< Hosea 4 >

1 Oasr kas toasr lun LEUM GOD lain mwet su muta in acn se inge. Israel, porongo ma El fahk: “Wangin inse pwaye ku kulang fin acn uh, ac mwet uh tiana etu ke God.
Inu Aisraeli, imvani mawu a Yehova, chifukwa Yehova ali ndi mlandu ndi inu amene mumakhala mʼdzikoli: “Mʼdziko mwanu mulibe kukhulupirika, mulibe chikondi mulibe kulabadira za Mulungu.
2 Elos orala wulela ac kunausla. Elos kikiap, akmas, pisrapasr ac kosro. Ma koluk uh yokelik, ac akmas uh fususeni.
Muli kutemberera kokha, kunama ndi kupha. Kuba ndi kuchita chigololo; machimo achita kunyanya ndipo akungokhalira kuphana.
3 Ke ma inge kof fin acn uh ac fah wanginla, ac ma nukewa fin acn uh ac fah misa. Kain kosro nukewa ac won uh, oayapa ik, ac fah misa.”
Chifukwa chake dziko likulira ndipo onse amene amakhalamo akuvutika; zirombo zakuthengo ndi mbalame zamumlengalenga ndiponso nsomba zamʼnyanja zikufa.
4 LEUM GOD El fahk, “Kowos in tia sufan kutena mwet ku kaelos — kowos mwet tol pa nga lain uh.
“Koma wina asapeze mnzake chifukwa, wina aliyense asayimbe mlandu mnzake, pakuti anthu ako ali ngati anthu amene amayimba mlandu wansembe.
5 Kowos tukulkul na ke len ac fong, ac mwet palu elos oapana kowos, tukulkul na. Nga fah kunausla Israel, su nina kiowos.
Mumapunthwa usana ndi usiku ndipo aneneri amapunthwa nanu pamodzi. Choncho ndidzawononga amayi anu.
6 Mwet luk elos ac fah lisyukla mweyen wangin etu lalos keik. Kowos mwet tol, kowos tia pac eteyu, ac kowos pilesru luti luk. Ke ma inge, nga fah pilesrekowos ac nga fah tia akilen wen nutuwos su pangon mu elos mwet tol luk.
Anthu anga akuwonongeka chifukwa chosadziwa. “Pakuti mwakana kudziwa, Inenso ndidzakukanani monga ansembe anga; chifukwa mwayiwala lamulo la Mulungu wanu, Inenso ndidzayiwala ana anu.
7 “Ke pisen mwet tol uh puseni, ma koluk lainyu uh yokelik pac; ke ma inge nga fah ekulla fulat lowos nu ke mwekin.
Ansembe ankati akachuluka iwo ankandichimwiranso kwambiri; iwo anasinthanitsa ulemerero wawo ndi chinthu china chonyansa.
8 Kowos kasrupi ke sripen ma koluk lun mwet luk, ouinge kowos lungse tuh ma koluk lalos in yokelik na.
Amalemererapo pa machimo a anthu anga ndipo amafunitsitsa kuti anthuwo azipitiriza kuchimwa.
9 Mwe kai nu sin mwet uh ac fah orek pac nu suwos. Nga fah kai kowos ac kowos fah eis molin ma koluk lowos.
Ndipo zidzakhala motere: zochitikira anthu ena, zidzachitikiranso ansembe. Ndidzawalanga onsewo chifukwa cha njira zawo, ndidzawabwezera chifukwa cha machitidwe awo.
10 Kowos fah mongo ac tia kihpi. Kowos fah orek kosro ke nien alu lun mwet pegan in oasr tulik nutuwos, tuh ac fah wangin tulik nutuwos, mweyen kowos forla likiyu in fahsr tukun god saya.”
“Iwo azidzadya koma sadzakhuta; azidzachita zachiwerewere koma sadzachulukana, chifukwa anasiya Yehova kuti adzipereke
11 LEUM GOD El fahk, “Wain mah ac wain sasu, kewa na akwelye nunak lun mwet luk.
ku zachiwerewere, ku vinyo wakale ndi watsopano, zimene zimachotsa nzeru zomvetsa zinthu
12 Elos sukok kas in kasru sin sie polosak! Ac elos nunku mu soko sikal sak ku in fahk nu selos ma elos ke etu. Elos sisyula. Oana sie mutan su orek kosro ac eis molin kosro lal, elos eisalosyang sifacna nu sin god ngia.
za anthu anga. Anthu anga amapempha nzeru ku fano lamtengo ndipo ndodo yawo yamtengo imawayankha. Mzimu wachiwerewere umawasocheretsa; iwo sakukhulupirika kwa Mulungu wawo.
13 Elos oru kisa lalos ke nien alyalu fin mangon eol uh, ac esukak mwe keng yen lullul ye sak lulap fin inging uh. “Ke ma inge acn nutuwos elos orek kosro in eis molo, ac mutan kien wen nutuwos elos orek kosro.
Amapereka nsembe pamwamba pa mapiri ndi kufukiza lubani pa zitunda, pa tsinde pa mtengo wa thundu, mnjale ndi mkundi, pamene pali mthunzi wabwino. Nʼchifukwa chake ana anu aakazi akuchita zachiwerewere ndipo akazi a ana anu akuchita zigololo.
14 Tusruk, nga ac fah tia kaelos ke ma elos oru inge, mweyen kowos sifacna fahsri mutan kosro ke nien alu lun mwet pegan ac orek kisa yorolos. Oana soakas se ma fahk mu, ‘Mutanfahl se ma wangin etauk la ac fah musalla.’
“Ine sindidzalanga ana anu aakazi pamene iwo adzachita zachiwerewere, kapena akazi a ana anu pamene adzachita zigololo. Paja inu nomwe amunanu mumayenda ndi akazi achiwerewere, ndipo mumapereka nsembe pamodzi ndi akazi achiwerewere a ku malo opembedzerako. Anthu amene alibe nzeru adzawonongeka ndithu!
15 “Kowos mwet Israel finne tia inse pwaye nu sik, lela mwet Judah in tia tafongla ke lumah sac pacna. Nimet alu in acn Gilgal ku Bethaven, ku orek wulela we ke Inen LEUM GOD moul.
“Ngakhale umachita chigololo, iwe Israeli, Yuda asapezeke ndi mlandu wotere. “Usapite ku Giligala. Usapite ku Beti-Aveni. Ndipo usalumbire kuti, ‘Pali Yehova wamoyo!’
16 Mwet Israel elos srangesr lohng kas oana soko cow fusr. Nga ac ku in kitalos fuka oana sheep fusr in imae?
Aisraeli ndi nkhutukumve, ngosamva ngati ana angʼombe. Kodi Yehova angathe kuwaweta bwanji ngati ana ankhosa pa msipu wabwino?
17 Mwet Israel elos oan ye ku lun ma sruloala. Tari, sang lungse laltal.
Efereimu waphathana ndi mafano; mulekeni!
18 Ke pacl elos arulana sruhila ke nim wain, elos orek pwar yurin mutan kosro su kukakin manolos; ouinge elos pilesrala fulat lalos ac sifacna akmwekinyalos.
Ngakhale pamene zakumwa zawo zatha, amapitiriza kuchita zachiwerewere; atsogoleri awo amakonda kwambiri njira zawo zochititsa manyazi.
19 Elos fah ukyukla oana ke ku lun eng uh okla ma uh, ac elos fah mwekin ke mwe kisa pegan ma elos oru.”
Adzachotsedwa ndi kamvuluvulu ndipo adzachita manyazi chifukwa cha nsembe zawo.

< Hosea 4 >