< Genesis 6 >

1 Ke mwet uh fahsrelik nu yen nukewa faclu, ac oasr tulik mutan osweyukla,
Anthu atayamba kuchuluka pa dziko lapansi ndi kubereka ana aakazi,
2 kutu sin mwet lucng liyauk lah tulik mutan inge oasku, ouinge elos payukyak selos su elos lungse.
ana aamuna a Mulungu anaona kuti ana aakazi a anthuwo anali okongola. Ndipo anakwatira aliyense amene anamusankha.
3 Na LEUM GOD El fahk, “Nga fah tia fuhlela mwet uh in moul nwe tok — elos mano na sukawil. Ingela elos ac fah tia moul loes liki yac siofok longoul.”
Tsono Yehova anati, “Sindilola kuti chipwirikiti chikuchitikachi chipitirire mpaka muyaya, pakuti iye ndi munthu; masiku a moyo wake adzakhala zaka 120.”
4 In len ingo, aok finne kutu pacl toko, oasr mwet na lulap pisa fin faclu pangpang Nephilim, su ma nutin mutan faclu nu sin mukul lucng. Elos mwet na pwengpeng ac pulaik in pacl so.
Masiku amenewo komanso pambuyo pake, pa dziko lapansi panali Anefili, anthu amphamvu ndiponso otchuka. Anthuwa ndi amene ankabadwa ana a Mulungu aja atakwatira ana aakazi a anthu.
5 Ke LEUM GOD El liye lupan koluk lun mwet nukewa fin faclu, ac lupan nunak koluk lalos ke pacl nukewa,
Pamene Yehova anaona kuti kuyipa kwa munthu pa dziko lapansi kunali kwakukulu ndi kuti nthawi zonse amalingalira ndi kukhumbira kuchita zoyipa zokhazokha,
6 El arulana auli lah el oralosla ac fuhlelosi fin faclu. Yohk oela lal,
Yehova anamva chisoni kuti analenga munthu ndi kumuyika pa dziko lapansi, ndipo anawawidwa mtima.
7 na El fahk, “Nga fah sukela mwet nukewa nga orala inge, wi ma orakrak ac won nukewa, mweyen yohk toasr luk lah nga oralosla.”
Choncho Yehova anati, “Ndidzafafaniza munthu, nyama, zonse zokwawa, ndi mbalame za mu mlengalenga pa dziko lapansi, pakuti ndikumva chisoni kuti ndinazilenga zimenezi.”
8 Tusruktu LEUM GOD El insewowo sel Noah.
Koma Yehova anamukomera mtima Nowa.
9 Pa inge sramsram kacl Noah ac fwilin tulik natul. Noah el moul in sie sin sie yurin God, ac el mukena moul suwohs ac wangin mwatal inmasrlon mwet nukewa in fwil lal.
Mbiri ya Nowa inali yotere: Nowa anali munthu wolungama ndi wopanda tchimo pakati pa anthu a mʼbado wake. Ndipo anayenda ndi Mulungu.
10 Oasr wen tolu natul Noah, inelos pa Shem, Ham, ac Japheth.
Nowa anabereka ana aamuna atatu: Semu, Hamu ndi Yafeti.
11 Tusruktu mwet nukewa sayal Noah arulana koluk ye mutun God, na lokoalok ac moul sesuwos apunla faclu.
Chiwawa chinadzaza pa dziko lapansi kotero kuti dziko linakhala lowonongeka pamaso pa Mulungu.
12 God El liye lah faclu arulana kolukla, mweyen moul lun mwet nukewa arulana koluk.
Mulungu atayangʼana, anaona kuti dziko layipadi chifukwa cha makhalidwe oyipa a anthu onse pa dziko lapansi.
13 God El fahk nu sel Noah, “Nga wotela tari ngan kunausla mwet nukewa. Nga ac sukelosla nufon, mweyen faclu sessesla ke orekma koluk lalos.
Ndipo Mulungu anati kwa Nowa, “Ndatsimikiza mtima kuti ndiwononge anthu onse, pakuti dziko lapansi ladzaza ndi ntchito zawo zoyipa. Ndithudi ndiwawononga pamodzi ndi zonse za pa dziko.
14 Musaela soko oak ah okom ke sak na wowo. Orala kutu fukil an loac, ac sroalela acn loac ac acn lik ke tar.
Tsono udzipangire chombo cha matabwa a mtengo wanjale; mʼkati mwake upange zipinda ndipo upake phula mʼkati ndi kunja.
15 Oru in fit angfoko lumngaul lusa, fit itngoul limekosr sralapa, ac fit angngaul limekosr fulata.
Uchipange motere: Chombo chikhale mamita 140 mulitali, mamita 23 mulifupi ndi mamita 13 mu msinkhu wake.
16 Sunya oak uh, ac likiya sie masrol ma inch singoul oalkosr inmasrlon susu sacn ac sisken oak uh. Musai tuh in oasr twek tolu ac orala sie srungul an ke siska uh.
Uchipangire denga ndi kuchimaliza ndi zenera la masentimita makumi asanu. Uyike khomo mʼmbali mwa chombocho ndi kupanga zipinda zosanjikana; chapansi, chapakati ndi chapamwamba.
17 Nga ac supwama sie sronot ah nu faclu in kunausla ma nukewa ma oasr moul la. Ma nukewa fin faclu ac fah misa,
Ndidzagwetsa mvula ya chigumula pa dziko lapansi kuti ndiwononge zamoyo zonse za pansi pa thambo ndipo chilichonse cha pa dziko lapansi chidzafa.
18 tusruktu nga ac orala sie wuleang inmasrlok kom. Utyak nu in oak uh wi mutan kiom, wen nutum, ac mutan kialos.
Koma ndidzachita pangano langa ndi iwe. Iwe, ana ako aamuna, mkazi wako ndi akazi a ana ako nonse mudzalowa mʼchombocho.
19 Kom fah use kais lukwa ke kain in ma orakrak nukewa nu in oak uh, mukul se mutan se, in wi kom moulla.
Iwe udzalowa mʼchombocho ndi zolengedwa zamoyo zonse ziwiriziwiri, chachimuna ndi chachikazi, kuti zisungike ndi moyo pamodzi ndi iwe.
20 Nu ke ip lun won uh, in fal nu ke kain in won, ac nu ke kosro uh, in fal nu ke kain in kosro, ke ma orakrak nukewa in fohk uh, in fal nu ke kain in lumah — kais luo ke kain nukewa fah utyak nu yurum tuh elos fah moul.
Udzatenga ziwiriziwiri za mitundu yonse ya mbalame, mitundu yonse ya nyama, ndi mitundu yonse ya zokwawa kuti zikhale ndi moyo.
21 Us kain in mwe mongo nukewa in wi kom, ma ac fal nu sum ac nu selos.”
Udzatengenso chakudya cha mtundu uliwonse ndi kuchisunga kuti inu ndi nyamazo muzidzadya.”
22 Noah el oru ma nukewa ma God El sapkin.
Nowa anachita zonse monga Mulungu anamulamulira.

< Genesis 6 >

The World is Destroyed by Water
The World is Destroyed by Water