< Ezra 5 >
1 In pacl sac mwet palu luo, Haggai ac Zechariah wen natul Iddo, eltal mutawauk in kaskas ke Inen God lun Israel nu sin mwet Jew su muta in Judah ac Jerusalem.
Nthawi imeneyo aneneri Hagai ndi Zekariya, mwana wa Ido, ankayankhula kwa Ayuda okhala mʼdziko la Yuda ndi mu Yerusalemu mʼdzina la Mulungu wa Israeli, amene anali nawo.
2 Ke Zerubbabel wen natul Shealtiel, ac Joshua wen natul Jehozadak, eltal lohng kas laltal, eltal mutawauk in sifil musai Tempul Jerusalem, ac mwet palu luo ah kasreltal.
Pambuyo pake Zerubabeli mwana wa Sealatieli ndi Yesuwa mwana wa Yozadaki ananyamuka nakayambanso kumanga Nyumba ya Mulungu mu Yerusalemu. Ndipo aneneri a Mulungu anali nawo pamodzi, kuwathandiza.
3 Na Governor Tattenai lun acn Roto-in-Euphrates, ac Shethar Bozenai, ac mwet pwapa wialos, elos sulaklak tuku nu Jerusalem ac kouyak fahk, “Su sap kowos in musai Tempul se inge ac sang kufwa nu kac?”
Pa nthawi imeneyo Tatenai, bwanamkubwa wa chigawo cha patsidya pa Yufurate pamodzi ndi Setari-Bozenai ndi anzawo anapita kwa iwo ndi kukawafunsa kuti, “Anakulolani ndani kuti mumangenso Nyumba imeneyi ndi kutsiriza khoma lake?”
4 Elos oayapa siyuk inen mukul nukewa su wi musai Tempul sac.
Anawafunsanso kuti, “Kodi anthu amene akumanga nyumbayi mayina awo ndani?”
5 Tusruktu God El tawi na mwet kol lun mwet Jew, ac mwet pwapa Persia elos sulela mu elos ac tia mukuikui kac nwe ke elos sim nu sin Tokosra Fulat Darius ac eis kas sel.
Koma Mulungu wawo amayangʼanira atsogoleri Ayuda, motero kuti anthu aja anaganiza kuti asawaletse kumanga Nyumbayo mpaka atalembera mfumu Dariyo kalata ndi kulandira yankho lake.
6 Pa inge kas ma elos supwala nu sel tokosra fulat:
Iyi ndi kalata imene Tatenai bwanamkubwa wa dera la patsidya pa Yufurate, ndiponso Setari-Bozenai ndi anzake, akazembe amene anali mʼchigawo cha patsidya pa Yufurate, anatumiza kwa mfumu Dariyo
7 “Nu sin Tokosra Fulat Darius, lela tokosrai lom in misla.
Analemba kalatayo motere: Kwa mfumu Dariyo: Mukhale ndi mtendere wonse.
8 “Kut ke kom in etu lah kut som nu in acn Judah ac konauk lah Tempul lun God fulat sifil musaiyuk inge ke eot maspang lulap ac ke sak maspang lulap oakwuki in sinka uh. Arulana oaru oreyen orekma uh, ac fahsr na ku.
Amfumu mudziwe kuti ife tinapita ku dziko la Yuda ku Nyumba ya Mulungu wamkulu. Nyumbayo ikumangidwa ndi miyala ikuluikulu ndipo akuyala matabwa pa makoma. Ntchitoyi ikugwiridwa mwachangu ndipo ikuyenda bwino kwambiri mwautsogoleri wawo.
9 “Kut tuh siyuk sin mwet kol lalos in fahk nu sesr lah su sapkin tuh elos in sifil musai Tempul sac ac sang kufwa nu kac.
Ndipo tinawafunsa atsogoleriwo kuti, “Anakulolezani kuti mumangenso Nyumbayi ndi kutsiriza makoma ake ndani?”
10 Kut oayapa siyuk selos inen mwet kol orekma uh kut in mau ku pac in akkalemye nu sum.
Tinawafunsanso mayina a atsogoleri awo, kuti tikalemba mayina atsogoleriwo tidzakudziwitseni kuti muwadziwe.
11 “Elos topuk ac fahk, ‘Kut mwet kulansap lun God lun kusrao ac faclu, ac kut sifil musai Tempul se su nuna musala ac itukyang kufwa nu kac yac puspis somla sin sie tokosra na ku lun Israel.
Yankho limene anatipatsa ndi ili: “Ife ndife atumiki a Mulungu wa kumwamba ndi wa dziko lapansi, ndipo tikumanganso Nyumba imene mfumu ina yamphamvu ya Israeli inamanga ndi kuyitsiriza zaka zambiri zapitazo.
12 Tuh ke sripen mwet matu lasr meet ah akkasrkusrakye God lun Kusrao, El fuhlela elos in sruoh sin Tokosra Nebuchadnezzar lun Babylonia, sie sin leum lun Chaldea. Tempul sac tuh kunausyukla, ac utukla mwet uh nu in sruoh Babylonia.
Koma chifukwa chakuti makolo athu anakwiyitsa Mulungu wakumwamba, Iye anawapereka kwa Nebukadinezara Mkalideya, mfumu ya Babuloni, amene anawononga Nyumbayi ndi kutenga anthu onse kupita nawo ku ukapolo ku Babuloni.
13 Na in yac se meet ke Tokosra Fulat Cyrus el leumi acn Babylonia, el sapkin tuh Tempul uh in sifil musaiyuk.
“Komabe chaka choyamba cha Koresi, mfumu ya ku Babuloni, mfumu Koresiyo anapereka lamulo lakuti Nyumba ya Mulunguyi imangidwenso.
14 El sifil folokunla ahlu gold ac silver ke Tempul su Nebuchadnezzar el tuh usla liki Tempul Jerusalem ac filiya in tempul in Babylon. Tokosra Fulat Cyrus el folokonang ma inge nu sin mwet se pangpang Sheshbazzar, su el srisrngiya in governor lun Judah.
Ndipo ziwiya zagolide ndi zasiliva za ku Nyumba ya Mulungu zimene Nebukadinezara anazitenga mʼNyumba ya Mulungu ku Yerusalemu ndi kukaziyika mʼnyumba ya milungu ya ku Babuloni, anakazichotsa ku nyumba ya milungu ya ku Babuloniko ndi kuzipereka kwa Sesibazara, amene mfumu inamusankha kukhala bwanamkubwa.
15 Tokosra Fulat el fahkang nu sel elan us ma inge ac folokunla nu in Tempul Jerusalem, oayapa elan sifil musaeak Tempul fin acn se ma tu we meet ah.
Tsono mfumuyo inamuwuza kuti, ‘Tenga ziwiyazi ukaziyike mʼNyumba ya Mulungu ku Yerusalemu. Ndipo Nyumba ya Mulunguyo ikamangidwenso pa maziko ake akale.’
16 Ouinge Sheshbazzar el som ac oakiya pwelung la. Na musa sac tutafla in pacl sac me nwe inge, tusruktu soenna safla.’
“Choncho Sesibazarayo anabwera ndi kumanga maziko a Nyumba ya Mulunguyo mu Yerusalemu. Kuyambira tsiku limenelo mpaka lero yakhala ikumangidwa ndipo sinathebe.”
17 “Inge, O Tokosra Fulat, fin ou lungse lom, sap in sukok in ma simla ke sramsram matu Babylon, tuh in kalem lah pwaye ku sutuu lah Tokosra Fulat Cyrus pa sapkin tuh Tempul se in Jerusalem inge in sifilpa musaiyuk. Na kom fah akkalemye nu sesr lah mea kom nunku mu fal in orek ke sripa se inge.”
Nʼchifukwa chake ngati chingakukomereni amfumu, pachitike kafukufuku mʼnyumba yaufumu mosungira chuma ndi mabuku okhudza mbiri ya Babuloni kuti tione ngati mfumu Koresi inalamuladi za kumanganso Nyumba ya Mulungu mu Yerusalemu. Kenaka amfumu mutiwuze zomwe zikukondweretsani kuti mugamule pa nkhani imeneyi.