< Luo Samuel 7 >

1 Tokosra David el muta okak in lohm sin tokosra, ac LEUM GOD El karinganulang liki mwet lokoalok lal nukewa.
Mfumu itakhazikika mʼnyumba yake yaufumu, Yehova atayipatsa mpumulo kwa adani ake onse woyizungulira,
2 Na tokosra el fahk nu sel Nathan mwet palu, “Inge nga muta in sie lohm musala ke sak cedar, a Tuptup in Wuleang lun LEUM GOD oan in lohm nuknuk se!”
mfumuyo inawuza mneneri Natani kuti, “Ine pano ndikukhala mʼnyumba yomanga ndi mitengo ya mkungudza, pomwe Bokosi la Mulungu lili mu tenti.”
3 Nathan el topuk, “Oru ma nukewa ma kom nunku an, mweyen LEUM GOD El wi kom.”
Natani anayankha mfumu kuti, “Chitani chilichonse chimene chili mu mtima mwanu chifukwa Yehova ali nanu.”
4 Tusruk in fong sac LEUM GOD El fahk nu sel Nathan,
Usiku umenewo mawu a Yehova anafika kwa Natani ndipo anati,
5 “Fahla fahk nu sel David mwet kulansap luk, lah nga fahk, ‘Tia kom pa mwet se ac musai sie tempul nu sik nga in muta loac.
“Pita kamuwuze mtumiki wanga Davide kuti, ‘Yehova akunena kuti: kodi ndiwe amene udzandimangira Ine nyumba yokhalamo?
6 Oe ke pacl se nga molela mwet Israel liki facl Egypt ah me nwe inge, nga soenna muta in sie tempul. Nga fufahsryesr na ac mutana in lohm nuknuk.
Ine sindinakhalepo mʼnyumba kuyambira tsiku limene ndinatulutsa Aisraeli mʼdziko la Igupto mpaka lero lino. Ndakhala ndikuyenda uku ndi uku ndipo mokhala mwanga munali mu tenti.
7 In fufahsryesr luk nukewa yurin mwet Israel, wanginna pacl nga tuh siyuk sin mwet kol su nga sulela ah lah efu ku elos tia musaela sie tempul ma orek ke sak cedar ah sik.’
Konse ndakhala ndikuyenda ndi Aisraeli onse, kodi ndinanenapo kwa wina aliyense atsogoleri awo, amene ndinamulamula kuweta anthu anga Aisraeli kuti, nʼchifukwa chiyani simunandimangire nyumba ya mitengo ya mkungudza?’”
8 “Ouinge fahk nu sel David mwet kulansap luk, lah nga, LEUM GOD Kulana, fahk nu sel, ‘Nga eiskomla liki liyaung sheep inimae, ac oru tuh kom in leum fin mwet luk, mwet Israel.
“Ndipo tsopano umuwuze mtumiki wanga Davide kuti, ‘Yehova Wamphamvuzonse akuti: Ine ndinakutenga ku busa ukuweta nkhosa kuti ukhale mtsogoleri wa anthu anga Aisraeli.
9 Nga tuh wi kom yen nukewa kom fahla nu we, ac nga tuh kutangla mwet lokoalok lom nukewa ye motom. Nga fah oru kom in pwengpeng oana mwet kol fulatlana fin faclu.
Ineyo ndinali nawe kulikonse kumene unkapita, ndipo ndachotsa adani ako onse pamaso pako. Tsopano ndidzakuza dzina lako kuti likhale mʼgulu la mayina a anthu otchuka kwambiri pa dziko lapansi.
10 Nga tuh sulela sie acn nu sin mwet luk mwet Israel, ac oakelosi we tuh elos in ku in muta ke acn selos sifacna, ac tia sifil aklokoalokyeyuk. Mwet koluk fah tia sifil akkeokyalos oana meet
Ndipo ndidzawapatsa malo anthu anga Aisraeli ndipo ndidzawadzala pamalo awoawo kuti asadzavutitsidwenso. Anthu oyipa sadzawazunzanso monga ankachitira poyamba paja,
11 ke pacl lun mwet nununku ah me, su nga tuh pakiya tuh elos in kol mwet luk mwet Israel. Nga wulela nu sum lah nga ac karingin kom liki mwet lokoalok lom nukewa, oayapa nga fah oru in oasr tulik nutum.
monga akhala akuchitira kuchokera nthawi imene ndinasankha atsogoleri a anthu anga Aisraeli. Ine ndidzakupatsaninso mpumulo kwa adani anu onse. “‘Yehova akulengeza kwa iwe kuti Iye mwini adzakhazikitsa banja lako:
12 Ke kom ac misa ac pukpuki yurin mwet matu lom, nga ac oru sie sin wen nutum in tokosra, ac nga ac fah liyaung tokosrai lal in ku.
Masiku ako akadzatha ndipo ukadzakapuma ndi makolo ako, Ine ndidzawutsa mphukira yako imene idzalowa mʼmalo mwako, imene idzachokera mʼthupi mwako, ndipo ndidzakhazikitsa ufumu wake.
13 El pa mwet se su ac musai sie tempul nu sik, ac nga fah oru fita lal in leum ma pahtpat.
Iye ndiye amene adzamangire nyumba Dzina langa, ndipo Ine ndidzakhazikitsa ufumu wake kwamuyaya.
14 Nga fah papa tumal ac el fah wen nutik. El fin oru kutena ma sufal, nga ac fah kael oana sie papa su kai tulik natul.
Ine ndidzakhala abambo ake, ndipo iye adzakhala mwana wanga. Akadzachita choyipa, Ineyo ndidzamulanga ndi ndodo ndi zikwapu za anthu.
15 Tusruktu nga ac fah tia tulokinya kasru luk nu sel oana nga tuh oru nu sel Saul, su nga sisella tuh kom in tokosrala.
Koma sindidzasiya kumukonda, monga ndinachitira ndi Sauli, amene ndinamuchotsa iwe usanakhale mfumu.
16 Ac fah oasr tulik nutum in fwil nukewa, ac nga ac fah oru tuh tokosrai lom in oan ma pahtpat. Ac fah wangin saflaiyen tokosrai lom nwe tok.’”
Nyumba yako ndi ufumu wako zidzakhala zamuyaya pamaso panga. Mpando wako waufumu udzakhazikika kwamuyaya!’”
17 Nathan el fahkang nu sel David ma nukewa ma God El akkalemye nu sel.
Natani anafotokozera Davide mawu onse avumbulutso limene analandira.
18 Na Tokosra David el som nu in Lohm Nuknuk sin LEUM GOD, ac el muta nu ten ac pre, “O LEUM GOD Fulatlana, nga ac sou luk arulana kupansuwol ke ma kom oru nu sesr tari.
Choncho Davide analowa mu tenti nakhala pamaso pa Yehova, ndipo anati: “Inu Yehova Wamphamvuzonse, ine ndine yani, ndipo banja langa nʼchiyani kuti mundifikitse pamene ndafikapa?”
19 Ac inge kom sifilpa oru yohk liki. LEUM GOD Fulatlana, kom orek wulela pac tari ke tulik nutik nwe ke yac yac fahsru. Ac kom oru tuh sie mwet in ku in liye ma inge, O LEUM GOD Fulatlana!
Ndipo kukhala ngati izi ndi zosakwanira pamaso panu, Inu Ambuye Wamphamvuzonse, mwayankhula zatsogolo la banja la mtumiki wanu. Kodi umu ndi mmene mumachitira ndi munthu, Inu Ambuye Wamphamvuzonse?
20 Mea pac nga ku in fahk nu sum! Kom eteyu, mwet kulansap lom.
Kodi Davide anenenso chiyani kwa Inu? Pakuti Inu Ambuye Wamphamvuzonse mukumudziwa mtumiki wanu.
21 Ma inge nukewa orek ke sripen lungse lom ac oakwuk lom. Kom orala ma yohk inge nukewa tuh in mwe luti nu sik.
Chifukwa cha mawu anu komanso mwa chifuniro chanu, mwachita chinthu chachikulu ichi ndipo mwachiwulula kwa mtumiki wanu.
22 Fuka yokiyen fulat lom, LEUM GOD Fulatlana! Wangin sie oana kom. Kut nuna etu oemeet me lah kom mukefanna pa God.
Inu ndinu wamkulu, Yehova Wamphamvuzonse! Palibe wina wofanana nanu, ndipo palibe Mulungu wina koma Inu nokha, monga tamvera ndi makutu athu.
23 Wangin pac sie mutunfacl fin faclu oana Israel, su kom molelosla liki kohs lalos tuh elos in mwet lom sifacna. Orekma yohk ac wolana su kom oru nu selos ah, oru tuh pwengpeng lom in fahsrelik nu yen nukewa faclu. Kom tuh lusak mutunfacl saya oayapa god lalos ye mutun mwet lom, aok, mwet su kom aksukosokyela liki facl Egypt tuh in ma lom.
Ndipo ndi ndani wofanana ndi anthu anu Aisraeli, mtundu wokhawo pa dziko lapansi umene Mulungu wake anapita kukawuwombola monga anthu akeake ndi kukadzitchukitsa yekha pochita zinthu zodabwitsa zazikulu, pothamangitsa mitundu ina ndi milungu yawo pamaso pa anthu ake, amene Inu munawawombola ku Igupto?
24 Kom orala Israel in mwet lom ma pahtpat, ac kom, LEUM GOD, pa God lalos.
Inu mwawapanga anthu anu Aisraeli kukhala anuanu kwamuyaya, ndipo Inu, Inu Yehova ndinu Mulungu wawo.
25 “Inge, LEUM GOD, oru tuh wuleang se su kom wulela keik ac ke tulik nutik in akpwayeyuk nwe tok, ac oru oana ma kom fahk mu kom ac oru.
“Ndipo tsopano Yehova Mulungu, sungani kwamuyaya lonjezo limene mwachita ndi mtumiki wanu ndi banja lake. Chitani monga mwalonjezera,
26 Pweng keim ac fah arulana yohk, ac mwet uh ac fah fahk nwe tok, ‘LEUM GOD Kulana, El God lun Israel.’ Ac kom fah karinganang tuh fita luk in leum in fwil nukewa.
kotero dzina lanu lidzakhala lotchuka mpaka muyaya. Ndipo anthu adzanena kuti, ‘Yehova Wamphamvuzonse ndi Mulungu wa Israeli!’ Ndipo banja la mtumiki wanu Davide lidzakhazikika pamaso panu.
27 LEUM GOD Kulana, God lun Israel! Nga pulaik in pre nu sum ouinge, mweyen kom akkalemye ma inge nukewa nu sik, mwet kulansap lom, ac kom fahk pac nu sik lah kom ac oru fwil nutik nukewa in tokosra.
“Inu Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli, mwaululira mtumiki wanu ponena kuti, ‘Ine ndidzakumangira iwe nyumba!’ Nʼchifukwa chake ine mtumiki wanu ndalimba mtima kupemphera motere.
28 “Ac inge, LEUM GOD Fulatlana, kom pa God. Kom karinganang wuleang lom pacl nukewa, ac kom oru wuleang wolana se inge nu sik.
Inu Ambuye Wamphamvuzonse, ndinu Mulungu! Mawu anu ndi odalirika, ndipo mwalonjeza zinthu zabwinozi kwa mtumiki wanu.
29 Nga siyuk sum in akinsewowoye fita luk, tuh elos in engankin lungkulang lom pacl e nukewa. LEUM GOD Fulatlana, kom pa orala wulela se inge, ac mwe akinsewowo lom ac fah oan fin fita luk ma pahtpat.”
Ndipo tsopano chikukomereni kudalitsa banja la mtumiki wanu, kuti likhale mpaka muyaya pamaso panu. Pakuti Inu, Yehova Wamphamvuzonse, mwayankhula, ndipo ndi mʼdalitso wanu banja la mtumiki wanu lidzakhala lodalitsika mpaka muyaya.”

< Luo Samuel 7 >