< Luo Tokosra 1 >

1 Tukun Tokosra Ahab lun Israel el misa, acn Moab tuyak ac alein nu sin Israel.
Atamwalira Ahabu, Mowabu anawukira Israeli.
2 Tokosra Ahaziah lun Israel el putatla ke sawalsrisr fulat in lohm sel in acn Samaria ac arulana musalla manol. Ouinge el supwala kutu mwet lal in som lolngok yorol Baalzebub, god lun acn Ekron, sie siti in acn Philistia, in konauk lah el ac kwela ku tia.
Ndipo Ahaziya anagwa kuchokera pa khonde la chipinda chake chammwamba ku Samariya, ndipo anavulala kwambiri. Choncho iye anatuma amithenga nawawuza kuti, “Pitani mukafunse kwa Baala-zebubu, mulungu wa ku Ekroni, ngati ndichire matendawa.”
3 A sie lipufan lun LEUM GOD sapkin nu sel Elijah, mwet palu in acn Tishbe, elan som osun nu sin mwet lal Tokosra Ahaziah ac siyuk selos, “Efu kowos ku som lolngok yorol Baalzebub, god lun Ekron? Ya mweyen kowos nunku mu wangin god lun Israel?
Koma mngelo wa Yehova anawuza Eliya wa ku Tisibe kuti, “Nyamuka, pita ukakumane ndi amithenga a mfumu ya ku Samariya ndipo ukawafunse kuti, ‘Kodi popeza kulibe Mulungu ku Israeli, nʼchifukwa chake inu mukupita kukafunsa nzeru kwa Baala-zebubu, mulungu wa ku Ekroni?’
4 Fahk nu sel tokosra lah LEUM GOD El fahk, ‘Kom ac fah tia kwela. Kom ac misa!’” Elijah el oru oana ma LEUM GOD El sapkin,
Tsono Yehova akuti, ‘Iweyo sudzadzuka pa bedi wagonapo. Udzafa ndithu!’” Ndipo Eliya ananyamuka.
5 ac mwet ma supweyuk sel tokosra inge folokla nu yorol. Na tokosra el siyuk, “Efu kowos ku sa na foloko?”
Amithenga aja atabwerera kwa mfumu, mfumuyo inawafunsa kuti, “Chifukwa chiyani mwabwerera?”
6 Elos topuk, “Kut sun mwet se su fahk nu sesr kut in foloko fahk nu sum mu LEUM GOD El fahk nu sum ouinge, ‘Efu kom ku supweyuk mwet in som lolngok yorol Baalzebub, god lun Ekron? Ya mweyen kom nunku mu wangin god lun Israel? Kom ac tia kwela. Kom ac misa!’”
Iwo anayankha kuti, “Munthu wina anabwera kudzakumana nafe, ndipo anatiwuza kuti, bwererani kwa mfumu imene inakutumani ndipo mukayiwuze kuti, ‘Yehova akuti, kodi popeza kulibe Mulungu ku Israeli, nʼchifukwa chake mukupita kukafunsa nzeru kwa Baala-zebubu, mulungu wa ku Ekroni? Tsono sudzadzuka pa bedi wagonapo. Udzafa ndithu!’”
7 Ac tokosra el siyuk, “Fuka luman mwet sacn?”
Mfumu inafunsa amithengawo kuti, “Kodi munthu amene anabwera kudzakumana nanuyo ndi kukuwuzani zimenezi amaoneka bwanji?”
8 Ac elos topuk, “El nukum nuknuk lik se orekla ke unen kosro, ac losya infulwal ke pel se orekla ke kulun kosro.” Na tokosra el fahk, “Elijah pa mwet sacn!”
Iwo anayankha kuti, “Munthuyo anavala zovala zaubweya ndi lamba wachikopa mʼchiwuno mwake.” Mfumu inati, “Munthu ameneyo ndi Eliya wa ku Tisibe.”
9 Na el supwala sie mwet leum lun mwet mweun wi mwet lumngaul lal in som usalu Elijah. Mwet leum sac konalak ke el muta fin inging soko ac el fahk nu sel Elijah, “Mwet lun God, tokosra el sap kom in oatui.”
Pamenepo mfumu inatuma mtsogoleri wa ankhondo ndi anthu ake makumi asanu kwa Eliya. Mtsogoleriyo anapita kwa Eliya, amene anali atakhala pamwamba pa phiri, ndipo anati, “Munthu wa Mulungu, mfumu ikuti, ‘Tsikani!’”
10 Elijah el topuk, “Nga fin mwet lun God, lela e in tuku inkusrao me unikomi ac mwet lom ingan!” In pacl sacna, e tuku inkusrao me ac uniya leum sac ac mwet lal ah.
Eliya anayankha mtsogoleriyo kuti, “Ngati ndine munthu wa Mulungu, moto utsike kuchokera kumwamba, ukupsereze iwe pamodzi ndi anthu makumi asanu akowo!” Pomwepo moto unatsikadi kuchokera kumwamba ndipo unapsereza mtsogoleriyo pamodzi ndi anthu akewo.
11 Tokosra el supwala pac sie leum wi mwet lumngaul lal, su som ac fahk nu sel Elijah, “Mwet lun God, tokosra el sap kom in oatui ingena!”
Zitachitika izi, mfumu inatumanso mtsogoleri wina pamodzi ndi asilikali ake makumi asanu. Mtsogoleriyo anati kwa Eliya, “Munthu wa Mulungu, zimene mfumu ikunena ndi izi, ‘Tsikani msangamsanga!’”
12 Elijah el topuk, “Nga fin mwet lun God, lela e in tuku inkusrao me unikomi ac mwet lom ingan!” In pacl sacna, e lun God tuku lucng me ac uniya leum sac ac mwet lal ah.
Eliya anayankha kuti, “Ngati ndine munthu wa Mulungu, moto utsike kuchokera kumwamba, ukupsereze iwe pamodzi ndi anthu ako makumi asanuwo!” Pomwepo moto unatsikadi kuchokera kumwamba ndipo unapsereza mtsogoleriyo pamodzi ndi anthu akewo.
13 Na tokosra el sifilpa supwala sie pac leum wi mwet lumngaul lal. El utyak nu fin inging soko ah, sikukmutunteyak ye mutal Elijah ac kwafe sel, “Mwet lun God, pakoten nu sik ac mwet luk inge. Nimet unikuti!
Ndipo mfumu inatumanso mtsogoleri wachitatu pamodzi ndi asilikali ake makumi asanu. Mtsogoleri wachitatuyu anakwera pa phiripo ndi kugwada pamaso pa Eliya. Iye anayankhula mopemba kuti, “Munthu wa Mulungu, chonde musandiwononge ineyo pamodzi ndi atumiki makumi asanu anuwa!
14 Leum luo meet ah wi mwet laltal ah anwuki ke e inkusrao me. A nga siyuk kom in nunak munas ac pakoten nu sik!”
Taonani, moto unatsika kuchokera kumwamba ndi kupsereza atsogoleri awiri pamodzi ndi anthu awo onse. Koma tsopano musawononge moyo wanga!”
15 Lipufan lun LEUM GOD fahk nu sel Elijah, “Oatui welul ac nimet sangeng.” Ouinge Elijah el wi mwet leum sac som nu yorol tokosra
Mngelo wa Yehova anati kwa Eliya, “Pita naye, usamuope.” Choncho Eliya ananyamuka natsika naye limodzi kupita kwa mfumu.
16 ac fahk nu sel, “Pa inge ma LEUM GOD El fahk, ‘Mweyen kom supwala mwet in som lolngok yorol Baalzebub, god lun Ekron, srulukin wangin god lun Israel kom in lolngok se, na pa kom ac tia kwela. Kom ac misa!’”
Eliya anawuza mfumu kuti, “Yehova akuti, ‘Chifukwa chiyani munatumiza amithenga kwa Baala-zebubu, mulungu wa ku Ekroni, kukafunsa ngati muti muchire? Kodi mu Israeli mulibe Mulungu woti nʼkukuyankhani funso lanu? Choncho, popeza mwachita izi, simudzadzuka pamene mwagonapo; mudzafa ndithu.’”
17 Ahaziah el misa oana ma LEUM GOD El fahkak sel Elijah. Wangin wen natul Ahaziah, na pa Joram tamulel lal, el aolul in tokosra ke yac akluo ke pacl in leum lal Jehoram wen natul Jehoshaphat, tokosra lun Judah.
Motero Ahaziya anafadi, monga mwa mawu a Yehova amene Eliya anayankhula. Tsono popeza Ahaziya analibe mwana, Yoramu analowa ufumu mʼmalo mwake mʼchaka chachiwiri cha Yehoramu mwana wa Yehosafati mfumu ya ku Yuda.
18 Ma nukewa saya ma Tokosra Ahaziah el orala, simla oasr in [Sramsram Matu Ke Tokosra Lun Israel.]
Ntchito zina zonse zimene Ahaziya anachita, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a ku Israeli?

< Luo Tokosra 1 >