< Isaiah 15 >
1 Sie kas in fahkak ke acn Moab pa inge. Siti lun Ar ac Kir ac kunanula ke fong sefanna, na ac fah arulana misla acn Moab.
Uthenga wonena za Mowabu: Popeza kuti mu usiku umodzi wokha mzinda wa Ari wa ku Mowabu wawonongedwa, wawonongedwa pa usiku umodzi wokha. Mzinda wa Kiri wawonongedwa, wawonongedwa pa usiku umodzi wokha.
2 Mwet Dibon elos fanyak nu fineol uh in tung in acn in alyalu lalos. Mwet Moab elos wowoyak ac tung tutaf ke sripen asor lalos ke siti Nebo ac Medeba. Elos mangsrasrala ac kalla alut lalos.
Anthu a ku Diboni akupita ku nyumba ya milungu yawo, akupita ku malo awo achipembedzo kukalira; anthu a ku Mowabu akulirira mofuwula mzinda wa Nebo ndi wa Medeba. Mutu uliwonse wametedwa mpala, ndipo ndevu zonse zametedwa.
3 Mwet inkanek uh elos asor ac nokomang nuknuk yohk eoa. Mwet uh tung ke nien tukeni in siti uh, ac fin lohm uh.
Mʼmisewu akuvala ziguduli; pa madenga ndi mʼmabwalo aliyense akulira mofuwula, misozi ili pupupu.
4 Mwet Heshbon a Elealeh elos wowoyak, ac pusren tung lalos ku in lohngyuk yen loessula nwe Jahaz. Finne mwet mweun uh, elos rarrar pac ke elos lohng, ac wanginla pulaik lalos.
Anthu a ku Hesiboni ndi Eleali akulira mofuwula, mawu awo akumveka mpaka ku Yahazi. Kotero asilikali a ku Mowabu akulira mofuwula, ndipo ataya mtima.
5 Insiuk tungi acn Moab! Mwet we elos kaingla nu in siti Zoar ac nu Eglath Shelishiyah. Kutu mwet uh fanyak ke inkanek nu Luhith, fahsr na tung; ac kutu kaingla nu Horonaim, arulana wowoyak ke asor.
Inenso ndikulirira Mowabu; chifukwa othawa nkhondo ake akupita akulira ku chikweza cha Luluti mpaka ku Zowari ndi Egilati-Selisiya akupita akulira ku chikweza cha Luhiti, Akulira mosweka mtima pa njira yopita ku Horonaimu; akulira mosweka mtima chifukwa cha chiwonongeko chawo.
6 Infacl srisrik Nimrim paola, ac mah siska uh uli. Wanginla mah folfol lula we.
Madzi a ku Nimurimu aphwa ndipo udzu wauma; zomera zawonongeka ndipo palibe chomera chobiriwira chatsala.
7 Mwet uh fahsr sasla Infahlfal Willow, ac srike in kaing wi ma lalos nukewa.
Kotero kuti chuma chomwe anachipeza ndi kuchisunga, achitenga kuti awoloke nacho chigwembe cha Misondozi.
8 Ke masrol nukewa lun acn Moab, tung uh lohngyuk we. Lohngyuk pac in siti Eglaim ac Beerelim.
Kulira kwawo kukumveka mʼdziko lonse la Mowabu; kulira kwawo kosweka mtima kukumveka mpaka ku Egilaimu ndi Beeri-Elimu.
9 Kof ke infacl soko in acn Dibon, srusrala ke srah, na srakna oasr ma upa liki inge ma God El akoo nu sin mwet in acn we. Aok, mwet nukewa su lula in acn Moab ac fah anwuki.
Madzi a ku Dimoni afiira ndi magazi, komabe ndidzabweretsa zina zambiri pa Dimoni, mkango woti udzagwire aliyense othawa mu Mowabu ndi aliyense wotsala mʼdzikomo.