< Ezekiel 27 >

1 LEUM GOD El fahk nu sik:
Yehova anandiyankhula kuti:
2 “Kom, mwet sukawil moul la, yuk soko on in mas misa an nu sin acn Tyre,
“Iwe mwana wa munthu, imba nyimbo yodandaulira Turo.
3 siti se ma oan weacn uh, su orek kuka nu sin mutunfacl nukewa ma oan weacn uh. Fahk nu sel kas su LEUM GOD Fulatlana El fahk inge: “Tyre, kom tuh filangkin oasku lom an.
Uza Turo, mzinda wokhala pa dooko la nyanja, wochita malonda ndi anthu ambiri a mʼmbali mwa nyanja kuti: Ambuye Yehova akuti, “Iwe Turo, umanena kuti, ‘Ndine wokongola kwambiri.’
4 Acn sum pa meoa uh. Mwet musaikomla uh orekomla oana soko oak na kato.
Malire ako anali mʼkati mwenimweni mwa nyanja; amisiri ako anakukongoletsa kwambiri.
5 Elos oru ipinsak lom nukewa ke sak fir Fineol Hermon, Ac soko sak cedar liki acn Lebanon nu ke kwesu lom.
Anakupanga ndi matabwa a payini ochokera ku Seniri; anatenga mikungudza ya ku Lebanoni kupangira mlongoti wako.
6 Elos eis sak oak Bashan me in orek oac kac, Ac orala falful ke oak an ke sak pine Cyprus me, Ac nawela ke ivory.
Ndi mitengo ya thundu ya ku Basani anapanga zopalasira zako; ndi matabwa a mitengo ya payini yochokera ku zilumba za Kitimu. Pakuti anapanga thandala lako pakati pa matabwawo panali minyanga ya njovu.
7 Nes nu ke oak an orekla ke nuknuk linen, Aok, nuknuk akul su tuku Egypt me, Arulana mahnek in liyeyuk yen loesla me. Ac nuknuk sunyen twek orekla ke nuknuk wowo, Tuhn kac uh folfol ac sroninmutuk, ma tuku Cyprus me.
Nsalu yabafuta yopeta yochokera ku Igupto inali thanga yako, ndipo inakhala ngati mbendera. Nsalu zophimba matenti ako zinali za mtundu wamtambo ndi pepo zochokera ku zilumba za Elisa.
8 Mwet in kal lom elos mwet Sidon ac Arvad, Ac mwet pisrla in us oak an mwet na lom sifacna.
Anthu a ku Sidoni ndi Arivadi ndi amene anali opalasa ako. Anthu aluso ako, iwe Turo, anali mwa iwe ndiwo amene ankakuyendetsa.
9 Mwet kamtu fin oak uh mwet na pah, Su tuku Byblos me. Selu fin oak nukewa su kalkal meoa Elos tuku moul ke acn in kuka lom.
Akuluakulu ndi eni luso a ku Gebala anali mʼkati mwako, ngati okonza zibowo zako. Sitima za pa nyanja zonse, ndi oyendetsa ake ankabwera pamodzi ndi katundu kudzachita nawe malonda.
10 “Mwet mweun lun Persia, Lydia ac Libya elos inmasrlon mwet mweun lom. Elos sripisrya mwe loeyuk lalos ac susu in mweun lalos in lohm sin mwet mweun lom. Elos pa akpwengpengye kom.
“Anthu a ku Perisiya, a ku Ludi ndi Puti anali asilikali mʼgulu lako la nkhondo. Iwo ankapachika zishango ndi zipewa zawo zankhondo pa makoma ako, kubweretsa kwa iwe ulemerero.
11 Mwet mweun liki siti Arvad pa mwet topang su karingin pot in siti lom, ac mwet Gamad pa karingin tower lom uh. Elos sripisrya mwe loeyuk lalos ke pot lom uh, ac elos inge pa akkatoye kom uh.
Anthu a ku Arivadi ndi Heleki ankalondera mbali zonse za mpanda wako; anthu a ku Gamadi anali mu nsanja zako, Iwo ankapachika zishango zawo pa makoma ako onse. Amenewo ndiwo anakukongoletsa kwambiri.
12 “Kom som kukakin ma puspis lom in acn Tarsis, ac kom eis silver, iron, tin ac lead in sang aol ma kom kukakunla.
“Dziko la Tarisisi linachita nawe malonda chifukwa cha kuchuluka kwa katundu wako wamtundumtundu. Iwo ankapereka siliva, chitsulo, chitini ndi mtovu mosinthanitsa ndi katundu wako.
13 Kom oayapa orek kuka in acn Greece, Tubal, ac Meshech, ac kukakunla mwe kasrup lom in moli mwet kohs ac ma orekla ke osra bronze.
“Yavani, Tubala ndi Mesaki ankachita nawe malonda; iwo ankapereka akapolo ndi ziwiya za mtovu mosinthanitsa ndi katundu wako.
14 Kom kukakunla ma lom in moli horse in orekma, horse in mweun, ac mule liki acn Beth Togarmah.
“Anthu a ku Beti Togarima ankapereka akavalo antchito, akavalo ankhondo ndi abulu mosinthanitsa ndi katundu wako.
15 Mwet Dedan elos oayapa tuku moul yurum, ac mwet in acn puspis su oan sisken meoa uh oayapa use ivory ac ebony in aolla mwe kasrup lom.
“Anthu a ku Dedani ankachita nawe malonda, ndipo anthu ambiri a mʼmbali mwa nyanja anali ogula malonda ako. Ankakupatsa minyanga ya njovu ndi phingo.
16 Mwet Syria elos molela pac mwe kuka lom ac ma puspis ma kom orala. Na elos sot nu sum wek emerald ac ruby, nuknuk sroninmutuk, nuknuk akul, nuknuk srik eoa, ac ma saok inkof uh, in sang moli ma oasr yurum.
“Anthu a ku Aramu ankachita nawe malonda chifukwa cha kuchuluka kwa zinthu zako. Iwo ankapereka miyala ya emeradi, nsalu zapepo, nsalu zopetapeta, nsalu zabafuta, korali ndi miyala ya rubi mosinthanitsa ndi katundu wako.
17 Mwet Judah ac mwet Israel elos moli mwe kuka lom ke wheat, honey, oil in olive, ac mwe akyuye mongo.
“Yuda ndi Israeli ankachita nawe malonda. Iwo ankapereka tirigu ochokera ku Miniti ndi zokometsera zakudya, uchi, mafuta ndi mankhwala mosinthanitsa ndi katundu wako.
18 Mwet Damascus elos oayapa moul yurum ke mwe kasrup su oasr yurum, ac elos moli ke wain lun Helbon ac unen sheep Sahar me.
“Anthu a ku Damasiko, chifukwa cha zinthu zako za malonda zambiri ndi katundu wako wosiyanasiyana, ankachita nawe malonda a vinyo wochokera ku Heliboni ndi ubweya wankhosa ochokera ku Zahari.
19 Vedan ac Javan liki acn Uzal eltal kukakin osra iron ac mwe akyu mongo, sang aol mwe kasrup su oan yurum.
Adani ndi Agriki ochokera ku Uzala ankagula katundu wako. Iwo ankapereka chitsulo chosalala, kasiya ndi bango lonunkhira mosinthanitsa ndi katundu wako.
20 Mwet Dedan elos kukakin mwe loeyuk mwe muta fin horse in moli mwe kuka lom.
“Anthu a ku Dedani ankakugulitsa nsalu zoyika pa zishalo za akavalo.
21 Mwet Arabia ac mwet leum lun facl Kedar elos moli mwe kuka lom ke sheep fusr, sheep mukul, ac nani.
“Arabiya ndi mafumu onse a ku Kedara anali ogula malonda ako. Iwo ankachita nawe malonda a ana ankhosa onenepa, nkhosa zazimuna ndi mbuzi.
22 Mwet kuka lun acn Sheba ac Raamah elos use mwe keng na wowo, wek saok, ac gold, in sang moli mwe kuka lom.
“Anthu amalonda a ku Seba ndi Raama ankachita nawe malonda. Iwo ankapereka zonunkhira zosiyanasiyana zabwino kwambiri, miyala yokongola ndi golide mosinthanitsa ndi katundu wako.
23 Siti lun Haran, Canneh ac Eden, oayapa mwet kuka lun Sheba ac siti lun Asshur ac Chilmad — elos kewa orek kuka ac moul yurum.
“Amalonda a ku Harani, Kane, Edeni, Seba, Asuri ndi Kilimadi ankachita nawe malonda.
24 Elos kukakin nu sum nuknuk na oasku, nuknuk sroninmutuk ac nuknuk akul, ac mwe loeyuk na kato ma nu in lohm, ac sucl ac ah na wowo.
Iwowa ankasinthanitsana nawe zovala zokongola, nsalu zopetapeta, zoyala pansi za mawangamawanga, atazimanga bwino ndi zingwe zolimba.
25 Mwe kuka lom inge wunyuk ke un oak na lulap. “Kom oana soko oak meoa Ma sessesla ke mwe kuka.
“Sitima za pa madzi za ku Tarisisi zinali zonyamula malonda ako. Motero iwe uli ngati sitima yapamadzi yodzaza ndi katundu wolemera.
26 Ke mwet in kal lom uh kuhlukinkomla nu meoa, Sie eng kutulap me kunausla oak okom infulwen meoa.
Anthu opalasa ako amakupititsa pa nyanja yozama. Koma mphepo yakummawa idzakuthyolathyola pakati pa nyanja.
27 Mwe kasrup ke mwe kuka lom nukewa, Ac mwet selu lom nukewa, Mwet kamtu fin oak uh wi mwet in kuka uh, Ac mwet mweun nukewa — Elos nukewa tuhlac in meoa uh Ke pacl oak uh musalla.
Chuma chako, katundu wako, malonda ako, okuyendetsa ako, okuwongolera ako ndi opanga sitima za pa madzi, anthu ako amalonda ndi asilikali ako onse ndiponso aliyense amene ali mʼmenemo adzamira mʼnyanja tsiku limene udzawonongeka.
28 Pusren mwet walomla uh Lohngyuk finmes uh.
Madera a mʼmbali mwa nyanja adzagwedezeka chifukwa cha kufuwula kwa oyendetsa sitimawo.
29 “Oak nukewa wanginla mwet fac, Ac mwet nukewa utyak nu finmes ah.
Onse amene amapalasa sitima zapamadzi, adzatuluka mʼsitima zawo; oyendetsa ndi onse owongolera sitima zapamadzi adzayimirira mʼmbali mwa nyanja.
30 Elos nukewa arulana asor ac tung keim, Na elos sisak kutkut nu fin sifalos ac oan ipippip in apat uh.
Iwo akufuwula, kukulira iwe kwambiri; akudzithira fumbi kumutu, ndi kudzigubuduza pa phulusa.
31 Ke sripom elos mangsrasrala, Ac nokomang nuknuk yohk eoa. Insialos arulana oela ke elos tung mwemelil.
Akumeta mpala mitu yawo chifukwa cha iwe ndipo akuvala ziguduli. Akukulira iweyo ndi mitima yowawa kwambiri.
32 Elos yuk on in mas misa soko inge keim: ‘Su ac ku in lumweyuk nu ke acn Tyre — Tyre, su oan misla ye kof uh?
Akuyimba nyimbo yokudandaulira nʼkumati: ‘Ndani anawonongedwapo ngati Turo pakati pa nyanja?’
33 Meet, ke mwe kuka lom uh sasla meoa uh, Kom akfalye enenu lun mutunfacl nukewa. Tokosra uh kasrupi Ke mwe kuka puspis lom.
Pamene malonda ako ankawoloka nyanja unakhutitsa mitundu yambiri ya anthu. Mafumu a dziko lapansi analemera ndi chuma chako komanso ndi malonda ako.
34 Inge kom musalla in meoa uh, Ac kom tili nu yen loal inkof uh. Mwe kasrup lom ac mwet orekma lom nukewa Wi kom na wanginla inkof uh.’
Koma tsopano wathyokera mʼnyanja, pansi penipeni pa nyanja. Katundu wako ndi onse amene anali nawe amira pamodzi nawe.
35 “Mwet nukewa su muta weacn uh elos oela ke mwe ongoiya ma sikyak nu sum. Finne tokosra lalos, elos sangengla pac, ac mutalos akkalemye sangeng lalos.
Onse amene amakhala mʼmbali mwa nyanja aopsedwa ndi zimene zakuchitikira. Mafumu awo akuchita mantha ndipo nkhope zangoti khululu.
36 Kom wanginla, wanginla ma pahtpat. Ac mwet kuka faclu nufon elos sangeng ma lulap, mweyen elos sensen mu elos ac sun ongoiya se ma sikyak nu sum uh.”
Anthu amalonda a mitundu ina akukunyogodola. Watha mochititsa mantha ndipo sudzakhalaponso mpaka muyaya.”

< Ezekiel 27 >