< Isaiah 11 >
1 Takin sou fulat lal David oana sak soko ma pakpuki nu infohk uh; na, oana ke lah sasu ac srunak ke sruen sak uh, ouinge sie tokosra sasu fah tuyak liki inmasrlon fwilin tulik natul David.
Padzatuluka mphukira pa tsinde la Yese ndipo nthambi idzaphukira kuchokera ku mizu yake.
2 Ngunin LEUM GOD ac fah oan facl — Ngunin lalmwetmet ac etauk in leumi mwet lal. El ac fah etu ma lungse lun LEUM GOD ac arulana akfulatyal,
Mzimu wa Yehova udzakhala pa iye Mzimu wanzeru ndi wa kumvetsa zinthu, Mzimu wauphungu ndi wamphamvu, Mzimu wachidziwitso ndi wakuopa Yehova.
3 Ac El ac fah insewowo in aksol. Nununku lal fah tia wiwimwet ku wiwikas;
Ndipo kuopa Yehova ndiye chidzakhale chinthu chomukondweretsa. Iye sadzaweruza potsata zooneka pamaso, kapena kugamula mlandu potsata zakumva;
4 El ac fah oru nununku suwohs nu sin mwet sukasrup Ac loango suwohs lun mwet ma kofla sifacna. Ke sap lal, mwet uh fah kalyeiyuk, Ac mwet koluk fah misa.
koma amphawi adzawaweruza mwachilungamo, adzaweruza mwachilungamo mlandu wa anthu osauka a dziko lapansi. Iye adzakantha dziko lapansi ndi mawu ake; atalamula Iyeyu anthu oyipa adzaphedwa.
5 El fah leumi mwet lal ke pwaye ac suwoswoslana.
Chilungamo chidzakhala ngati lamba wake ndipo kukhulupirika kudzakhala ngati chomangira mʼchiwuno mwake.
6 Kosro wolf ac sheep fusr fah tukeni muta in misla, Ac leopard sulallal fah wi na nani fusr uh oan. Cow fusr ac lion fusr fah tukeni mongo Ac tulik srisrik fah ku in karingnalos.
Mʼmbulu udzakhala pamodzi ndi mwana wankhosa, kambuku adzagona pansi pamodzi ndi mwana wambuzi, mwana wangʼombe ndi mwana wa mkango adzadyera limodzi ndipo mwana wamngʼono adzaziweta.
7 Cow ac bear fah tukeni mongo, Ac cow fusr ac bear fusr natulos fah tukenina oan. Lion ac fah mongo mah, oana cow.
Ngʼombe yayikazi ndi chimbalangondo zidzadya pamodzi, ana awo adzagona pamodzi, ndipo mkango udzadya udzu ngati ngʼombe.
8 Finne tulik fusr se, ac fah tia sensen In srital apkuran nu yurin wet pwasin.
Mwana wakhanda adzasewera pa dzenje la mamba, ndipo mwana wamngʼono adzapisa dzanja lake ku phanga la mphiri osalumidwa.
9 Fin acn Zion, inging mutal lun God, Ac fah wangin mwe sensen ku ma koluk. Acn we ac fah sessesla ke mwet su arulana etu ke LEUM GOD Oana ke meoa uh nwanala ke kof.
Sipadzakhala chilichonse chopweteka kapena chowononga pa phiri lopatulika la Yehova, pakuti anthu a dziko lapansi adzadzaza ndi nzeru yotha kudziwa Yehova monga momwe nyanja imadzazira ndi madzi.
10 Len se ac fah tuku ke tokosra sasu, su sie sin fwilin tulik natul David, ac fah sie mwe akul nu sin mutunfacl puspis. Elos ac toeni in siti fulat sel ac akfulatyal.
Tsiku limenelo mfumu yatsopano yochokera pa Muzu wa Yese idzakhala ngati chizindikiro kwa anthu a mitundu yonse. Mitundu ya anthu idzasonkhana kwa Iye, ndipo malo awo okhalapo adzakhala aulemerero.
11 In len sac, Leum El ac sifilpa orekmakin ku lal in folokonma mwet lal su lula in acn Assyria ac Egypt, in acn Pathros, Ethiopia, Elam, Babylonia, Hamath, ac liki acn ma oan sisken meoa.
Tsiku limenelo Ambuye adzatambasula dzanja lake kachiwiri kuti awombole anthu ake otsalira ku Asiriya, ku Igupto, ku Patirosi, Kusi, ku Elamu, ku Sinana, ku Hamati ndi pa zilumba za nyanja yamchere.
12 Leum El ac fah kolak sie flag tuh in sie mwe akul nu sin mutunfacl uh lah El sifilpa eisani mwet lisyukla lun Israel ac Judah, ac folokunulosme liki eng akosr lun faclu.
Adzakwezera mitundu ya anthu mbendera, ndipo adzasonkhanitsa otayika a ku Israeli; Iye adzasonkhanitsa anthu obalalika a ku Yuda kuchokera ku mbali zonse zinayi za dziko lapansi.
13 Tokosrai lun Israel fah tia sifil kwase Judah, ac Judah fah tia sifilpa mwet lokoalok lun Israel.
Nsanje ya Efereimu idzatha, ndipo adani a Yuda adzatha; Efereimu sadzachitira nsanje Yuda, ngakhale Yuda sadzamuda Efereimu.
14 Elos ac tukeni mweuni acn Philistia layen nu roto, ac wapi mwet su muta layen nu kutulap. Elos ac kutangla mwet Edom ac mwet Moab, ac mwet Ammon fah aksolos.
Yuda ndi Efereimu adzathira nkhondo pa Afilisti mbali ya kumadzulo; ndipo onsewo pamodzi adzalanda zinthu za anthu a kummawa. Adzalimbana ndi Edomu ndi Mowabu, ndipo Aamoni adzawagonjera.
15 LEUM GOD El ac akmihnyela inalok ke Meoa Srusra, ac El ac use sie eng fol in akpaoyela Infacl Euphrates, ac filiya infacl srisrik itkosr na tuh mwet uh fah ku in tupalla.
Yehova adzaphwetsa mwendo wa nyanja ya Igupto; adzatambasula dzanja lake ndipo adzawombetsa mphepo yotentha pa mtsinje wa Yufurate. Iye adzawugawa mtsinjewo kukhala timitsinje tisanu ndi tiwiri kuti anthu athe kuwoloka powuma atavala nsapato.
16 Ac fah oasr soko inkanek lulap tuku liki acn Assyria nu sin mwet lal mwet Israel, su srakna moul oasr we, oana ke tuh orek nu sin mwet matu lalos ke elos tuku liki facl Egypt.
Padzakhala msewu waukulu woti ayendepo anthu ake otsalira amene anatsalira ku Asiriya, monga mmene panali msewu waukulu woyendapo Israeli pamene amachokera ku Igupto.