< Ezekiel 16 >

1 LEUM GOD El sifil kaskas nu sik,
Yehova anayankhula nane kuti,
2 ac fahk, “Mwet sukawil moul la, fahkang nu sin Jerusalem orekma srungayuk ma el orala.
“Iwe mwana wa munthu, udzudzule Yerusalemu za ntchito zake zonyansa.
3 Fahk nu sin Jerusalem ma LEUM GOD Fulatlana El fahk nu sel: “Kom tuh isusla in facl sin mwet Canaan. Papa tomom el sie mwet Amor ac nina kiom el sie mwet Hit.
Umuwuze kuti, ‘Ambuye Yehova akukuwuza, iwe Yerusalemu kuti: Kwawo kwa makolo ako ndi ku Kanaani ndipo iwe unabadwira komweko. Abambo ako anali Mwamori, amayi ako anali Mhiti.
4 Ke pacl se kom isusla ah, wangin mwet lusala futom, ku twetekinkomla, ku sohlela monum, ku pwikomla ke ipin nuknuk.
Pa tsiku lomwe unabadwa sanadule mchombo wako. Sanakusambitse mʼmadzi kuti uyere. Sanakuthire mchere kapena kukukulunga mʼnsalu.
5 Wangin mwet pakomutom in oru kutu sin ma inge nu sum. Ke kom isusla ah, sisila kom nu inima ke sripen wangin mwet lungse kom.
Palibe ndi mmodzi yemwe anakusamala kapena kukumvera chisoni kuti akuchitire zimenezi. Mʼmalo mwake anakutaya panja poyera, chifukwa ananyansidwa nawe pa tsiku lako lobadwa.
6 “Na nga fahsryak ac liye ke kom oan tipirpir in srah keim an. Monum afla ke srah, tusruktu nga tia lela kom in misa.
“‘Tsono pamene ndinkadutsa, ndinakuona ukuvimvinizika mʼmagazi ako. Ndinakuyankhula uli mʼmagazi ako omwewo kuti, ‘Khala ndi moyo,’
7 Nga tufwe kom in kapak oana soko sacn ma kapak wo. Kom kapak kui ac mutan fusrla. Wo aten titi lom, loes aunsifom, tusruktu kom koflufol.
ndi kuti ukule ngati mbewu ya mʼmunda. Iwe unakula ndipo unatalika ndi kutha msinkhu. Mawere ako anayamba kumera ndi tsitsi lakonso linayamba kutalika. Komabe unali wamaliseche ndi wausiwa.
8 “Ke nga sifil fahsryak insac, nga liye lah kom nunak in payuk. Na nga afinya monum ke nuknuk lik luk, ac wuleot mu nga ac lungse kom. Aok, nga orala sie wuleang in marut inmasrloktal, na kom ma lac luk.” Pa inge ma LEUM GOD Fulatlana El fahk.
“‘Tsono pamene ndinkadutsanso ndinaona kuti nthawi yako yomanga banja inakwana. Tsono ndinakufunditsa chovala changa ndi kubisa umaliseche wako. Ndinachita nawe pangano la ukwati ndipo unakhala wanga, akutero Ambuye Wamphamvuzonse.
9 “Na nga otema kutu kof ac twanla srah keim, ac nga sang oil in olive mosrwekomla.
“‘Ine ndinakusambitsa mʼmadzi kutsuka magazi ako ndikukudzoza mafuta.
10 Nga nukumkomyang ke nuknuk orekla ke mwe akul na kato, ac sot fahluk orek ke kulun kosro na wowo, ac nga sot sie nuknuk linen mwe lohl suf, ac sie nuknuk lik orekla ke silk.
Ndinakuveka zovala zopetapeta ndi nsapato za chikopa. Ndinakuveka zovala zabafuta ndi kukuveka zovala za bafuta.
11 Nga nawekomla ke mwe lohlpo, ac ah nu inkwawom ma orekla ke eot saok.
Ndinakukongoletsa ndi zokometsera zamtengowapatali: ndinakuveka zibangiri mʼmanja mwako ndi mkanda mʼkhosi mwako,
12 Nga sot sie ring nu ke fwem, oayapa yaring, ac sie tefuro na oasku.
ndipo ndinakuveka chipini pa mphuno yako, ndolo ku makutu ako ndiponso chipewa chaufumu pa mutu wako.
13 Oasr mwe naweyuk lom orekla ke gold ac silver, ac pacl nukewa kom nukum nuknuk linen ac silk ma akul uh. Kom mongo bread ma orekla ke flao wowo, ac oasr honey ac oil in olive kom kang. Katoiyom arulana oasku, na kom kasrala.
Choncho unavala zokongoletsa zagolide ndi siliva. Zovala zako zinali zabafuta, zasilika ndi za nsalu zopetapeta. Chakudya chako chinali ufa wosalala uchi ndi mafuta a olivi. Motero unakhala wokongola kwambiri ndipo unasanduka mfumukazi.
14 Kom pwengpeng in mutunfacl nukewa ke sripen kato lom, mweyen nga pa orekomla in arulana oasku.” Pa inge ma LEUM GOD Fulatlana El fahk.
Ndipo mbiri ya kukongola kwako inawanda pakati pa anthu a mitundu ina, chifukwa ulemerero umene ndinakupatsa unapititsa patsogolo kukongola kwako, akutero Ambuye Yehova.
15 “Tuh ke sripen kom konkun kato ac pwengpeng lom, kom oan yurin kutena mukul su tuku nu yurum.
“‘Koma iwe unatama kukongola kwako ndipo unayamba kuchita zadama chifukwa cha kutchuka kwako. Unkachita chigololo ndi kumangodzipereka kwa aliyense wodutsa ndipo kukongola kwako kunakhala kwake.
16 Kom orekmakin kutu nuknuk lom in sang yuni nien alu sum. Na kom eiskomyang nu sin kutena mukul, oana sie mutan kosro su eis molin kosro lal.
Unatenga zovala zako zina nukakongoletsera malo opembedzerako mafano, ndipo kumeneko umachitirako zigololo. Zinthu izi sizinachitikepo nʼkale lomwe ndipo sizidzachitikanso.
17 Kom eisla mwe yun silver ac gold su nga sot lom, ac kom sang taflela ma sruloala in luman mukul uh, ac orek kosro nu kac.
Unatenga zokongoletsera zopangidwa ndi golide ndi siliva zimene ndinakupatsa ndipo unadzipangira wekha mafano aamuna amene unkachita nawo za dama.
18 Kom eisla nuknuk akul su nga sot lom ac sang nokomang ma sruloala ingan, ac kom kisakin nu selos oil in olive ac mwe keng ma nga sot nu sum.
Ndipo iwe unatenga zovala zako zopetapeta ndi kuveka mafano. Mafuta anga ndi lubani wanga unapereka kwa mafanowo.
19 Nga sot nom flao na wowo, oil in olive, ac honey, tuh pa kom kisakin ma inge in akinsewowoye ma sruloala uh.” Pa inge ma LEUM GOD Fulatlana El fahk.
Chakudya chimene ndinakupatsa, ufa, mafuta ndi uchi, zimene ndinkakudyetsa nazo unazitenga nʼkuzipereka kwa mafanowo ngati nsembe ya fungo lokoma. Ndikutero Ine Ambuye Yehova.
20 “Na kom eis tulik mukul ac mutan ma kom oswela nu sik, ac kisakunulos nu ke ma sruloala uh. Ya tia fal tari ke kom tia pwaye nu sik?
“‘Ndipo unatenga ana ako aamuna ndi ana aakazi amene unandibalira ine, ndipo unakawapereka ngati nsembe kwa mafanowo. Kodi zigololo zakozo sizinakukwanire
21 Na efu kom ku sifil sang tulik nutik uh in mwe kisa nu ke ma sruloala?
kuti uziphanso ana anga ndi kuwapereka ngati nsembe kwa mafano akowo?
22 Ke pacl se kom moulkin lumah srungayuk oana sie mutan kosro, kom tiana esamak pacl se kom tulik, koflufol ac tipirpir in srah keim sifacna.”
Chifukwa cha zadama zako zonyansazi unayiwala masiku a ubwana wako pamene unali wamaliseche, wausiwa ndiponso womangovivinizika mʼmagazi.
23 LEUM GOD Fulatlana El fahk, “We nu sum! Kom oru ma koluk inge nukewa,
“‘Tsoka! Tsoka kwa iwe, akutero Ambuye Yehova chifukwa powonjezera pa zoyipa zako zonse,
24 na sisken inkanek nukewa kom musaela nien alu nu ke ma sruloala, ac iwen orek kosro.
wadzimangira wekha nsanja ndi guwa pa mabwalo onse.
25 Kom akfohkfokyela kato lom yen furarrar, ac kom fuhleang monum nu sin kutena mukul su fahsryak, ac moul in kosro lom uh yokelik len na len.
Pa msewu uliwonse wamanga nsanjazo. Motero wanyazitsa kukongola kwako podzipereka kwa aliyense amene adutsapo.
26 Kom kukakin monum nu sin mwet Egypt, su mwet tulan elahn kosro, na kom oru kosro lom uh in akkasrkusrakyeyu.
Umachita chigololo ndi Aigupto, anthu adama oyandikana nawe. Choncho unandikwiyitsa chifukwa unachulukitsa za dama zako.
27 “Na inge, nga srukak pouk in kai kom, ac in eisla ip lom ke mwe insewowo luk uh. Nga eiskomyang nu inpoun mwet Philistia su srungakom ac mwekin ke moul fohkfok lom.
Nʼchifukwa chake ndinatambasula dzanja langa kukukantha ndi kuchepetsa dziko lako. Ndinakupereka kwa adani ako, Afilisti amene amayipidwa ndi makhalidwe ako onyansa.
28 “Ke sripen kom tiana muti yorolos, oru kom ukwe mwet Assyria. Kom kukakin monum nu selos, tuh kom tia pac muti selos.
Chifukwa cha chilakolako chako unachitanso zadama ndi Aasiriya. Ngakhale unachita nawo chigololo koma sunakhutitsidwebe.
29 Kom oayapa orek kosro yurin mwet Babylonia, sie facl pwengpeng ke kuka, tuh pa kom tia pac muti selos.”
Choncho unapitirirabe kuchita chigololo ndi Ababuloni, anthu a mʼdziko lokonda zamalonda. Ngakhale unachita izi, komabe sunakhutitsidwe.
30 Pa inge ma LEUM GOD Fulatlana El fahk: “Kom oru ma inge nukewa oana sie mutan kosro na sumwekin.
“‘Ambuye Yehova akuti: Mtima wako ndi wofowoka kwambiri chifukwa unachita zonsezo monga ngati mkazi wopanga manyazi.
31 Kom musaela acn in alu nu ke ma sruloala oayapa iwen orek kosro ke inkanek nukewa. Tusruktu kom tia sukok mani in oana mutan saya ma kukakin manolos.
Unamanga nsanja pa msewu uliwonse. Unamanganso kachisi pabwalo lililonse. Komabe sunachite ngati mkazi wadama chifukwa unakana malipiro.
32 Kom oana mutan su lungse orek kosro yurin mukul saya, ac tia lungse oan yurin mukul tumal sifacna.
“‘Iwe mkazi wachigololo! Umakonda amuna achilendo kupambana mwamuna wakowako!
33 Mutan kosro uh elos eis molin kosro lalos, a kom sang monum, tia moul, nu sin mukul ma orek pwar nu sum, ac kom sang mani in eyeinse nu selos in tuku liki acn nukewa ac oan yurum.
Amuna ndiwo amapereka malipiro kwa mkazi wadama. Koma iwe ndi amene ukupereka mphatso kwa zibwenzi zako zonse. Choncho umazinyengerera kuti zizibwera kwa iwe kuchokera mbali zonse kudzagona nawe.
34 Kom tiana oana mutan kosro saya. Wangin mwet akkohsye kom in sie mutan kosro. Tia moul nu sum, a kom moli nu selos! Pwayena lah kom siena lukelos.”
Chotero iwe ukusiyana ndi akazi ena achigololo, pakuti palibe amene ankakunyengerera kuti uchite naye chigololo. Iweyo ndiye unkapereka ndalama osati ena kukupatsa ndalama ayi. Motero unalidi wosiyana kwambiri ndi akazi ena.
35 Jerusalem, kom mutan kosro se! Inge, lohng ma LEUM GOD El fahk uh.
“‘Tsono mkazi wachigololo iwe, imva mawu a Yehova!
36 Pa inge ma LEUM GOD Fulatlana El fahk: “Kom tuh sarukla nuknuk lom, na oana sie mutan kosro kom tuh eiskomyang sifacna nu sin mukul kawuk lom ac nu ke ma sruloala srungayuk nukewa lom. Ac kom oayapa uniya tulik nutum ac kisakunulos nu ke ma sruloala uh.
Ambuye Yehova akuti, popeza unavula ndi kuonetsa umaliseche wako mopanda manyazi, unachita chigololo ndi zibwenzi zako pamodzi ndi mafano ako onyansa, komanso popeza unapereka ana ako kuti aphedwe ngati nsembe zoperekedwa kwa mafano,
37 Ke sripa inge, nga ac eisani nufon mwet kom orek pwar nu se meet ah — elos su kom lungse ac elos su kom srunga. Nga ac usalosme elos in raunikomla, na nga ac sarukkomla ac sang elos in liye ke kom koflufol uh.
nʼchifukwa chake Ine ndidzasonkhanitsa zibwenzi zako zonse, zimene unkasangalala nazo, amene unkawakonda ndi amene unkawada. Ndidzawasonkhanitsa motsutsana nawe kuchokera ku madera onse okuzungulira ndipo Ine ndidzakuvula pamaso pawo, ndipo iwo adzaona umaliseche wako wonse.
38 Nga ac nununkekom ke sripen kom kunausla wulela in marut lom, ac oayapa akmas. In kasrkusrak lulap luk, nga wotela mu kom ac misa.
Ine ndidzakulanga monga mmene amalangira akazi amene amachita chigololo ndiponso opha anthu. Chifukwa cha ukali wanga ndi nsanje yanga, ndidzakhetsa magazi ako mokwiya kwambiri.
39 Nga ac filikomi ye ku lalos, ac elos ac kunausya acn kom orekmakin in kukakin monum, ac nien alu lom nu ke ma sruloala. Elos ac usla nuknuk lom ac mwe yun lom, ac filikomi koflufol.
Ndidzakupereka mʼmanja mwa zibwenzi zako ndi kuwononga nyumba zopembedzera mafano ako. Iwo adzakuvula zovala zako ndi kutenga zodzikometsera zako zabwino. Choncho adzakusiya wa maliseche ndi wausiwa.
40 “Elos ac purakak sie un mwet in tungal kom nwe ke kom misa, ac elos ac sipsipikya monum nu ke ip srisrik ke cutlass natulos.
Iwo adzabweretsa gulu la anthu limene lidzakuponya miyala ndi kukutematema ndi malupanga awo.
41 Elos ac esukak lohm sum nukewa, ac oru tuh mutan puspis in liye kaiyuk nu sum uh. Nga ac oru kom in tui liki moul in kosro lom an, ac oru kom in tia sifil sang mwe moul nu sin mukul kom orek pwar yoro.
Adzatentha nyumba zako ndi kukulanga iwe pamaso pa akazi ambiri. Ndidzathetsa chigololo chako, ndipo sudzalipiranso zibwenzi zako.
42 Ouinge kasrkusrak luk ac safla, ac nga fah inse misla. Nga fah tia sifil kasrkusrak, ac tia sifilpa lemta.
Ukali wanga udzalekera pamenepo ndipo sindidzakuchitiranso nsanje. Ndidzakhala chete osakwiyanso.
43 Kom mulkunla orekma luk nu sum ke kom srik ah, ac kom akkasrkusrakyeyu ke ma nukewa kom orala. Ouinge nga ac oru kom in eis mwatan ma inge nukewa. Efu kom ku sang elahn kosro in weang ma srungayuk nukewa ma kom orala?” LEUM GOD Fulatlana pa fahk ma inge.
“‘Popeza sunakumbukire masiku a ubwana wako koma unandikwiyitsa ndi zinthu zonsezi, Ine ndidzakubwezera ndithu chilango pamutu pako chifukwa cha zimene wachita, akutero Ambuye Yehova. Paja unawonjezera chigololo pa machitidwe ako onyansa.
44 LEUM GOD El fahk, “Jerusalem, mwet uh ac fahk soakas se inge keim: ‘Tulik mutan se ac kwa nina kial.’
“‘Taona, onse onena miyambi adzakuphera mwambi wakuti, ‘Make mbuu, mwana mbuu.’
45 Pwayena lah kom kwa nina kiom uh. El arulana srunga mukul tumal ac tulik natul. Kom oana tamtael wiom su srunga mukul tumalos ac tulik natulos. Kom, ac siti wiom ingan, ma nutin nina Hit se ac papa Amor se.
Ndiwedi mwana weniweni wamkazi wa mayi wako, amene amanyoza mwamuna wake ndi ana ake. Ndiwe mʼbale weniweni wa abale ako, amene amanyoza amuna awo ndi ana awo. Amayi ako anali Mhiti ndipo abambo ako anali Mwamori.
46 “Mutan se wiom ma matu pa Samaria layen epang, wi inkul ma oan raunela. Ac mutan se wiom ma fusr pa Sodom layen eir, wi inkul ma oan raunela.
Mkulu wako anali Samariya, ndipo iye pamodzi ndi ana ake aakazi ankakhala cha kumpoto kwako. Mngʼono wako, Sodomu ankakhala cha kummwera kwako pamodzi ndi ana ake aakazi.
47 Ku kom falkin in fahsr in falkalos ac etai ouiya srungayuk elos oru? Mo. In kitin pacl ah na kom orekma koluk yohk lukelos in ma nukewa kom oru.”
Iwe sunangotsatira kokha njira zawo zoyipa ndi kuchita zonyansa zawo, koma patangopita nthawi pangʼono machitidwe ako oyipa anaposa awo.
48 LEUM GOD Fulatlana El fahk, “Oana ke nga pa God moul, Sodom mutan se wiom ac inkul ma raunela, tiana oru ouiya koluk ma kom, ac inkul raunikomla ingan, orala.
Ndithu pali Ine wamoyo, akutero Ambuye Yehova, ngakhale mʼbale wako Sodomu ndi ana ake aakazi sanachitepo zimene iwe ndi ana ako aakazi munachita.
49 El, ac acn natul uh, arulana konkin ke pus mwe mongo nalos ac elos muta in misla ac insraelak, tusruktu elos tiana kasru mwet sugasrup ac mwet enenu.
“‘Tsono tchimo la mʼbale wako Sodomu linali ili: Iye ndi ana ake aakazi ankanyadira kuchuluka kwa chakudya ndi chuma chawo. Koma sanalabadireko kuthandiza osauka ndi aumphawi.
50 Elos inse fulat ac likkeke ac oru ma nga srunga, pwanang nga kunauselosla, oana kom etu.
Anali odzitukumula ndipo ankachita zonyansa pamaso panga. Nʼchifukwa chake ndinawachotsa monga mmene waoneramu.
51 “Ma koluk lal Samaria tia tafu nu ke ma koluk kom orala. Kom oru ma srungayuk arulana yohk liki ma el orala. Ouiya srungayuk lom uh arulana yohk, oru oana in wangin ma koluk lun mutan luo wiom kut fin kapsra ma koluk lalos nu ke ma koluk lom uh.
Samariya sanachite ngakhale theka la machimo amene unachita. Iwe wachita zinthu zonyansa zambiri kuposa iwo, motero kuti abale ako awiriwo amaoneka ngati olungama kuyerekeza ndi iye.
52 Inge mwekin lom uh ac fah oanna fom. Moul koluk lom an arulana yohk liki mutan luo wiom, pwanang mwet uh pangon mu wangin ma koluk lalos. Kom ac mwekyekinna, mweyen ma koluk lom uh oru oana in wangin mwatan mutan luo wiom.”
Tsono iwenso uyenera kuchita manyazi popeza waonetsa abale ako ngati osachimwa. Popeza kuti machimo ako ndi onyansa kwambiri kupambana awo, tsonotu iwowo akuoneka olungama kupambana iweyo. Choncho iwenso uchite manyazi ndi kunyozedwa popeza unaonetsa abale ako ngati olungama.
53 LEUM GOD El fahk nu sin Jerusalem, “Nga ac oru tuh Sodom ac inkul we, oayapa Samaria ac inkul we, in sifil kapkapak. Aok, nga ac oru tuh kom in kapkapak pac.
“‘Koma, ndidzadalitsanso Sodomu ndi ana ake aakazi. Ndidzadalitsanso Samariya ndi ana ake aakazi. Pa nthawi yomweyo ndidzakudalitsanso iwe Yerusalemu.
54 Kom ac mwekyekin orekma koluk lom an, na mwekin lom uh ac oru mutan wiom an in akilen lah ma koluk lalos uh srik liki kom.
Ndidzatero kuti uchite manyazi ndi kunyozeka chifukwa cha zonse zimene unachita powatonthoza anthuwa.
55 Elos ac sifilpa akwoyeyuk oana meet, na kom, ac inkul lom, ac sifil akwoyeyukla pac.
Motero mʼbale wako Sodomu ndi ana ake akadzakhala monga mmene analili poyamba paja, ndiponso mʼbale wako Samariya akadzakhalanso monga mmene anali poyamba paja, ndiye kuti iwenso ndi ana ako mudzakhala monga mmene munalili payamba paja.
56 Ya kom tuh tia orek aksruksruk ke acn Sodom in pacl kom inse fulat,
Kale lija pamene unkanyada, suja unkanyogodola mʼbale wako Sodomu
57 meet liki ma koluk lom fwackyak? Inge kom oapana el, sie mwe aksruksruk yurin mwet Edom, mwet Philistia, ac mutunfacl atulani lom su srungakom.
kuyipa kwako kusanadziwike? Koma tsopano wafanana naye. Wasandukano chinthu chonyozeka kwa anthu a ku Edomu ndi kwa onse owazungulira ndiponso kwa Afilisti. Ndithu onse amene akuzungulira amakunyoza.
58 Kom ac fah keok ke ouiya fohkfok ac srungayuk ma kom orala.” LEUM GOD pa fahk ma inge.
Choncho udzalangidwa chifukwa cha zigololo zako ndi machitidwe anu onyansa, akutero Yehova.
59 LEUM GOD Fulatlana El fahk, “Nga fah oru nu sum fal nu ke orekma lom, mweyen kom pilesru wulela lom ac kunausla wuleang inmasrlosr.
“‘Ine Ambuye Yehova ndikuti: Ndidzakulanga molingana ndi zimene unachita. Iwe unanyoza lumbiro lako pophwanya pangano langa.
60 Tusruktu nga fah esam na wuleang su nga orala nu sum ke kom srakna fusr, ac nga fah oakiya yurum sie wuleang su ac fah oan nwe tok.
Komabe, Ine ndidzakumbukira pangano limene ndinachita nawe mʼmasiku a unyamata wako, ndipo ndidzakhazikitsa pangano losatha ndi iwe.
61 Kom ac esam ouiyen moul lom ac mwekin kac ke kom ac sifil eis tamtael matu ac fusr wiom. Nga fah eisaloswot tuh elos in oana acn nutum, finne tia ipin wuleang se ma nga orala yurum ah.
Tsono udzakumbukira njira zako zakale. Udzachita manyazi polandiranso abale ako, wamkulu ndi wamngʼono yemwe. Ndidzawaperekanso kwa iwe kuti akhale ngati ana ako ngakhale kuti sali a mʼpangano langa ndi iwe.
62 Nga ac aksasuyela wuleang luk yurum, ac kom fah etu lah nga pa LEUM GOD.
Kotero ndidzakhazikitsa pangano langa ndi iwe, ndipo iwe udzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
63 Nga fah nunak munas ke ma koluk nukewa ma kom orala, tusruktu kom fah esam na ma ingan ac mwekin in fahk kutena ma.” LEUM GOD Fulatlana pa fahk ma inge.
Ndikadzakukhululukira zoyipa zako zonse zimene unachita, udzazikumbukira ndipo udzachita manyazi kwambiri, kotero kuti sudzatha nʼkuyankhula komwe, akutero Ambuye Yehova.’”

< Ezekiel 16 >