< Deuteronomy 32 >

1 “Faclu ac yen engyeng uh, lohng kas luk, Lohng akwoya ma nga ac fahk inge.
Mverani, inu mayiko a mmwamba ndipo ine ndidzayankhula; imva, iwe dziko lapansi, mawu a pakamwa panga.
2 Mwe luti luk fah putat oana tulin af, Ac sikyak fin faclu oana aunfong. Kas luk fah putat oana af sringsring nu fin sacn ma tufahna srunak, Oana af loang nu fin mah srisrik uh.
Chiphunzitso changa chigwe ngati mvula ndipo mawu anga atsike ngati mame, ngati mvumbi pa udzu watsopano, ngati mvula yochuluka pa zomera zanthete.
3 Nga fah kaksakin Inen LEUM GOD, Ac mwet lal fah fahkak fulatlana lal.
Ndidzalalikira dzina la Yehova. Aa, tamandani ukulu wa Mulungu wathu!
4 “LEUM GOD El nien molela kulana lowos, El suwohs ac pwaye in ma nukewa El oru; God lowos El oaru ac pwaye; El suwoswos ac El oru ma suwohs.
Iye ndi Thanthwe, ntchito zake ndi zangwiro, njira zake zonse ndi zolungama. Mulungu wokhulupirika amene salakwitsa, Iye ndiye wolungama ndi wosalakwa.
5 A kowos tia pwaye nu sel; kowos tia fal in mwet lal, Sie mutanfahl koluk ac kutasrik.
Koma iwo achita mosakhulupirika pamaso pake, iwo si ana akenso, koma iwo ndi mʼbado wachinyengo ndi wokhotakhota.
6 Kowos mwet lalfon ac selalkung, Ya kowos ac moli kulang lun LEUM GOD ouinge? El papa tomowos; El pa orekowosla, El oru tuh kowos in sie mutunfacl.
Kodi mukumubwezera Yehova chotere, inu anthu opusa ndi opanda nzeru? Kodi Iye si Atate anu, Mlengi wanu, amene anakupangani ndi kukuwumbani?
7 “Nunku ke pacl meet ah, ke fwilin mwet somsomla; Siyuk papa tomowos in srumun nu suwos lah mea sikyak meet, Siyuk sin mwet matu in srumun ke pacl somla.
Kumbukirani masiku amakedzana; ganizirani za mibado yakalekale. Funsa abambo ako ndipo adzakuwuza, akuluakulu ako, ndipo adzakufotokozera.
8 El su Fulatlana El oakiya acn nu sin kais sie mutunfacl; El kitalik acn, ac srisrngiya masrol nu ke acn in muta lun mwet uh. El sang lipufan in karingin kais sie mutunfacl.
Pamene Wammwambamwamba anapereka mayiko kwa anthu a mitundu ina kukhala cholowa chawo, pamene analekanitsa anthu onse, anayikira malire anthu onse molingana ndi chiwerengero cha ana a Israeli.
9 A El sulela fwilin tulik natul Jacob nu sel sifacna.
Pakuti gawo la Yehova ndi anthu ake, Yakobo ndiye cholowa chake.
10 “El konalosyak ke elos raraun yen mwesis, Sie acn wangin mwet muta we, a pusren ngirngir na lun eng uh. El loangelosla ac karinganulosyang, Mweyen elos arulana saok sel.
Anamupeza mʼchipululu, ku malo owuma ndi kopanda kanthu. Anamuteteza ndi kumusamalira; anamutchinjiriza ngati mwanadiso wake,
11 Oana ke sie eagle el luti ma fusr natul in sohksok ke el ac sinukla liki ang uh, Na el ukwalos in molelosla ac srakalosyak fin posohksok lal, Ouinge LEUM GOD El liyaung Israel tuh elan tia putatla.
ngati chiwombankhanga chimene chimasasula chisa chake nʼkumazungulira pamwamba pa ana ake, chimene chimatambalalitsa mapiko ake kuti chigwire anawo ndi kuwanyamula pa mapiko ake otambalalawo.
12 LEUM GOD mukena kolma mwet lal, Ac wangin kasru sin god saya.
Yehova yekha ndiye anamutsogolera; popanda thandizo la mulungu wachilendo.
13 “El lela nu selos in leumi fulan eol uh, Ac elos kang ma kapak inimae. Elos konauk honey inmasrlon eot uh; Sak olive sunalos kapak wo in acn eoteot uh.
Anamuyendetsa pamwamba pa mapiri a mʼdziko ndi kumudyetsa zipatso za mʼminda. Anamudyetsa uchi wofula pa thanthwe, ndiponso mafuta ochokera mʼnthaka ya miyala,
14 Cow ac nani natulos arulana sroanom tetelos; Un sheep ac nani ac cow natulos pa wo oemeet; Wheat ac wain lalos arulana yu.
pamodzi ndi chambiko ndi mkaka wochokera ku ngʼombe ndi nkhosa, ndiponso ana ankhosa onenepa ndi mbuzi, pamodzinso ndi nkhosa zazimuna zabwino za ku Basani ndiponso tirigu wabwino kwambiri. Munamwa vinyo wa thovu lofiira.
15 “Mwet lun LEUM GOD elos kasrupi, tusruktu elos orek likkeke lain God; Elos fatelik ke kainmongo lalos. Elos forla liki God su oralosla Ac pilesru Mwet Lango ku lalos.
Yesuruni ananenepa ndi kuyamba kuwukira; atakhuta, ananenepa ndi kukula thupi. Anasiya Mulungu amene anamulenga ndipo anakana Thanthwe ndi Mpulumutsi wake.
16 Alu lalos nu ke ma sruloala oru LEUM GOD El lemta; Orekma koluk lalos akkasrkusrakyal.
Anamuchititsa nsanje ndi milungu yawo yachilendo ndiponso anamukwiyitsa ndi mafano awo onyansa.
17 Elos orek kisa nu sin kutu god ma tia pwaye, God sasu ma papa matu tumalos tiana etu kac, Kutu god ma mwet Israel soenna wi alu nu kac.
Anapereka nsembe kwa ziwanda zimene si Mulungu, milungu imene sankayidziwa nʼkale lomwe, milungu yongobwera kumene, milungu imene makolo anu sankayiopa.
18 Elos mulkunla God lalos su langoelos ke ku lulap lal, El su sang moul nu selos.
Inu munasiya Thanthwe limene linakulerani; munayiwala Mulungu amene anakubalani.
19 “Ke LEUM GOD El liye ma inge, El arulana kasrkusrak, Ac sisla wen ac acn nukewa natul.
Yehova anaona zimenezi ndipo anawakana chifukwa ana ake aamuna ndi aakazi anamukwiyitsa.
20 El fahk, ‘Nga ac fah tia sifil kasrelos, Na nga fah liye lah mea ac sikyak nu selos, Elos mwet likkeke ac soaru.
Iye anati, “Ndidzawabisira nkhope yanga, ndi kuona kuti mathero awo adzakhala otani; pakuti ndi mʼbado wopotoka, ana amene ndi osakhulupirika.
21 Elos akkasrkusrakyeyu ke ma sruloala lalos, Ac oru nga in lemta ke sripen god lusrongten lalos, Kutu god su tia god pwaye. Ke ma inge nga fah oru sie mutunfacl lusrongten in akkasrkusrakyalos. Nga fah oru tuh elos in lemtai sie mutunfacl lalfon.
Anandichititsa kukhala wansanje pamene ankapembedza chimene si mulungu ndi kundikwiyitsa chifukwa cha mafano awo achabechabe. Ine ndidzawachititsa kuti achite nsanje ndi mtundu wina wopandapake; ndidzawakwiyitsa ndi mtundu wina wachabechabe.
22 Kasrkusrak luk ac fah ngutyak oana sie e Ac esukak faclu wi ma nukewa ma kapak fac. Ac fah sun acn loallana ke facl lun misa, Ac esukla kapin eol uh. (Sheol h7585)
Pakuti mkwiyo wanga wayaka ngati moto, umene umayaka mpaka ku dziko la anthu akufa. Motowo udzanyeketsa dziko lapansi ndi zokolola zake ndipo udzapsereza maziko a mapiri. (Sheol h7585)
23 “Nga fah sang nu faclos mwe ongoiya wangin saflaiya, Ac orekmakin mwe pisr nukewa nutik lainulos.
“Ndidzawawunjikira masautso ndipo mivi yanga yonse idzathera pa iwo.
24 Elos ac fah misa ke masrinsral ac ke musen fol ke mano; Elos ac misa ke mas na keok. Nga ac fah supwama kosro lemnak in anwuk nu selos, Ac wet pwasin in ngalselosi.
Ndidzawatumizira njala yoopsa, malungo woopsa ndi nthenda zofa nazo; ndidzawatumizira zirombo zakuthengo zowavuta, ululu wa njoka ya mʼphiri imene imakwawa pa fumbi.
25 Mweun ac fah oru mwet uh misa inkanek uh; Mwet muta in lohm uh ac tuninfongla. Mukul fusr ac mutan fusr fah misa; Wangin tulik fusr ku mwet matu ac fah moul.
Mʼmisewu lupanga lidzawasandutsa kukhala wopanda ana; mantha adzalamulira nyumba zawo. Anyamata ndi atsikana adzafa, ngakhalenso makanda ndi okalamba.
26 Nga nunku in sukelosla nukewa, In wangin mwet sifil esamulos.
Ine ndinanena kuti ndidzawamwaza ndi kuwafafaniza kuti anthu asawakumbukirenso,
27 Tusruktu nga tia lungse mwet lokoalok lalos in konkin Mu elos kutangla mwet luk, Ke nga sifacna pa kunauselosla.’
koma sindinafune kuti adani anga adzandinyoze, mwina adani anga sadzandimvetsetsa ndipo adzanena kuti, ‘Tagonjetsa anthuwa ndife; Yehova sanachite zonsezi.’”
28 “Israel el sie mutunfacl wangin nanka; Wangin na pwaye etu lalos.
Iwo ndi mtundu wopanda maganizo, iwo alibe nzeru nʼpangʼono pomwe.
29 Elos tiana akilenak lah efu ku kutangyukla elos. Elos tia kalem kac lah efu ma inge sikyak.
Ngati iwo akanakhala anzeru akanamvetsetsa izi ndi kuzindikira kuti mathero awo adzakhala otani!
30 Efu ku tausin se in kutangyukla sin mwet sefanna, Ac singoul tausin sin mwet luo na? Mweyen LEUM GOD lalos El som lukelos; God kulana lalos El siselosla.
Kodi munthu mmodzi akanathamangitsa bwanji anthu 1,000 kapena anthu awiri kuthamangitsa anthu 10,000, kuti awagonjetse, Thanthwe lawo likanapanda kuwagulitsa, Yehova akanapanda kuwataya?
31 Mwet lokoalok lalos etu na lah god lalos sifacna arulana munas, Tiana ku oana God lun Israel.
Pakuti thanthwe lawo silofanana ndi Thanthwe lathu, ngakhale adani athu amavomereza zimenezi.
32 Mwet lokoalok lalos kolukla, oana Sodom ac Gomorrah. Elos oana fain in grape ma fokkakin grape mwen ac pwasin,
Mpesa wawo umachokera ku mpesa wa ku Sodomu ndiponso ku minda ya ku Gomora. Mphesa zawo zili ndi ululu wakupha ndipo maphava ake ndi owawa.
33 Ac wain nimalos oana pwasin ma tuku ke oalin wet uh.
Vinyo wawo ndi wa ululu wa njoka, ululu woopsa wa mphiri.
34 “LEUM GOD El esam ma mwet lokoalok lalos tuh oru; Ac El tupan sie pacl fal in kaelos kac.
“Kodi zimenezi sindinazisunge ndi kuzitsekera mʼkatikati mwa chuma changa?
35 LEUM GOD El ac fah oru foloksak lal ac kaelos; Oasr pacl se ac tuku ke elos ac ikori, Len in ongoiya lalos apkuranme.
Kubwezera chilango nʼkwanga; ndidzawalanga ndine. Pa nthawi yake phazi lawo lidzaterera; tsiku lawo la masautso layandikira ndipo chiwonongeko chawo chikubwera pa iwo mofulumira.”
36 LEUM GOD El ac fah molela mwet lal Ke pacl se El liye lah ku lalos wanginla. El ac pakomutalos su kulansupwal Ke El ac liye lupan munasla lalos.
Yehova adzaweruza anthu ake ndipo adzachitira atumiki ake chifundo pamene adzaona kuti mphamvu zawo zatha ndipo kuti palibe amene watsala, kapolo kapena mfulu.
37 Na LEUM GOD El ac fah siyuk sin mwet lal, ‘Pia god kulana lowos ma kowos lulalfongi uh?
Iye adzanena kuti, “Nanga ili kuti milungu yawo, thanthwe limene ankabisalamo,
38 Kowos kitalos ke mwe mongo yuyu ke mwe kisa lowos Ac sang wain ma kisakinyuk elos in nim. Inge, lela god ingan in tuku kasrekowos, Ac molikowosla.
milungu imene inkadya mafuta a nsembe zawo ndi kumwa vinyo wa chopereka chawo cha chakumwa?” Iwuzeni ibwere kuti idzakuthandizeni! Ibwere kuti idzakutetezenitu!
39 “‘Liye, nga mukefanna pa God; Wangin pac sie god sayuk. Nga uniya ac nga sang moul, nga kanteya ac nga akkeyala, Ac wangin sie ku in lain ma nga oru.
“Onani tsopano kuti Ine ndine Iyeyo! Palibe mulungu wina koma Ine ndekha. Ine ndimapha ndiponso kupereka moyo, ndavulaza ndipo ndidzachiritsa, ndipo palibe angathe kupulumutsa munthu mʼmanja mwanga.
40 In oana ke nga pa God moul, Nga sralak pouk ac wulela ku
Ndikweza dzanja langa kumwamba ndi kulumbira kuti, ‘Pali Ine wamoyo wamuyaya,
41 Lah nga fah tamla cutlass saromrom nutik Ac liyaung tuh nununku suwohs in orek. Nga fah foloksak nu sin mwet lokoalok luk Ac kaelos su srungayu.
pamene ndidzanola lupanga langa lonyezimira ndipo dzanja liligwira pakubweretsa chiweruzo, ndidzabwezera chilango adani anga ndi kulanga onse odana nane.
42 Sukan pisr nutik fah tultul ke srah kaclos, Ac cutlass nutik fah onelosi nukewa su lainyu. Nga fah tia likiya moul lun kutena mwet su lainyu; Finne mwet pakpuki ke cutlass, wi mwet sruoh ke mweun, elos nukewa fah misa.’
Mivi yanga idzakhuta magazi awo pamene lupanga langa lidzawononga mnofu: magazi a anthu ophedwa ndi ogwidwa ukapolo, mitu ya atsogoleri a adani.’”
43 “Kowos mutanfahl uh, kowos in kaksakin mwet lun LEUM GOD— El kalyaelos nukewa su onelosla. El foloksak nu fin mwet lokoalok lal, Ac El nunak munas ke ma koluk lun mwet lal.”
Kondwerani, inu mitundu yonse ya anthu pamodzi ndi anthu ake, pakuti Iye adzabwezera chilango anthu amene anapha atumiki ake; adzabwezera chilango adani ake ndipo adzakhululukira dziko lake ndi la anthu ake.
44 Moses ac Joshua, wen natul Nun, eltal fahkak kas ke on soko inge tuh mwet Israel nukewa in ku in lohng.
Mose anabwera ndi Yoswa mwana wa Nuni ndipo anayankhula mawu onsewa mʼnyimbo anthu akumva.
45 Ke Moses el aksafyela luti lal ke kas lun God nu sin mwet uh
Mose atatsiriza kunena mawu onsewa pamtima kwa Aisraeli,
46 el fahk, “Aklohya in akos sap inge nukewa ma nga sot nu suwos misenge. Kalweni nu sin tulik nutuwos tuh elos in ku in oaru ac akos mwe luti nukewa lun God.
iye anawawuza kuti, “Muwasunge bwino mu mtima mwanu, mawu onse amene lero lino ndikukuwuzani kuti mudzawuze ana anu, kuti adzamvere mosamalitsa mawu onse a malamulo amenewa.
47 Mwe luti inge tia kas lusrongten — a moul na lowos. Akos ma inge ac kowos fah moul paht fin facl se lefahl ingo Infacl Jordan ma kowos apkuran in oakwuki we.”
Mawuwa sikuti ndi mawu achabe kwa inu. Mawuwa ndi moyo wanu. Mukawamvera mudzakhala ndi moyo wautali mʼdziko limene mukukalitenga kukhala lanu mukawoloka Yorodani.”
48 In len sacna LEUM GOD El fahk nu sel Moses,
Tsiku lomwelo Yehova anawuza Mose kuti,
49 “Fahla nu Fineol Abarim in acn Moab tulanang siti Jericho. Fanyak Fineol Nebo ac ngetla liye facl Canaan ma nga akola in sang nu sin mwet Israel.
“Pita ku mapiri a ku Abarimu ukakwere pa Phiri la Nebo ku Mowabu, moyangʼanana ndi Yeriko, ndipo ukaone dziko la Kanaani, dziko limene ndikulipereka kwa Aisraeli kukhala lawo.
50 Kom ac fah misa fineol soko an oana ke Aaron, tamulel lom, el misa Fineol Hor,
Iwe udzafera pa phiri limenelo ndipo udzapita kumene makolo ako anapita, monga mʼbale wako Aaroni anafera pa phiri la Hori ndipo anakakhala ndi anthu a mtundu wake.
51 mweyen komtal kewa tuh fahsr sayen ma nga sapkin nu sumtal ye mutun mwet Israel. — Pacl se komtal tuh muta ke kof in acn Meribah, apkuran nu ke siti Kadesh in acn mwesis Zin, komtal tuh tia akfulatyeyu ye mutun mwet uh.
Chifukwa chake nʼchakuti inu nonse awiri simunakhulupirike kwa Ine pamaso pa Aisraeli pa madzi a Meriba ku Kadesi mʼchipululu cha Zini chifukwa simunandilemekeze kokwanira pakati pa Aisraeli.
52 Kom ac ngetla liye facl sac ke oan loessula, tusruktu kom ac tia ilyak nu in facl sac su nga ac sang nu sin mwet Israel.”
Choncho udzalionera kutali dziko limene ndikupereka kwa Aisraeli. Sudzalowa mʼdziko limene ndi kulipereka kwa Aisraeli.”

< Deuteronomy 32 >