< Luo Samuel 9 >

1 Sie len ah David el siyuk, “Ya oasr mwet lula in sou lal Saul? Fin oasr, nga lungse fahkak kulang nu sel ke sripal Jonathan.”
Davide anafunsa kuti, “Kodi alipo amene watsala mʼbanja la Sauli kuti ndimuchitire chifundo chifukwa cha Yonatani?”
2 Oasr sie mwet kulansap lal Saul, el pa Ziba, na fwackyang nu sel elan som nu yorol David. Ke el som, tokosra el siyuk, “Ku kom pa Ziba?” Na el topuk, “Aok, nga tupan enenu lom.”
Tsono panali mtumiki wina wa banja la Sauli wotchedwa Ziba. Iwo anamuyitana kuti aonekere pamaso pa Davide, ndipo mfumu inamufunsa kuti, “Kodi ndiwe Ziba?” Iyeyo anayankha kuti, “Ine mtumiki wanu.”
3 Tokosra el siyuk sel, “Ku oasr mwet lula in sou lal Saul su nga ac ku in kasru ac fahkak kulang nu sel, oana nga tuh wulela nu sin LEUM GOD mu nga ac oru?” Ac Ziba el fahk, “Sie sin wen natul Jonathan el srakna moul, tuh el sukapasla.”
Mfumu inafunsa kuti, “Kodi palibe amene watsala wa banja la Sauli amene ndingamuchitire chifundo cha Mulungu?” Ziba anayankha mfumu kuti, “Alipo mwana wa Yonatani, koma ndi wolumala mapazi ake onse.”
4 Na tokosra el siyuk, “El aya?” Ziba el fahk, “El oasr lohm sel Machir wen natul Ammiel, in acn Lodebar.”
Mfumu inafunsa kuti, “Ali kuti?” Ziba anayankha kuti, “Iye ali ku nyumba ya Makiri mwana wa Amieli ku Lodebara.”
5 Ouinge Tokosra David el sapla solal.
Kotero mfumu inamubweretsa kuchokera ku Lodebara, ku nyumba ya Makiri mwana wa Amieli.
6 Ke Mephibosheth, wen natul Jonathan natul Saul, el tuku el srimi ye mutal David in akfulatyal. Na David el fahk, “Mephibosheth.” Ac el topuk, “Nga pa inge, nga tupan enenu lom.”
Mefiboseti mwana wa Yonatani, mwana wa Sauli atafika kwa Davide, anawerama pansi kupereka ulemu kwa iye. Davide anati, “Mefiboseti!” Iye anayankha kuti, “Ine mtumiki wanu.”
7 David el fahk, “Nikmet sangeng. Nga ac fah kulang nu sum ke sripal Jonathan, papa tomom. Nga fah folokonot acn nukewa lal Saul, papa matu tomom, ac pacl nukewa kom arulana sukosok in tuku nu ke tepu luk uh.”
Davide anati kwa iye, “Usachite mantha, pakuti ndidzakuchitira ndithu chifundo chifukwa cha abambo ako Yonatani. Ine ndidzakubwezera iwe dziko lonse limene linali la agogo ako Sauli, ndipo iweyo udzadya ndi ine nthawi zonse.”
8 Mephibosheth el sifilpa srimi ac fahk, “Efu kom oru arulana wo nu sik, sruhk nga tia wo liki kosro ngalngul misa soko?”
Mefiboseti anawerama pansi ndipo anati, “Mtumiki wanu ndine yani kuti musamale galu wakufa ngati ine?”
9 Na tokosra el pangnol Ziba, mwet kulansap lal Saul, ac fahk, “Nga ac folokonang ma nukewa lal Saul, leum lom, ac lun sou lal, nu sel Mephibosheth, wen nutin natul Saul.
Kenaka Davide anayitanitsa Ziba, mtumiki wa Sauli, ndipo anati, “Ine ndapereka kwa chidzukulu cha mbuye wako chilichonse chimene chinali cha Sauli ndi banja lake.
10 Kom, ac wen nutum ac mwet kulansap lom, ac fah imai acn inge nu sin sou lal Saul, leum lom. Kowos in orani fokin kosrani ac sang kitalos. Tusruktu Mephibosheth sifacna el ac fah sukosok nu ke tepu luk pacl nukewa.” (Oasr wen singoul limekosr natul Ziba, ac mwet kulansap longoul lal.)
Iwe ndi ana ndi antchito anu muzimulimira mʼdziko lake ndipo muzibweretsa zokololazo kuti chidzukulu cha mbuye wako chikhale ndi chakudya. Ndipo Mefiboseti, chidzukulu cha mbuye wako adzadya ndi ine nthawi zonse.” (Tsono Ziba anali ndi ana aamuna khumi ndi asanu ndi antchito makumi awiri).
11 Na Ziba el fahk, “O Tokosra, nga fah oru ma nukewa ma kom sapkin.” Ouinge Mephibosheth el wi mongo ke tepu lun tokosra, oapana sie tulik nutin tokosra.
Ndipo Ziba anati kwa mfumu, “Mtumiki wanu adzachita chilichonse chimene mbuye wanga mfumu mudzalamulire wantchito wanu kuti achite.” Kotero Mefiboseti ankadya ndi Davide monga mmodzi wa ana a mfumu.
12 Oasr sie wen fusr natul Mephibosheth pangpang Mica. Mwet nukewa in sou lal Ziba elos mwet kulansapla lal Mephibosheth.
Mefiboseti anali ndi mwana wamngʼono wamwamuna wotchedwa Mika, ndipo onse a banja la Ziba anali antchito a Mefiboseti.
13 Ouinge Mephibosheth, su ulla nial kewa, el mutana Jerusalem ac mongo yurin tokosra ke pacl in mongo nukewa.
Ndipo Mefiboseti anakhala mu Yerusalemu chifukwa nthawi zonse amadya ndi mfumu. Iye anali wolumala mapazi ake onse.

< Luo Samuel 9 >