke Eol Zion, yen mwet uh alu nu sin LEUM GOD Kulana we.
Pa nthawi imeneyo anthu adzabwera ndi mphatso kwa Yehova Wamphamvuzonse, zochokera kwa anthu ataliatali ndi osalala, kuchokera kwa mtundu wa anthu woopedwa ndi anthu apafupi ndi akutali omwe, mtundu wa anthu amphamvu ndi a chiyankhulo chachilendo, anthu amene dziko lawo ndi logawikanagawikana ndi mitsinje. Adzabwera nazo mphatso ku Phiri la Ziyoni, ku malo a Dzina la Yehova Wamphamvuzonse.

< Isaiah 18 >