< Ezekiel 21 >

1 LEUM GOD El kaskas nu sik ac fahk,
Yehova anandiyankhula nati:
2 “Kom, mwet sukawil moul la, fahkak kas in lain Jerusalem ac lain yen mwet uh alu we. Sang kas in sensenkakin facl Israel
“Iwe mwana wa munthu, tembenuka uyangʼane ku Yerusalemu ndipo ulalike mawu odzudzula malo ake opatulika. Unenere zodzudzula anthu a ku Yerusalemu.
3 lah nga, LEUM GOD, fahk mu: ‘Nga mwet lokoalok lowos. Nga ac fwauk cutlass nutik ac unikowosi nukewa, mwet wo ac mwet koluk oana sie.
Uwawuze kuti, Ambuye Yehova akuti, ‘Taona, Ine ndidzalimbana nawe. Ndidzasolola lupanga langa mʼchimake ndi kuwononga anthu olungama ndi ochimwa omwe.
4 Nga ac orekmakin cutlass nutik uh in uni mwet nukewa, eir lac nwe epang.
Motero ndidzapha aliyense kuchokera kummawa mpaka kumpoto.
5 Mwet nukewa fah etu lah nga, LEUM GOD, fwauk tari cutlass nutik, ac nga fah tia sifil folokonang nu yen se.
Pamenepo anthu onse adzadziwa kuti Ine Yehova ndi amene ndasolola lupanga langa mʼchimake; sindidzalilowetsanso mʼchimakemo.’
6 “Kom, mwet sukawil, sao ac tung ke asor lulap. Sasao yen mwet nukewa ac ku in liye kom we.
“Tsono iwe mwana wa munthu, buwula. Buwula pamaso pawo ndi mtima wosweka ndi wachisoni chachikulu.
7 Ke elos siyuk sum lah efu kom ku tung, fahk nu selos lah ma ke sripen pweng su tuku inge. Ke pacl se ac tuku, insialos ac arulana sangeng, ac paolos ac atla ac uli, ac kuiyalos ac munasla, ac nialos ac rarrar. Pacl sac pa inge.” LEUM GOD Fulatlana pa fahk ma inge.
Ndipo akadzakufunsa kuti, ‘Nʼchifukwa chiyani ukubuwula?’ Iwe udzayankhe kuti, ‘Ndikubuwula chifukwa cha nkhani imene ndamva. Zikadzachitika zimenezi, mitima yonse idzangoti fumu, manja onse adzangolefuka, mpweya wawo udzawathera, ndipo mawondo onse adzangoti zii.’ Izi zikubwera! Ndipo zidzachitika ndithu, akutero Ambuye Yehova.”
8 LEUM GOD El fahk nu sik,
Yehova anandiyankhulanso kuti,
9 “Mwet sukawil, palye ac fahk nu sin mwet uh lah mea nga, LEUM GOD, fahk inge: Sie cutlass, aok sie cutlass pa twetela ac aksaromromyeyukla.
“Iwe mwana wa munthu, unenere ndipo unene kuti, Ambuye Yehova akuti, “Izi ndi zimene Yehova akunena: Lupanga, lupanga, lanoledwa ndipo lapukutidwa.
10 Temyukla in uniya, Aksaromromyeyukla in sarmelik oana sarom uh. Na ac fah wangin enganak yurin mwet luk Mweyen elos pilesru kas in sensen nukewa, oayapa kas in kai.
Lanoledwa kuti likaphe, lapukutidwa kuti lingʼanime ngati mphenzi! “‘Kodi tingakondwere bwanji? Wanyoza ndodo, mwana wanga ndi chilichonse cha mtengo.
11 Cutlass uh akmusrala tari Ac akola in orekmakinyuk. Temyukla ac akmusrala Tuh in oan inpoun sie mwet akmas.
“‘Lupanga laperekedwa kuti lipukutidwe, ndi kuti linyamulidwe, lanoledwa ndi kupukutidwa, kuti liperekedwe mʼmanja mwa munthu amene amapha.
12 Mwet sukawil, wowoyak ke keok; Cutlass se inge ma ac lain mwet luk Oayapa mwet kol nukewa lun mwet Israel. Elos ac anwuki Wi mwet luk nukewa. Puokya iniwom ke supwarla ac wanginla finsrak!
Fuwula ndi kulira, iwe mwana wa munthu, pakuti zimenezi zidzagwera anthu anga; zidzagweranso akalonga onse a Israeli. Adzaphedwa ndi lupanga pamodzi ndi anthu anga. Chifukwa chake udzigugude pa chifuwa ndi chisoni.
13 Nga srike mwet luk inge Ac elos fin srunga auliyak, Na ma inge nukewa ac sikyak nu selos.
“‘Ambuye Wamphamvuzonse akuti: Ndikuwayesa anthu anga, ndipo ngati satembenuka mtima, ndiye kuti zimenezi sizidzalephera kuwagwera.’
14 “Inge, mwet sukawil, palye ac paspas, na cutlass sac ac pakpuk na pakpuk. Cutlass sac mwe uniya, mwe aksangeng, ac mwe fakfuk.
“Tsono mwana wa munthu, nenera ndipo uwombe mʼmanja. Lupanga likanthe kawiri ngakhale katatu. Limenelo ndilo lupanga lophera anthu. Inde ndilodi lupanga lophera anthu koopsa limene likuwazungulira.
15 Ac oru mwet luk in tila pulaik, ac elos ac fahsr tukulkul. Nga aksangengye siti selos ke sie cutlass sarmelik oana sie sarom, su akola in uniya mwet.
Ndawayikira pa zipata zawo zonse lupanga laphuliphuli kuti ataye mtima ndiponso kuti anthu ambiri agwe. Aa! Lapangidwa lupanga kuti lizingʼanima ngati mphenzi ndi kuti azilisolola kuphera anthu.
16 Kom, cutlass kosroh, pakpuk nu layot ac nu lasa. Pakpuk nu acn nukewa kom for we.
Iwe lupanga, ipha anthu kumanja, kenaka kumanzere, kulikonse kumene msonga yako yaloza.
17 Nga fah paspas pac, na kasrkusrak luk ac fah wanginla. Nga, LEUM GOD, pa fahk ma inge.”
Inenso ndidzawomba mʼmanja mwanga, ndipo ndidzaziziritsa ukali wanga Ine Yehova ndayankhula.”
18 LEUM GOD El kaskas nu sik
Yehova anandiyankhulanso kuti,
19 ac fahk, “Mwet sukawil, akilenya lukwa inkanek ma tokosra Babylonia elan ku in ut we wi cutlass natul. Mutaweyen inkanek lukwa inge in tuku ke mutunfacl sefanna. Tulokunak sie akul an yen ma inkanek an sengelik we.
“Iwe mwana wa munthu, ulembe zizindikiro za misewu iwiri imene lupanga la mfumu ya ku Babuloni lingathe kudzeramo. Misewu yonse ikhale yochokera mʼdziko limodzi. Ika chikwangwani pa mphambano yopita mu mzinda.
20 Soko in akkalemye nu sin tokosra lah ma ac som nu Rabbah, siti lun mwet Ammon. Ac ma soko ngia, ma ac som nu Judah, nu ke Jerusalem, siti se ma akkeyeyukla ke pot ku.
Ulembe chizindikiro pa msewu umene lupanga lidzadzere popita ku Raba wa ku Amoni, ndiponso ku Yuda ndi ku Yerusalemu, mzinda wotetezedwa.
21 Tokosra lun acn Babylonia el ac tu ke akul ke yen inkanek ah sengelik we. In konauk acn el ac ut we, el usruk sukan pisr natul, na el siyuk kasru sin ma sruloala lal; na el ac lohang nu ke esan kosro soko ma kisakinyukla.
Pakuti mfumu ya ku Babuloni yayima pa msewu, pa mphambano ya misewu iwiriyo. Ikuwombeza ndi mivi yake kuti idziwe njira yoyenera kudzeramo. Ikupempha nzeru kwa milungu yake ndipo ikuyangʼana chiwindi cha nyama yoperekedwa ku nsembe.
22 Inge, lac po layot sel sruok sukan pisr ma akilenya acn ‘Jerusalem’! Ma se inge akkalemye nu sel elan som ac akola polosak mwe fokfok mutunpot uh, na sala ke sasa lun mweun, ac likiya mwe fokfok mutunpot uh sisken pot ah, ac elosak fohk sisken pot uh, ac pukpuk laf.
Mʼdzanja lake lamanja muli muvi waula wolembedwa Yerusalemu. Kumeneko mfumuyo idzayika zida zogumulira, idzalamula kupha anthu ndiponso kufuwula mfuwu wa nkhondo. Mfumuyo idzapanga zida zogumulira makoma, kuwunda mitumbira ya nkhondo ndi kumanga nsanja za nkhondo.
23 Mwet Jerusalem ac tia lulalfongi ma inge mweyen elos orala tari sie wuleang inmasrlolos. Tusruktu kas in palu inge akesmakyalos ke ma koluk lalos, ac akkalemye nu selos lah elos ac fah sruoh.
Koma kwa anthu a ku Yerusalemu zidzaoneka ngati zowombeza zabodza chifukwa cha malumbiro amene anachita kwa mfumuyo. Koma mfumuyo idzawakumbutsa za zolakwa zawo kuti atengedwe ku ukapolo.
24 Pa inge ma nga, LEUM GOD Fulatlana, fahk uh: Ma koluk lowos kalem sin mwet e nukewa, ac elos etu lupan ma koluk lowos uh. Kalem ke mukuikui nukewa lowos, na nga fah eiskowosyang nu inpoun mwet lokoalok lowos.
“Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akuti, ‘Popeza mwandikumbutsa zolakwa, moti kundiwukira kwanu kwaonekera poyera ndi kuti mu zochita zanu zonse mukuonetsa machimo anu, nʼchifukwa chake mudzagwidwa ndi kutengedwa ukapolo.
25 “Kom su mwet kol koluk ac sesuwos lun Israel, len in kaiyuk safla lom pa ac tuku inge.
“‘Tsono iwe kalonga wonyozedwa ndi woyipa wa Israeli, amene tsiku lako lafika, amene nthawi yako yolangidwa yafika penipeni,
26 Nga, LEUM GOD Fulatlana, pa fahk ma inge. Eisya tefuro lom ac susu lom an. Wangin ma ac fah sifil oana meet. Akleumye mwet pusisel, ac akpusiselye mwet leum.
Ambuye Yehova akuti: Vula nduwira, chotsa chipewa chaufumu. Zinthu sizidzakhala monga zinalili: anthu wamba adzakwezedwa ndipo okwezedwa adzatsitsidwa.
27 Musalla! Musalla! Aok, nga fah oru tuh siti sac in musalla. Tusruktu ac fah tia sikyak nwe ke pacl se mwet se ma nga sulela el tuku in kalyei siti uh. El pa nga fah sang siti uh nu se.
Chipasupasu! Chipasupasu! Ine ndidzawupasula mzindawo! Ndipo sadzawumanganso mpaka atafika amene ali woyenera kuwulandira; Ine ndidzawupereka kwa iyeyo.’
28 “Mwet sukawil, palye ac fahkak ma nga, LEUM GOD Fulatlana, fahk nu sin mwet Ammon, su fahk kas koluk lain mwet Israel. Fahk nu selos: ‘Sie cutlass pa akola in kunausla; Akmusrala tari in uniya, in sarmelik oana sarom uh.
“Ndipo iwe mwana wa munthu, nenera kuti, ponena za Aamoni ndi zonyoza zawo, Ambuye Yehova akuti, “‘Lupanga, lupanga, alisolola kuti liphe anthu, alipukuta kuti liwononge ndi kuti lingʼanime ngati mphenzi.
29 Aruruma kowos liye uh tia pwaye, ac ma kowos motko mu ac sikyak uh ma kikiap. Kowos mwet sesuwos ac koluklana. Len in kalya safla lowos ac tuku. Cutlass uh akola in twacla inkwawowos.
Zimene akuti akuona mʼmasomphenya zokhudza inu ndi zabodza. Mawula awo okhudza inu ndi abodzanso. Mudzakhala pamodzi ndi anthu oyipa amene tsiku lawo lafika, ndiye kuti nthawi ya kulangidwa kwawo komaliza.
30 “‘Filiya cutlass an! Nga ac nununkekowos in acn kowos orekla we, in facl su kowos isusla we.
“‘Bwezerani lupanga mʼchimake. Ku malo kumene inu munabadwira, mʼdziko la makolo anu, ndidzakuweruzani.
31 Kowos ac pula kasrkusrak luk ke nga ac fuhleot nu fowos oana sie e firir. Ac nga ac eiskowosyang nu inpoun mwet sulallal, su arulana etu in kunaus mau.
Ndidzakhuthula ukali wanga pa inu, ndipo mkwiyo wanga udzakuyakirani. Ndidzakuperekani mʼmanja mwa anthu ankhanza; anthu odziwa bwino kuwononga zinthu.
32 Kowos ac fah isisyak ke e. Srah keiwos ac fah sororla fin facl suwos sifacna, ac wangin sie mwet ac esam kowos.’” LEUM GOD pa fahk ma inge.
Mudzakhala ngati nkhuni pa moto. Ena adzakhetsa magazi anu mʼdziko lanu lomwe. Simudzakumbukiridwanso pakuti Ine Yehova ndayankhula.’”

< Ezekiel 21 >