< Luo Samuel 15 >

1 Tukun ma inge Absalom el akoela chariot se ac horse ekasr nu sel sifacna, oayapa mwet lumngaul in atlol.
Patapita nthawi, Abisalomu anadzipezera galeta ndi akavalo pamodzi ndi amuna makumi asanu amene amathamanga patsogolo pake.
2 El ac toang tukakek ac som tu pe inkanek ah ke mutunpot lun siti ah. Na pacl nukewa mwet se fin tuku in fahkak sie fohs ku alein ma el lungse tuh tokosra elan aksuwosye, na Absalom el ac pangonma mwet sac ac siyuk lah el tuku ya me. Tukun mwet sac el fahk lah el tuku ke sruf ya me,
Iye amadzuka mmamawa ndi kuyima pa njira yopita ku chipata cha mzinda. Munthu wina aliyense akakhala ndi zodandaula zopita nazo kwa mfumu kuti akaweruze, Abisalomu amamuyitana iye ndi kumufunsa kuti, “Kodi ukuchokera ku limodzi mwa mafuko a Israeli?”
3 na Absalom el ac fahk, “Liye, ma sap uh wi kom lac, tusruktu wangin aolyal tokosra in lohng ke tukak lom uh.”
Kenaka Abisalomu amanena kwa iye kuti, “Taona, madandawulo ako ndi abwino ndi oyenera, koma palibe woyimira mfumu woti akumvere.”
4 Ac el ac sifilpa fahk, “Saok ngan mwet nununku se! Lukun kutena mwet su oasr amei ku tukak yorol, ku in tuku nu yuruk ac nga sang nununku suwohs nu sel.”
Ndipo Abisalomu amawonjezera kunena kuti, “Ine ndikanangosankhidwa kukhala woweruza mʼdziko muno bwenzi munthu aliyense amene ali ndi madandawulo kapena milandu akubwera kwa ine ndipo ndikanaonetsetsa kuti chilungamo chachitika.”
5 Mwet sac fin kalukyang nu yorol Absalom in srimi ye mutal, na Absalom el ac saplakot sruokilya ac ngokya mutal.
Ndipo nthawi zonse amati munthu akasendera pafupi ndi kumugwandira, Abisalomu amatambalitsa dzanja lake, kumuyimiritsa munthuyo ndi kupsompsona.
6 Absalom el oru ouinge nu sin mwet Israel nukewa su tuku nu yurin tokosra in suk nununku suwohs, ouinge mwet nukewa insewowo sel.
Abisalomu amachitira izi Aisraeli onse amene amabwera kwa mfumu kuti adzaweruzidwe ndipo Abisalomuyo anagwira mtima anthu a mu Israeli.
7 Tukun yac akosr Absalom el fahk nu sel Tokosra David, “Leum luk, lela ngan som nu Hebron, ac akfalye wulela se nga wuleang nu sin LEUM GOD kac.
Patapita zaka zinayi Abisalomu anati kwa mfumu, “Loleni ndipite ku Hebroni kuti ndikakwaniritse lonjezo limene ndinachita kwa Yehova.
8 Ke pacl se nga muta in acn Geshur in acn Syria, nga tuh wulela nu sin LEUM GOD mu El fin folokinyula nu Jerusalem, nga ac alu nu sel in acn Hebron.”
Pamene mtumiki wanu amakhala ku Gesuri ku Aramu, anachita lonjezo ili: ‘Ngati Yehova adzandibweretsadi ku Yerusalemu, ndidzapembedza Yehovayo mu Hebroni.’”
9 Na tokosra el fahk, “Fahsr in misla.” Ouinge Absalom el som nu Hebron.
Mfumu inati kwa iye, “Pita mu mtendere” Kotero iye anapita ku Hebroni.
10 Tusruktu el supwala mwet utuk kas nu sin sruf nukewa Israel in fahk, “Pacl se kowos lohngak pusren mwe ukuk uh, kowos sala ac fahk, ‘Absalom el tokosrala in acn Hebron!’”
Ndipo Abisalomu anatuma amithenga ake mwamseri kwa mafuko onse a Israeli kukanena kuti, “Mukangomva kulira kwa malipenga pamenepo munene kuti, ‘Abisalomu ndiye mfumu mu Hebroni.’”
11 Absalom el tuh suli mwet luofoko in acn Jerusalem in welul som. Elos tiana etu ke pwapa lukma se el akoo — elos fahsrna ke sripen elos lulalfongel.
Anthu 200 ochokera mu Yerusalemu anapita naye Abisalomu. Iwo anayitanidwa monga alendo ndipo anapita osadziwa chilichonse pa nkhaniyi.
12 Ke pacl Absalom el oru kisa lal, el supwala pac mwet nu in acn Gilo elos in solal Ahithophel, su sie sin mwet pwapa fulat lal Tokosra David. Pwapa se lal Absalom in lain tokosra inge kui, ac pisen mwet lal yokyokelik.
Pamene Abisalomu amapereka nsembe, iye anayitanitsanso Ahitofele Mgiloni, mlangizi wa Davide, wa ku Gilo, kotero kuwukiraku kunakula kwambiri, ndipo anthu otsatira Abisalomu anapitirira kuchuluka.
13 Sie mwet utuk kas el som fahk nu sel David, “Mwet Israel elos wulela lah elos ac welulla Absalom.”
Munthu wina anabweretsa uthenga ndi kudzamuwuza Davide kuti, “Mitima ya Aisraeli onse ili pa Abisalomu.”
14 Ouinge David el fahk nu sin mwet pwapa nukewa lal su welul muta Jerusalem, “Kut enenu in som liki acn Jerusalem ingena, kut fin lungse kaingla lukel Absalom! Aksaye! El akura tuku nu inge, kutangkutla ac uniya mwet nukewa in siti uh!”
Ndipo Davide anati kwa akuluakulu ake amene anali mu Yerusalemu. “Bwerani! Tiyeni tithawe, mwina palibe adzapulumuke kwa Abisalomu. Tiyeni tichoke msanga, mwina iye adzabwera msanga ndi kutipitirira, nʼkuwononga ife ndi mzinda wathu ndi lupanga.”
15 Na elos fahk, “Aok, leum fulat lasr. Kut akola in oru ma nukewa kom fahk.”
Akuluakulu a mfumu anamuyankha kuti, “Antchito anu ndi okonzeka kuchita chilichonse chimene mbuye wathu mfumu mukufuna kuchita.”
16 Na tokosra el mukuila wi sou lal nukewa, ac mwet pwapa lal, sayen mutan kulansap singoul kial ma el filiya in karingin lohm sin tokosra.
Mfumu inanyamuka pamodzi ndi banja lake lonse. Koma iye anasiya azikazi khumi kuti azisamalira nyumba yaufumu.
17 Ke tokosra ac mwet lal nukewa som liki siti uh, elos tui ke lohm se safla.
Kotero mfumu inanyamuka pamodzi ndi anthu onse oyitsatira, ndipo anayima pamalo pena chapatalipo.
18 Mwet pwapa lal nukewa elos tu siskal ke mwet mweun karinginyal elos fahsr ye mutal. Mwet mweun onfoko ma welulma liki acn Gath elos oayapa fahla ye mutal.
Ankhondo ake onse anayamba kuyenda pamaso pa Davide, ndipo Akereti ndi Apeleti, pamodzinso ndi Agiti okwanira 600 amene anamutsata kuchokera ku Gati, nawonso anayenda pamaso pake.
19 Ac tokosra el fahk nu sel Ittai, mwet kol lun mwet Gath inge, “Efu ku kom wi kut som? Folokla muta yurin tokosra sasu sac. Kom sie mwetsac ac kom kaingla liki facl sum sifacna.
Mfumu inati kwa Itai Mgiti, “Nʼchifukwa chiyani iwe ukupita ndi ife? Bwerera ndipo ukakhale ndi mfumu Abisalomu. Iwe ndiwe mlendo munthu wothawa kwawo.
20 Kom tufahna tuku muta yenu kitin pacl na, na efu ku ngan lela kom in wiyu forfor? Nga sifacna, nga tia etu lah nga ac som nu ya. Folokla, ac us mwet lom ingan in wi kom. Lela LEUM GOD Elan kulang ac pwaye nu suwos.”
Wangobwera dzulo lomweli, lero ndikutenge kuti uziyendayenda ndi ife, pamene ine sindikudziwa kumene ndikupita? Bwerera, ndipo tenga abale ako. Chifundo ndi kukhulupirika zikhale nawe.”
21 A Ittai el topuk, “Leum fulat, nga fulahk nu sum inen LEUM GOD lah yen nukewa kom forfor nu we, nga ac wi kom in pacl nukewa, finne nu ke misa.”
Koma Itai anayankha mfumu kuti, “Pali Yehova wamoyo, kulikonse kumene mbuye wanga mfumu mudzakhala, kaya ndi moyo kapena imfa, mtumiki wanu adzakhala komweko.”
22 David el topuk, “Wona. Fahsr nu meet!” Na Ittai el fahsr nu meet wi mwet lal ac sou lalos nukewa.
Davide anati kwa Itai, “Tiye pita nafe” Kotero Itai Mgiti anayenda pamodzi ndi anthu ake ndi mabanja amene anali naye.
23 Mwet uh tung ma lulap ke David ac mwet lal ah som. Tokosra el tupalla Infacl srisrik Kidron, ac mwet lal elos fahsr tokol. Na elos tukeni oatula in som nu yen mwesis.
Anthu onse a madera ozungulira analira mofuwula pamene anthu onsewo amadutsa. Mfumunso inawoloka chigwa cha Kidroni, ndipo anthu onse anayenda kulowera ku chipululu.
24 Zadok, mwet tol, el muta in acn sac, ac mwet Levi su us Tuptup in Wuleang elos muta pac yorol. Elos filiya tuptup sac ac tia sifil srukak nwe ke na mwet nukewa illa liki siti ah. Abiathar, mwet tol, el oasr pac we.
Zadoki anali nawonso, ndipo Alevi onse amene anali naye ananyamula Bokosi la Chipangano la Mulungu. Iwo anayika pansi Bokosi la Mulungulo ndipo Abiatara ankapereka nsembe mpaka pamene anthu onse anamaliza kutuluka mu mzinda.
25 Na tokosra el fahk nu sel Zadok, “Folokunla Tuptup in Wuleang uh nu in siti uh. LEUM GOD El fin insewowo sik, El ac fah lela nga in foloko ac liye, oayapa liye acn oan we uh.
Kenaka mfumu inati kwa Zadoki, “Tenga Bokosi la Mulungu ubwerere nalo mu mzinda. Ngati ndidzapeza chifundo pamaso pa Yehova, adzandibweretsa kuti ndilionenso ndi malo ake okhalamo.
26 A El fin tia insewowo sik, lela Elan oru nu sik fal nu ke lungse lal.”
Koma iye anati, ‘Akapanda kukondwera nane,’ chabwino, andichite chimene chimukomere.”
27 Na el sifilpa fahk nu sel Zadok, “Usalla Ahimaaz wen nutum, ac Jonathan wen natul Abiathar, ac folokla nu in siti ah in misla.
Mfumu inatinso kwa wansembe Zadoki, “Kodi siwe mlosi? Bwerera mu mzinda mwamtendere pamodzi ndi mwana wako Ahimaazi ndi Yonatani mwana wa Abiatara. Iwe ndi Abiatara tengani ana anu awiri.
28 A nga ac muta soanekom ke acn in tupalla infacl uh ke yen mwesis, nwe ke na nga eis kas sum me.”
Ine ndidzadikira powolokera Yorodani ku chipululu mpaka nditalandira mawu ochokera kwa iwe ondiwuza mmene zilili zinthu.”
29 Ouinge Zadok ac Abiathar us Tuptup in Wuleang folokla nu in Jerusalem ac mutana we.
Kotero Zadoki ndi Abiatara ananyamula Bokosi la Mulungu lija nabwerera nalo ku Yerusalemu, ndipo anakakhala kumeneko.
30 David el fahsryak nu Fineol Olive, ac el tung. El tia fahluk, ac el sunya sifal in akkalemye asor lal. Mwet nukewa su fahsr tokol elos afinya pac sifalos ac tung pac.
Koma Davide anapitirira ndi kukakwera phiri la Olivi akupita nalira. Anafunda kumutu koma sanavale nsapato. Anthu onse amene anali naye anafundanso kumutu, ndipo nawonso amalira pamene amapita.
31 Ke fwackyang nu sel David lah Ahithophel el welulla Absalom ac elos su lainul, el pre ac fahk, “O LEUM GOD, nunak munas oru tuh kas in kasru lal Ahithophel in ekla kas lusrongten!”
Tsono Davide anamva kuti, “Ahitofele ali pakati pa anthu owukira pamodzi ndi Abisalomu.” Choncho Davide anapemphera, “Inu Yehova, musandutse uphungu wa Ahitofele ukhale uchitsiru.”
32 Ke David el sun fin tohktok uh, acn se ma acn in alu se oan we, Hushai mwet Arch, kawuk se lal David su el lulalfongi yohk, el tuku sonol, ac nuknuk lal ah mihsalik, ac fohkfok oan fin sifal.
Davide atafika pamwamba pa phiri pomwe anthu ankapembedzerapo Mulungu, Husai Mwariki anadzakumana naye atangʼamba mkanjo wake ndi kudzithira fumbi kumutu.
33 Ac David el fahk nu sel, “Kom ac fah tia mwe kasru nu sik kom fin wiyu inge.
Davide anati kwa iye, “Ngati iwe upite ndi ine, udzakhala chondilemetsa.
34 Tusruktu kom ku in kasreyu kom fin folokla nu in siti ah, ac fahk nu sel Absalom lah inge kom ac kulansupal ke insiom na pwaye, oana ke kom tuh kulansupu papa tumal. Ac oru ma nukewa kom ku in oru in lain kas in kasru lal Ahithophel nu sel.
Koma ngati ubwerera ku mzinda ndi kukanena kwa Abisalomu kuti, ‘Inu mfumu ine ndidzakhala wantchito wanu.’ Mʼmbuyomu ndinali wantchito wa abambo anu koma tsopano ndidzakhala wantchito wanu. Ukatero udzandithandiza kulepheretsa malangizo a Ahitofele.
35 Mwet tol Zadok ac Abiathar eltal ac muta we. Fahkang nu seltal ma nukewa kom lohng in lohm sin tokosra ah.
Kodi ansembe, Zadoki ndi Abiatara, sakukhala nawe kumeneko? Ukawawuze zonse zimene umamva mʼnyumba yaufumu.
36 Wen natultal, Ahimaaz ac Jonathan, eltal oasr yoroltal, ac kom ku in supwaltalma nu yuruk in fahk nu sik ma nukewa ma kom lohng.”
Ana awo awiri, Ahimaazi wa Zadoki, ndi Yonatani mwana wa Abiatara ali nawo pamodzi, uzikawatuma kwa ine ndi china chilichonse chimene ukamve.”
37 Ouinge Hushai, kawuk lal David, el folok nu in siti ah, in pacl se na ma Absalom el utyak nu we.
Ndipo Husai bwenzi la Davide anafika ku Yerusalemu pamene Abisalomu amalowa mu mzinda.

< Luo Samuel 15 >