< Ezekiel 12 >
1 LEUM GOD El fahk nu sik,
Yehova anayankhula nane kuti,
2 “Kom, mwet sukawil moul la, kom muta inmasrlon mwet lungsena alein. Oasr mutalos, a elos tia liye mau. Oasr insraclos, a elos tia lohng mau, mweyen elos lungse alein.
“Iwe mwana wa munthu, ukukhala pakati pa anthu owukira, iwowo maso openyera ali nawo, koma sakuona ndipo makutu omvera ali nawo, koma sakumva chifukwa choti ndi anthu owukira.
3 “Inge, mwet sukawil, apweni kutu ma lom ingan in oana luman sie mwet kaing, ac mukuiyak meet liki fongeni. Lela mwet uh in liye lah kom ac som nu ke sie pac acn. Sahp mwet lungse alein ingan ac akilen kom.
“Choncho, iwe mwana wa munthu, longedza katundu wako wopita naye ku ukapolo. Unyamuke nthawi yamasana iwo akuona. Uchite ngati wanyamuka kuchoka kumene ukukhala kupita ku dziko lachilendo iwowo akuona. Mwina adzamvetsetsa, paja ndi anthu aupandu.
4 Apweni ma kom ac us nu in sruoh ke srakna len. Lela mwet nukewa in liye ke kom ac fahla ke ekela uh, elos in pangon mu kom ac som nu in sruoh.
Utulutse katundu wako wopita naye ku ukapolo nthawi ya masana iwo akuona. Ndipo nthawi ya madzulo, iwo akuona, uchoke monga ngati ukupita ku ukapolo.
5 Ke pacl elos ac liye kom an, pukanla sie pat ah ke sinka in lohm sum, ac eis ap lom an ac tufoki kac.
Iwo akuona, ubowole pa khoma ndipo utulutsirepo katundu wako.
6 Lela elos in liye ke kom ac srukak ap lom nu finpisom ac illa nu in lohsr uh. Afinya motom kom in tia ku in liye acn kom fahsr we. Ma kom oru inge ac fah sie mwe akul in sensenkin mwet Israel.”
Usenze katundu wako pa phewa iwo akuona, ndipo upite kunja ku mdima. Uphimbe nkhope yako kuti usaone pansi, pakuti ndakusandutsa iwe chizindikiro chochenjeza Aisraeli.”
7 Na nga oru oana LEUM GOD El fahk nu sik. In len sac nga apweni ap se in oana mwet ac kaingla se, ac ke eku sac ke mutawauk in lohsrla, nga pukanla sinka ah ke pouk, ac illa. Na nga srukak ap sac nu finpisuk ac som ke mwet nukewa liye.
Choncho ine ndinachita monga momwe anandilamulira. Nthawi yamasana ndinatulutsa zinthu zanga nditazimanga ngati ndikupita ku ukapolo. Ndipo nthawi yamadzulo ndinabowola khoma ndi manja anga. Pamene chisisira chinkayamba, ndinasenza katundu wanga pa phewa kutuluka naye iwo akuona.
8 Ke lotutan tok ah LEUM GOD El kaskas nu sik ac fahk,
Mmawa mwake Yehova anandiyankhula nati:
9 “Mwet sukawil, inge mwet alein lun Israel fin siyuk lah mea kom oru an
“Iwe mwana wa munthu, kodi anthu aupandu a Israeli sanakufunse kuti ukuchita chiyani?
10 kom fahkang ma nga, LEUM GOD Fulatlana, fahk nu selos. Kas inge ma nu sin fisrak se su leumi acn Jerusalem, oayapa mwet nukewa su muta we.
“Uwawuze kuti, ‘zimene ndikunena Ine Ambuye Wamphamvuzonse ndi izi: Uthengawu ndi wonena za kalonga wa ku Yerusalemu pamodzi ndi banja lonse la Israeli amene akukhala kumeneko.’
11 Fahk nu selos lah ma kom oru inge ac sie mwe akul nu ke ma ac sikyak nu selos. Elos ac fah mwet kaing ac mwet sruoh.
Uwawuze kuti, ‘Ndiwe chizindikiro chowachenjeza.’ “Zidzakuchitikirani monga momwe zakuchitikira iwemu. Iwo adzatengedwa kupita ku ukapolo.”
12 Fisrak se su leum faclos ac fah lippisauk ap lal in lohsr uh, ac kaingla ke pat se ma elos pukanla nu sel ke sinka ah. El ac fah afinya mutal ac tia liye acn el fahsr nu we.
“Kalonga wawo adzatenga katundu wake nʼchisisira nʼkunyamuka. Adzatulukira pa bowo limene anthu anabowola pa khoma. Adzaphimba nkhope yake kuti asaone kumene akupita.
13 Tusruk nga fah sisalik nwek nutik uh in sruokilya. Na nga fah usalla nu in siti Babylon, yen el ac misa we ac tia liye acn uh.
Ndidzayala ukonde wanga pa iye ndi kumukola mu msampha wanga. Ndidzabwera naye ku Babuloni, dziko la Akaldeya, koma sadzaliona dzikolo, ndipo adzafera kumeneko.
14 Nga fah akfahsryelik mwet nukewa inkul sel nu yen nukewa — mwet pwapu fulat lal ac mwet mweun karinginyal. Ac mwet uh fah sokolos in onelosi.
Ine ndidzabalalitsa kumbali zonse zinayi onse okhala naye pafupi, ndiwo omuthandiza ake pamodzi ndi ankhondo ake. Ndidzawalondola ndi lupanga losolola.
15 “Ke nga ac akfahsreloselik nu in mutunfacl saya uh, elos ac fah etu lah nga pa LEUM GOD.
“Iwo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova, ndikadzawamwaza pakati pa anthu a mitundu ina ndi kuwabalalitsira ku mayiko ena.
16 Nga ac fah lela kutu selos in moulla liki mweun, sracl, ac mas. Ouinge ke elos muta inmasrlon mwet in facl saya an elos fah akilen lupan moul koluk lalos, ac etu lah nga pa LEUM GOD.”
Koma ndidzasiyako ena pangʼono amene adzapulumuke ku lupanga, njala ndi mliri, kuti akafotokoze ntchito zawo zonse zonyansa pakati pa anthu achilendo kumene akupitako. Pamenepo adzadziwa kuti ndine Yehova.”
17 LEUM GOD El kaskas nu sik
Pambuyo pake Yehova anandiyankhulanso nati,
18 ac fahk, “Mwet sukawil, kom in rarrar ke pacl kom mongo, ac sangeng rarrar ke pacl kom ac nim.
“Iwe mwana wa munthu, uzinjenjemera ukamadya chakudya chako, ndipo uzinthunthumira ndi mantha ukamamwa madzi ako.
19 Fahk nu sin mwet in facl sacn nufon lah pa inge kas sin LEUM GOD Fulatlana nu sin mwet su muta Jerusalem — elos su srakna muta in facl selos: Elos ac fah rarrar ke pacl elos mongo, ac sangeng ac rarrar ke elos ac nim. Facl selos ac sikiyukla mweyen mwet nukewa su muta we elos moul sulallal ac kunaus ma sap.
Uwawuze anthu a mʼdzikomo kuti izi ndi zimene Ambuye Wamphamvuzonse akunena za anthu okhala mu Yerusalemu ndi dziko la Israeli: Iwo adzadya chakudya chawo ndi mantha ndi kumwa madzi awo ndi nkhawa. Zonse za mʼdziko lawo zidzalandidwa chifukwa cha ziwawa za anthu onse okhala mʼmenemo.
20 Siti nukewa ma nwanala ke mwet in pacl inge ac fah kunausyukla, ac facl sac nufon ac fah acn mwesisla. Na elos ac fah etu lah nga pa LEUM GOD.”
Mizinda imene ili ndi anthu idzasakazika ndipo dziko lidzasanduka chipululu. Pamenepo inu mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.”
21 LEUM GOD El kaskas nu sik,
Yehova anayankhulanso nane kuti,
22 ac fahk, “Mwet sukawil, efu ku mwet Israel elos kalwenina soakas se inge: ‘Pacl uh somla, a kas in palu uh tiana sikyak.’
“Iwe mwana wa munthu, kodi mwambi umene ukunenedwa mu Israeli ndi wotani: ‘Masiku akupita koma masomphenya onse sakukwaniritsidwa?’
23 Inge, fahkang nu selos ma nga, LEUM GOD Fulatlana, fahk ke ma ingan. Nga ac sisla soakas se ingan, na ac fah tia sifil srumunyuk in Israel. Fahkang nu selos lah pa inge pacl kas in palu uh ac akpwayeiyuk!
Choncho uwawuze anthuwo kuti, ‘Ine Ambuye Yehova ndidzawuthetsa mwambi umenewu ndipo sadzawunenanso mu Israeli.’ Uwawuze kuti, ‘masiku ayandikira oti zonse zimene ndinanena mʼmasomphenya zichitikedi.
24 “Ac fah tia sifil oasr aruruma kikiap ku kas in palu tia pwaye inmasrlon mwet Israel.
Pakuti masiku amenewo sikudzakhalanso masomphenya abodza kapena kuwombeza kwa chinyengo pakati pa anthu a Israeli.
25 Nga, LEUM GOD, fah sifacna kaskas nu selos, ac ma nga ac fahk uh ac tia pahtlac in sikyak. Kowos mwet likkeke, nga ac oru ma nga fahk mu nga ac oru ke pacl kowos srakna moul. Nga, LEUM GOD Fulatlana, pa fahk ma inge!”
Koma Ine Ambuye ndidzayankhula chimene ndikufuna, ndipo chidzachitikadi, osachedwa ayi. Pakuti mʼmasiku anu omwe ano, inu anthu opanduka, ndidzakwaniritsa chilichonse chimene ndidzanena. Ndikutero Ine Yehova.’”
26 LEUM GOD El fahk nu sik,
Yehova anandiyankhula nati:
27 “Mwet sukawil, mwet Israel elos nunku mu aruruma lom ac kas in palu lom tia ma ac sa sikyak, a ma na nwe tok.
“Iwe mwana wa munthu, Aisraeli akunena kuti, ‘masomphenya amene ukuona sadzachitika kwa zaka zambiri. Iwo akuti ukulosa za zinthu zimene zidzachitika ku tsogolo kwambiri.’
28 Ke ma inge fahkang nu selos lah nga, LEUM GOD Fulatlana, fahk mu: Ac fah tia sifilpa pahtlac. Ma nga fahkla uh ac orekla. Nga, LEUM GOD Fulatlana, pa fahk ma inge!”
“Choncho uwawuze kuti, ‘zimene Ine Ambuye Yehova ndikunena ndi izi: Zonena zanga sizidzachedwanso; chilichonse chimene ndikunena chidzachitikadi. Ndikutero Ine Yehova.’”