< Luo Samuel 13 >

1 Oasr sie tamtael lal Absalom, wen natul David, su arulana kato ac el soenna payuk. Inel pa Tamar. Amnon, sie pac sin wen natul David, el arulana lungse Tamar.
Patapita nthawi, Amnoni mwana wa Davide anakonda Tamara, mlongo wa Abisalomu, mwana wa Davide, amene anali wokongola.
2 Yoklana lungse lal nu sel, oru el masak mweyen el nunku mu Tamar el ac koflana muta yorol. Na mweyen Tamar el virgin se, tia filfilla elan ku in osun nu sin mukul.
Amnoni sankagona tulo mpaka anadwala chifukwa cha Tamara mlongo wakeyo, pakuti iye anali asanagonepo ndi mwamuna ndipo zimaoneka kuti zinali zosatheka kuti achite chilichonse kwa iye.
3 Tusruktu oasr kawuk se lal Amnon, su mwet na kutasrik in nunak. El pa Jonadab wen natul Shammah, tamulel lal David.
Koma Amnoni anali ndi mnzake dzina lake Yehonadabu mwana wamwamuna wa Simea, mʼbale wake wa Davide. Yonadabu anali munthu wochenjera kwambiri.
4 Jonadab el fahk nu sel Amnon, “Kom wen sruhk nutin tokosra, a len nukewa nga liye tuh kom ngetnget in asor. Mea se sis an?” Na Amnon el topuk, “Nga arulana lungse Tamar, tamtael lal Absalom, a nga Absalom papa sefanna, nina luo.”
Iye anafunsa Amnoni, “Nʼchifukwa chiyani iwe mwana wa mfumu, umaoneka wowonda mmawa uliwonse? Bwanji wosandiwuza?” Amnoni anamuyankha kuti, “Ine ndamukonda Tamara, mlongo wa mʼbale wanga Abisalomu.”
5 Jonadab el fahk nu sel, “Fahla ona ke bed kiom an, in mu kom mas. Ke papa tomom el tuku in liye kom, na kom fahk nu sel, ‘Nunak munas, sap Tamar tamtael luk, elan tuku kiteyu mongo. Nga lungse elan tuku orala ma nak uh yen nga ac ku in liyal we uh, ac elan sifacna kiteyuwi pac.’”
Yehonadabu anati, “Pita ukagone ndipo unamizire kudwala. Abambo ako akabwera kudzakuona, udzati kwa iwo, Ine ndikufuna mlongo wanga Tamara abwere kuti adzandikonzere chakudya kuti ndidye. Adzandikonzere chakudyacho ine ndikumuona ndi kudya chili mʼmanja mwake.”
6 Na Amnon el oru mu el mas, ac el som ona ke bed kial ah. Tokosra David el som in liyal, ac Amnon el fahk nu sel, “Nunak munas, supwalma Tamar elan tuku orala ekasr cake ah nak inge yen nga ac ku in liyal we, ac elan sifacna kiteyuwi.”
Kotero Amnoni anagona nakhala ngati akudwala. Mfumu itabwera kudzamuona, Amnoni anati kwa iyo, “Ine ndikufuna mlongo wanga Tamara kuti abwere adzandipangire buledi wapamwamba ineyo ndikuona, kuti ndidye ali mʼmanja mwake.”
7 Ouinge David el supwala kas inge nu yorol Tamar, su muta in lohm sin tokosra, “Fahla nu lohm sel Amnon ac orala kutu mongo nal.”
Davide anatumiza mawu kwa Tamara ku nyumba yaufumu kuti, “Pita ku nyumba ya mlongo wako Amnoni ndipo ukamukonzere chakudya.”
8 El som nu we, tuh na Amnon el oan ke bed kial ah. Na Tamar el eis kutu flao takmwek ac sang orauk kutu cake yen Amnon el ku in liyal we. El munanla cake ah,
Choncho Tamara anapitadi ku nyumba ya mlongo wake Amnoni kumalo kumene ankagona. Anakanda ufa, nawumba buledi Amunoniyo akuona ndipo anaphika bulediyo.
9 ac eisla liki pan ah, sang elan mongo, tuh el srangesr. Amnon el fahk, “Sap mwet nukewa in illa.” Ac elos nukewa som.
Kenaka iye anatenga chiwaya ndipo anamupatsa bulediyo, koma iyeyo anakana. Amnoni anati “Uza aliyense atuluke muno.” Ndipo aliyense anatuluka.
10 Na el fahk nu sel Tamar, “Use cake an nu ke bed kiuk uh ac kiteyuwi.” Na Tamar el eis cake ah, ac som nu yorol.
Kenaka Amnoni anati kwa Tamara, “Bweretsa chakudya kuno, ku chipinda changa chogona kuti ndidye chili mʼmanja mwako.” Ndipo Tamara anatenga buledi amene anapanga ndi kubwera naye kwa mlongo wake ku chipinda chake.
11 Ac ke el sang nu sel, Amnon el sruokilya ac fahk, “Fahsru wiyu oan.”
Koma atabweretsa kwa iye kuti adye, anamugwira ndipo anati, “Bwera ugone nane, iwe mlongo wanga.”
12 Na Tamar el fahk, “Mo! Nimet akkohsyeyu in oru kain ouiya fohkfok sacn! Arulana koluk!
Tamara anati kwa iye, “Ayi mlongo wanga! Usandikakamize. Zotere siziyenera kuchitika mu Israeli! Usachite chinthu choyipa chotere.
13 Ku nga ac ngetnget fuka nga fin forfor ye mutun mwet uh? Ac kom, kom ac fah arulana oakasla in facl Israel. Nunak munas, kaskas nu sel tokosra. Nga lulalfongi mu el ku in eisyuwot nu sum.”
Kodi ukuganiza bwanji za ine? Kodi manyazi anga ndidzawachotsa bwanji? Ndipo nanga iweyo? Udzakhalatu monga mmodzi mwa zitsiru zoyipitsitsa muno mu Israeli. Chonde kapemphe kwa mfumu. Sadzakuletsa kuti undikwatire.”
14 A Amnon el tia lohng ma el fahk, na mweyen el ku lukel, el sruinkuilya ac oan yorol.
Koma sanamvere zimene amanena Tamara ndipo popeza anali wamphamvu kuposa Tamarayo, iye anamugwirira.
15 Na Amnon el srungalla na upa. Srunga lal kacl uh alukela lungse lal kacl meet ah, ac el fahk nu sel, “Tiok!”
Atatero Amnoni anadana naye kwambiri. Iyeyo anamuda kuposa momwe anamukondera. Amnoni anati, “Dzuka ndipo tuluka!”
16 Tamar el fahk, “Mo. Kom fin lisyula ouingan, koluk se inge ac tuh yohk liki na ma koluk se kom tufahna orala ah.” Tusruktu Amnon el tiana lohngol.
Iye anayankha, “Ayi! Kundithamangitsa kukhala kulakwa kwakukulu kuposa zimene wachita kale kwa ine.” Koma anakana kumumvera.
17 El pangon mwet kulansap se lal sifacna ac fahk, “Usla mutan se inge liki ye mutuk! Tolulla nu likinum uh ac lakiya srungul an!”
Amnoni anayitana wantchito wake ndipo anati, “Mutulutse mkazi uyu muno ndipo utseke chitseko akatuluka.”
18 Mwet kulansap sac sisella ac lakiya srungul sac. Tamar el nukum nuknuk loeloes se ac loes pac pao ah. In pacl ingo, pa inge nuknuk lun sie mutan fisrak su soenna payuk.
Choncho wantchito wakeyo anamutulutsa ndipo anatseka chitseko atatuluka. Tamara anali atavala mkanjo wokongoletsedwa kwambiri, pakuti ichi chinali chovala chimene ana aakazi a mfumu amene sanagonepo ndi mwamuna amavala.
19 El sang apat nu fin sifal, ac seseya nuknuk loeloes lal, ac afinya mutal ke paol, ac fahsr na tung som.
Tamara anatsira phulusa pamutu pake ndipo anangʼamba mkanjo wokongoletsedwa umene anavalawo. Iye anagwira manja ake kumutu ndipo anachoka, akulira mokweza pamene amapita.
20 Ke Absalom tamulel lal, el liyalak el siyuk, “Ya Amnon el akkolukye kom? Nunak munas, ma louk, nimet sang in arulana aktoasrye kom. El ma pac wiom, na pa kom in tia fahk nu sin kutena mwet kac.” Ouinge Tamar el muta in lohm sel Absalom, ac el asor ac mukaimtal.
Mlongo wake Abisalomu anati, “Kodi Amnoni uja mlongo wako wagona nawe? Khala chete mlongo wanga. Iye uja ndi mlongo wako ndipo usazilabadire.” Choncho Tamara anakhala mʼnyumba ya Abisalomu mlongo wake ngati woferedwa.
21 Ke Tokosra David el lohng ke ma sikyak inge, el foloyak.
Mfumu Davide itamva zimenezi, inakwiya kwambiri.
22 Ac Absalom el arulana srungalla Amnon ke sripen el orekma koluk nu sel Tamar ma loul, na el tiana sifil kas nu sel.
Abisalomu sananene mawu aliwonse kwa Amnoni; abwino kapena oyipa. Iye anamuda Amunoniyo chifukwa anachititsa manyazi mlongo wake Tamara.
23 Yac luo toko ah, Absalom el sang sheep natul ah in kalkul in acn Baal Hazor, apkuran nu ke siti Ephraim. Na el suli mukul nukewa nutin tokosra tuh elos in som nu we.
Patapita zaka ziwiri, pamene wometa nkhosa za Abisalomu anali ku Baala-Hazori pafupi ndi malire a fuko la Efereimu, iye anayitana ana onse aamuna a mfumu kuti apite kumeneko.
24 El som nu yorol Tokosra David ac fahk, “O leum luk, nga sang sheep nutik uh in kalkulla, na nga siyuk lah kom, ac mwet pwapa lom an ku in tuku nu ke pacl in kufwa ah?”
Abisalomu anapita kwa mfumu ndipo anati, “Ometa nkhosa za mtumiki wanu anabwera. Chonde mfumu ndi akuluakulu anu mubwere kudzakhala nane?”
25 Na tokosra el topuk, “Mo, wen nutik. Ac fah yokla elya lom kacsr kut nukewa fin fahsrot.” Absalom el kwafe na, tuh tokosra el tiana wi ma el siyuk ah, ac el sap Absalom elan som.
Mfumu inayankha kuti, “Ayi mwana wanga, tisapite tonsefe. Tidzakhala cholemetsa kwa iwe.” Ngakhale Abisalomu anayesetsa kuwumiriza mfumuyo, inakana kupita. Mʼmalo mwake inangomudalitsa Abisalomuyo.
26 Na Absalom el fahk, “Kwal, fin upa, kom ku in nunak munas fuhlella Amnon tamulel luk, elan tuku?” Ac tokosra el siyuk, “Efu ku elan wi?”
Kenaka Abisalomu anati, “Ngati sizitero, chonde mulole mʼbale wanga Amnoni apite nane.” Mfumu inamufunsa kuti, “Apite nawe chifukwa chiyani?”
27 Na Absalom el kwafe nwe ke na tokosra el tari lela Amnon ac mukul wial nukewa in welul som. Absalom el akoo mongo na lulap se, fal nu sin tokosra.
Koma Abisalomu anamuwumiriza, kotero analola kuti Amnoni pamodzi ndi ana onse a mfumu apite naye.
28 Ac el fahk nu sin mwet kulansap lal ah, “Liye na, tuh ke pacl se Amnon el nimnim nwe sruhila, nga fah fahkla sap se, na komtal unilya. Nimet sangeng. Ma na luk in fosrngakin ma se inge. Komtal in pulaik ac tia sensen.”
Abisalomu analamula antchito ake kuti, “Tamverani! Amnoni akakaledzera ndi vinyo ndipo ine ndikakanena kuti, ‘Mukantheni Amnoni,’ pamenepo mukamuphe. Musakachite mantha. Kodi ine sindinakulamuleni? Mukhale amphamvu ndipo mulimbe mtima.”
29 Ouinge mwet kulansap lal Absalom elos oru oana ma el sapkin, ac unilya Amnon. Wen nukewa natul David saya elos sroang nu fin kosro natulos, ac kaingla.
Kotero antchito a Abisalomu anachita kwa Amnoni zimene Abisalomu anawalamula. Kenaka ana onse a mfumu anayimirira ndipo anakwera pa abulu awo nathawa.
30 Ke elos srakna fahsr inkanek lalos in folok nu yen selos ah, fwackyang nu sel David mu, “Absalom el uniya nufon wen nutum ah. Tia sie selos lula!”
Ali mʼnjira, Davide anamva mphekesera yakuti, “Abisalomu wakantha ana onse a mfumu ndipo palibe ndi mmodzi yemwe amene watsala.”
31 Tokosra el tuyak ac seya nuknuk lal ke el arulana asor, ac el putati nu infohk uh. Mwet kulansap lal ma welul in pacl sac elos seya pac nuknuk lalos.
Mfumu inayimirira, ningʼamba zovala zake ndi kugona pa dothi. Antchito ake onse anayimirira pomwepo atangʼamba zovala zawo.
32 A Jonadab wen natul Shammah, tamulel lal David, el fahk, “Leum fulat, elos tia uniya nufon wen nutum ah. Amnon mukena pa misa. Kalem na lah Absalom el tuh akoo nunak se lal inge e in len se ma Amnon el akkolukyalla Tamar, ma lohl.
Koma Yehonadabu mwana wa Simea, mʼbale wake wa Davide anati, “Mbuye wanga mfumu musaganize kuti wapha ana onse a mfumu; wafa ndi Amnoni yekha. Awa ndiwo akhala maganizo a Abisalomu kuyambira tsiku limene Amnoni anagwirira mlongo wake Tamara.
33 Na pa nimet kom lulalfongi pweng se ma fahk mu wen nutum nukewa misa ah. Amnon mukena anwuki.”
Mbuye wanga mfumu musavutike ndi maganizo ndi nkhani yoti ana onse a mfumu afa. Wafa ndi Amnoni yekha.”
34 In pacl se na ingan Absalom el kaingla. Na mwet mweun se su topang in acn sac, el liye u na lulap se oatui fineol uh me, ke inkanek nu Horonaim. El som nu yorol tokosra ac fahkak ma el liye.
Nthawi imeneyi nʼkuti Abisalomu atathawa. Tsono munthu amene amalondera anayangʼana ndipo anaona anthu ambiri pa msewu wa kumadzulo kwake, akubwera kutsetsereka phiri. Mlondayo anapita kukawuza mfumu kuti, “Ndikuona anthu pa njira ya Horonaimu, mʼmbali mwa phiri.”
35 Jonadab el fahk nu sel David, “Wen nutum an pa tuku ingan, oana ke nga fahk ah.”
Yehonadabu anati kwa mfumu, “Taonani ana a mfumu afika. Zachitika monga momwe mtumiki wanu ananenera.”
36 Ke el tufahna safla in fahk ma inge, na wen natul David ah utyak, ac elos mutawauk in tung, ac David ac mwet pwapa lal ah wi pac tung na upa.
Pamene amatsiriza kuyankhula, ana a mfumu analowa, akulira mofuwula. Mfumunso ndi antchito ake onse analira mokhudzidwa.
37 Na Absalom el kaingla ac som nu yurin Tokosra Talmai, wen natul Ammihud, lun acn Geshur. David el tung kacl Amnon, wen natul, pacl na loeloes.
Abisalomu anathawa, napita kwa Talimai mwana wa Amihudi, mfumu ya ku Gesuri. Koma mfumu Davide inalira mwana wake tsiku ndi tsiku.
38 Absalom el muta in acn Geshur ke yac tolu.
Abisalomu atathawa ndi kupita ku Gesuri, anakhala kumeneko zaka zitatu.
39 Na ke David el tila asor ke misa lal Amnon, el arulana ke liyalak Absalom, wen natul.
Ndipo Davide anagwidwa ndi chifundo chofuna kumulondola Abisalomu pakuti anali atatonthozedwa pa imfa ya Amnoni.

< Luo Samuel 13 >